< Levitiko 18 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
Još reèe Gospod Mojsiju govoreæi:
2 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Kaži sinovima Izrailjevim, i reci im: ja sam Gospod Bog vaš.
3 Musamachite zomwe amachita anthu a ku Igupto kumene munkakhala kuja, ndiponso musamachite zomwe amachita anthu a ku Kanaani kumene ndikukupititsani. Musatsatire miyambo yawo.
Nemojte èiniti što se èini u zemlji Misirskoj, u kojoj ste živjeli, niti èinite što se èini u zemlji Hananskoj, u koju vas vodim, i po uredbama njihovijem nemojte živjeti.
4 Inu muzimvera malamulo anga ndipo muzisamalitsa kutsatira malangizo anga. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Nego moje zakone vršite i moje uredbe držite živeæi po njima. Ja sam Gospod Bog vaš.
5 Choncho sungani malangizo ndi malamulo anga, popeza munthu amene amvera zimenezi adzakhala ndi moyo. Ine ndine Yehova.
Držite uredbe moje i zakone moje; ko ih vrši, živ æe biti kroz njih. Ja sam Gospod.
6 “‘Munthu aliyense asagonane ndi wachibale wake. Ine ndine Yehova.
Niko da ne pristupa k rodici svojoj po krvi, da otkrije golotinju njezinu. Ja sam Gospod.
7 “‘Usachititse manyazi abambo ako pogonana ndi amayi ako. Iwo ndi amayi ako. Usagonane nawo.
Golotinje oca svojega ni golotinje matere svoje ne otkrij; mati ti je; ne otkrij golotinje njezine.
8 “‘Usagonane ndi mkazi wa abambo ako (osakhala amayi okubala). Ukatero ukuchititsa manyazi abambo ako.
Golotinje žene oca svojega ne otkrij; golotinja je oca tvojega.
9 “‘Usagonane ndi mlongo wako, mwana wamkazi wa abambo ako, kapena mwana wamkazi wa amayi ako, kaya anabadwira mʼnyumba mwanu kapena kwina.
Golotinje sestre svoje, kæeri oca svojega ili kæeri matere svoje, koja je roðena u kuæi ili izvan kuæe, ne otkrij golotinje njihove.
10 “‘Usagonane ndi mdzukulu wako: mwana wa mwana wako wamwamuna kapena mwana wa mwana wako wamkazi. Kutero nʼkudzichotsa ulemu.
Golotinje kæeri sina svojega, ili kæeri kæeri svoje ne otkrij; jer je tvoja golotinja.
11 “‘Usagonane ndi mwana wamkazi wa mkazi wa abambo ako, amene abambo akowo anabereka; popeza ameneyo ndi mlongo wako.
Golotinje kæeri žene oca svojega, koju je rodio otac tvoj, ne otkrij; sestra ti je.
12 “‘Usagonane ndi mlongo wa abambo ako; popeza ameneyo ndi thupi limodzi ndi abambo ako.
Golotinje sestre oca svojega ne otkrij; jedna je krv s ocem tvojim.
13 “‘Usagonane ndi mchemwali wa amayi ako chifukwa ameneyo ndi thupi limodzi ndi amayi ako.
Golotinje sestre matere svoje ne otkrij; jer je jedna krv s materom tvojom.
14 “‘Usachititse manyazi mchimwene wa abambo ako pogonana ndi mkazi wake popeza amenewo ndi azakhali ako.
Golotinje brata oca svojega ne otkrij pristupajuæi k ženi njegovoj; strina ti je.
15 “‘Usagonane ndi mpongozi wako popeza ameneyo ndi mkazi wa mwana wako. Choncho usamuchititse manyazi.
Golotinje žene sina svojega ne otkrij; snaha ti je, ne otkrij golotinje njezine.
16 “‘Usagonane ndi mkazi wa mchimwene wako popeza potero ukuchititsa manyazi mʼbale wakoyo.
Golotinje žene brata svojega ne otkrij; golotinja je brata tvojega.
17 “‘Usagonane ndi mkazi ndiponso mwana wake wamkazi. Usagonane ndi mwana wamkazi wa mwana wake wamwamuna, kapena mwana wamkazi wa mwana wake wamkazi. Amenewo ndi thupi limodzi ndi mkaziyo. Kutero ndikuchita chinthu choyipa kwambiri.
Golotinje žene i kæeri njezine ne otkrij; kæeri sina njezina ni kæeri kæeri njezine nemoj uzeti da otkriješ golotinju njihovu; jedna su krv; zlo je.
18 “‘Usakwatire mchemwali wa mkazi wako ndi kumagonana naye mkazi wakoyo ali moyo ngati wopikisana naye.
Nemoj uzeti žene preko jedne žene, da je ucvijeliš otkrivajuæi golotinju drugoj za života njezina.
19 “‘Usamuyandikire mkazi kuti ugonane naye pa nthawi yake yosamba.
K ženi dokle se odvaja radi neèistote svoje ne idi da otkriješ golotinju njezinu.
20 “‘Usagonane ndi mkazi wa mnzako ndi kudziyipitsa naye.
Sa ženom bližnjega svojega ne lezi skvrneæi se s njom.
21 “‘Usapereke mwana wako aliyense kuti akhale nsembe yamoto kwa Moleki ndi kuyipitsa dzina la Yehova. Ine ndine Yehova.
Od sjemena svojega ne daj da se odnese Molohu, da ne oskvrniš imena Boga svojega; ja sam Gospod.
22 “‘Usagonane ndi mwamuna ngati mkazi; chimenecho ndi chinthu chonyansa.
S muškarcem ne lezi kao sa ženom; gadno je.
23 “‘Usagonane ndi nyama ndi kudziyipitsa nayo. Mkazi asadzipereke kwa nyama kuti agonane nayo. Chimenecho ndi chisokonezo.
Živinèeta nikakoga nemoj obležati skvrneæi se s njim; i žena da ne legne pod živinèe; grdilo je.
24 “‘Musadzidetse ndi zinthu zimenezi chifukwa umo ndi mmene mitundu ina imene ndikuyithamangitsa pamaso panu inadzidetsera.
Nemojte se skvrniti nijednom ovom stvarju; jer su se svijem tijem stvarima oskvrnili narodi koje æu odagnati ispred vas.
25 Choncho dziko linayipa ndipo ndinalilanga chifukwa cha tchimo lake. Motero dzikolo linasanza anthu ake okhalamo.
Jer se oskvrnila zemlja, i nevaljalstvo æu njezino pohoditi na njoj, i izmetnuæe zemlja stanovnike svoje.
26 Koma inu mukasunge malangizo ndi malamulo anga. Mbadwa ndiponso alendo amene akukhala pakati panu asakachite china chilichonse cha zinthu zonyansazi,
Nego vi držite zakone moje i uredbe moje, i ne èinite nijednoga ovoga gada, ni domorodac ni došljak koji se bavi meðu vama;
27 pakuti zinthu zonsezi ndi zomwe ankachita anthu amene ankakhala mʼdzikomo inu musanafike, ndipo dziko linayipitsidwa.
Jer sve ove gadove èiniše ljudi u ovoj zemlji koji su bili prije vas, i zemlja je od toga oskvrnjena;
28 Koma inu musachite zimenezi kuti dziko lingakusanzeni mutaliyipitsa monga linasanzira mitundu imene imakhalamo inu musanafike.
Da ne izmetne zemlja vas, ako je oskvrnite, kao što je izmetnula narod koji je bio prije vas.
29 “‘Aliyense wochita zinthu zonyansa zimenezi achotsedwe pakati pa anthu anzake.
Jer ko uèini štogod od ovijeh gadova, istrijebiæe se iz naroda svojega duše koje uèine.
30 Choncho mverani malangizo anga oletsa kuchita miyambo yonyansayi imene ankatsatira anthu amene analipo inu musanafike ndi kudziyipitsa nayo. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’”
Zato držite što sam naredio da se drži, da ne èinite što od gadnijeh obièaja koji su bili prije vas, i da se ne skvrnite o njih. Ja sam Gospod Bog vaš.

< Levitiko 18 >