< Yohane 1 >

1 Pachiyambi panali Mawu, ndipo Mawu anali kwa Mulungu, ndipo Mawu ndiye Mulungu.
MAJAN kotier ni tapi o, a majan kotier ren Kot, a majan me udan Kot.
2 Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.
I me kotikot ren Kot ni tapi o.
3 Zinthu zonse zinalengedwa ndi Iye; ndipo popanda Iye sikukanakhala kanthu kalikonse kolengedwa.
I me dipijou karoj tapi kidar, o jota man meakot mia, me kaidin i kotin wiadar
4 Mwa Iye munali moyo, ndipo moyowo unali kuwunika kwa anthu.
Maur mi re a; o iei maur o marain en aramaj.
5 Kuwunika kunawala mu mdima, koma mdimawo sunakuzindikire.
A marain o me dakarada rotorot, a rotorot jota linan kila.
6 Kunabwera munthu amene anatumizidwa kuchokera kwa Mulungu; Iyeyo dzina lake linali Yohane.
Aramaj amen me pakadarador jan ren Kot ad a loanej!
7 Iye anabwera ngati mboni kudzachitira umboni kuwunikako kuti kudzera mwa iye anthu onse akhulupirire.
I me pwara don kadede, pwen kadede marain o pwe karoj en pojon pweki i.
8 Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.
Kaidin i me marain o, a a kin kadede marain o.
9 Kuwunika koona kumene kuwunikira munthu aliyense kunabwera ku dziko lapansi.
Iei marain melel, me pwara don jappa, ap kamaraini aramaj karoj.
10 Iye anali mʼdziko lapansi, ndipo ngakhale kuti dziko lapansi linalengedwa ndi Iye, dziko lapansilo silinamuzindikire Iye.
I me kotier jappa, o i me jappa tapi kidar, a jappa jaja i.
11 Iye anabwera kwa iwo amene anali akeake, koma akewo sanamulandire Iye.
A koti don udan japwilim a, a japwilim a kan me jan i.
12 Koma kwa onse amene anamulandira Iye, kwa amene anakhulupirira mʼdzina lake, Iye anawapatsa mphamvu yokhala ana a Mulungu;
Karoj, me kajamo i, a kotiki on ir manaman, en wiala jeri en Kot, ir, me pojon mar a,
13 ana wobadwa osati monga mwachilengedwe, kapena chisankho cha munthu, kapena chifuniro cha mwamuna koma wobadwa mwa Mulungu.
Me kaidin ipwidi jan nta, de inon en uduk, de inon en ol o, pwe ipwidier jan ren Kot.
14 Mawu anasandulika thupi ndipo anakhala pakati pathu. Ife tinaona ulemerero wake, ulemerero wa Iye amene ndi Mwana mmodzi yekhayo wa Atate, wodzaza ndi chisomo ndi choonadi.
Majan me wia uduk ala okotikot re atail, o kitail kilaner a linan, linan dueta linan en leroj eu jan ren Jam o, me dir en mak melel.
15 Yohane achitira umboni za Iye. Iye akufuwula kuti, “Uyu ndi Iye amene ndinati, ‘Iye amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa, Iyeyo analipo ine ndisanabadwe.’”
loanej me kadede i nil laudeda indada: lei i, me i padaki wei: Me pan kotido mur i, iei me mier mo i, pwe a kotikotier mo i.
16 Kuchokera mʼkuchuluka kwa chisomo chake ife tonse talandira madalitso pamwamba pa madalitso.
Pwe kitail karoj ale jan nan audepa a mak japan potopot.
17 Pakuti lamulo linapatsidwa kudzera mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinabwera kudzera mwa Yesu Khristu.
Pwe kapun me kokido jan Mojej, a mak o melel jan Iejuj Krijtuj.
18 Palibe munthu amene anaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekhayo amene ali wa pamtima pa Atate, ndiye anafotokoza za Iye.
Jota me kilaner Kot kokodo, o ieroj ta, me kin kotikot pan kupur en Jam o, i me kotin kajaledar i.
19 Tsopano uwu ndi umboni wa Yohane pamene Ayuda a ku Yerusalemu anatumiza ansembe ndi Alevi kudzamufunsa kuti iye anali yani.
A met en Ioanej a kadede, ni men Juj kadarala jan Ierujalem jamero o lepit oko, pwen idok re a: Ij koe
20 Iye sanalephere kuvomereza, koma iye anavomereza momasuka kuti, “Ine sindine Khristu.”
I ari kotin kadede; a jota likam; a kotin kadede: Kaidin Krijtuj nai.
21 Iwo anamufunsa kuti, “Nanga iwe ndiwe yani? Kodi ndiwe Eliya?” Iye anati, “Sindine.” “Kodi ndiwe Mneneri?” Iye anayankha kuti, “Ayi.”
Irail idok re a: A ij? Eliaj komui? A majani: Kaidin nai i. Komui jaukop o? A japen: Kaidin.
22 Pomaliza iwo anati, “Ndiwe yani? Tipatse yankho kuti tipite nalo kwa amene anatituma. Kodi iwe ukuti chiyani za iwe mwini?”
Irail ap indan i: A ij komui? Pwe jen japen irail me kadar kit dor. Da me komui kadedeki pein komui?
23 Yohane anayankha ndi mawu a mneneri Yesaya kuti, “Ine ndi mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Wongolani njira ya Ambuye.’”
A majani: Nai nil eu, me likelikwir jili nan jap tan: Kaineneda al en Kaun o, duen jaukop Iejaia majanier!
24 Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa
A irail pakadaradoer jan ren Parijar akan.
25 anamufunsa Iye kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani, umabatiza ngati iwe si Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneri?”
Irail ap idok re a indada: Da me komui wia paptaijiki, ma komui kaidin Krijtuj, o kaidin Eliaj, o pil kaidin jaukop o?
26 Yohane anayankha kuti, “Ine ndimabatiza ndi madzi, koma pakati panu payima amene simukumudziwa.
Ioanej japen irail majani: Nai me paptaijiki pil, a amen kin kotikot nan pun omail, me komail jaja.
27 Iye ndi amene akubwera pambuyo panga, ine siwoyenera kumasula zingwe za nsapato zake.”
lei i me kotido mur i, me nai jowar on, en lapwada jal en japwilim a jut.
28 Zonsezi zinachitika ku Betaniya kutsidya lina la mtsinje wa Yorodani, kumene Yohane ankabatizira.
Mepukat wiauier Petapara palilan Iordan, waja Ioanej kin wia paptaij ia.
29 Pa tsiku lotsatira Yohane anaona Yesu akubwera kwa iye ndipo anati, “Taonani, Mwana Wankhosa wa Mulungu, amene achotsa tchimo la dziko lapansi!
Mandan ran o a majani Iejuj a koti don i ap majani: Kilan Jippul en Kot, me kin wawei dip en jappa!
30 Uyu ndi amene ndimatanthauza pamene ndinanena kuti, ‘Munthu amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa analipo ine ndisanabadwe.’
lei i, me i padaki wei: ol amen pan kotido mur i iei, me mier mo i, pwe a kotikotier mo i.
31 Ine mwini sindinamudziwe Iye, koma ndinabwera kubatiza ndi madzi kuti Iye adziwike mu Israeli.”
A nai jo aja i, a pwe i en janjal don Ijrael, iei me i kokido paptaijiki pil.
32 Kenaka Yohane anapereka umboni uwu: “Ine ndinaona Mzimu Woyera ngati nkhunda kuchokera kumwamba nakhala pa Iye.
A Ioanej kadede majani: I kilaner Nen o kotidido jan nanlan ni mom en muroi kotikot re a.
33 Ine sindikanamudziwa Iye, koma kuti amene anandituma ine kudzabatiza ndi madzi anati kwa ine, ‘Munthu amene udzaona Mzimu Woyera akutsika nakhazikika pa Iye ndi amene adzabatize ndi Mzimu Woyera.’
A nai jo aja i, a me porone ia don wia paptaijiki pil, iei me kotin majani on ia: Me koe pan kilan. Nen piridi jok poa, o kotikoteta re a, iei i, me kin wia paptaijiki Nen jaraui.
34 Ine ndaona ndipo ndikuchitira umboni kuti uyu ndi Mwana wa Mulungu.”
A i kilanadar ap kadedeki, me iei Japwilim en Kot.
35 Pa tsiku lotsatira Yohane analinso pamenepo pamodzi ndi awiri a ophunzira ake.
Mandan ran o Ioanej pil kotida waja o, o na tounpadak riamen ian i.
36 Iye ataona Yesu akudutsa anati, “Taonani Mwana Wankhosa wa Mulungu!”
A ni a udial Iejuj kotikot kokodo, ap majani: Kilan Jippul en Kot!
37 Ophunzira ake awiriwo atamva iye akunena izi, iwo anamutsatira Yesu.
A tounpadak riamen ronadar a majan, ap idauen wei Iejuj.
38 Atatembenuka, Yesu anaona iwo akumutsatira ndipo anawafunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” Iwo anati, “Rabi (kutanthauza kuti Aphunzitsi), kodi mukukhala kuti?”
Iejuj ap kotin jaupeido majani ara idedauen, ap kotin majani on ira: Da me koma rapaki? Ira potoan on: Rapi (iet wewe: Jaunpadak), ia waja re kin kotikot ia?
39 Iye anayankha kuti, “Bwerani mudzaone.” Choncho iwo anapita ndi kukaona kumene Iye amakhala, ndipo anakhala naye tsiku limenelo. Linali ngati pafupifupi ora la khumi.
A kotin majani on ira: Kodo kilan! Ira ap poto don kilaner waja, me a kotikot ia, ap mimieta re a ni ran o. Mepukat wiauier impan auer kaeijok.
40 Andreya mʼbale wake wa Simoni Petro, anali mmodzi wa awiriwo amene anamva zimene Yohane ananena ndiponso amene anamutsata Yesu.
Andreaj, ri en Jimon Petruj amen re ra, me ronadar jan ren Ioanej ap idedauen i.
41 Choncho chimene Andreya anachita ndi kukapeza mʼbale wake Simoni ndipo anamuwuza kuti, “Ife tamupeza Mesiya,” (kutanthauza kuti Khristu).
I me diaradar maj udan ri a Jimon, indai on i: Je diaradar Mejiaj (iet wewe: Krijtuj).
42 Kenaka iye anabweretsa Simoni kwa Yesu, amene anamuyangʼana ndipo anati, “Iwe ndiwe Simoni, mwana wa Yohane. Udzatchedwa Kefa” (limene litanthauza kuti Petro).
I ap kalualan i ren Iejuj. A Iejuj lao majani i, ap majani: Jimon, koe nain Iona, koe nok adaneki Kepaj (iet wewe: Paip).
43 Pa tsiku lotsatira Yesu anaganiza zopita ku Galileya. Atamupeza Filipo, anati kwa iye, “Nditsate.”
Mandan ran o a pan kotilan Kalilaa, Iejuj ap kotin diaradar Pilipuj, majani on i: Idauen ia do!
44 Filipo monga Andreya ndi Petro, anali wochokera ku mzinda mudzi Betisaida.
Pilipuj men Petjaida, kanim en Andreaj o Petruj.
45 Filipo anakapeza Natanieli ndipo anamuwuza kuti, “Ife tapeza amene Mose analemba za Iye mʼmalamulo, ndi zimene aneneri analembanso za Iye, Yesu wa ku Nazareti, mwana wa Yosefe.”
Pilipuj diaradar Natanael, ap indan i: Je diaradar i, duen me Mojej intiniedier nan puk en kapun o jaukop akan: Iejuj men Najaret, japwilim en Iojep.
46 Natanieli anafunsa kuti, “Nazareti! Kodi kanthu kalikonse kabwino kangachokere kumeneko?” Filipo anati, “Bwera udzaone.”
A Natanael indai on i: Pala maukot pan kak pwarada jan Najaret? Pilipuj indan i: Kodo kilan!
47 Yesu atamuona Natanieli akuyandikira, anati kwa iye, “Uyu ndi Mwisraeli weniweni, mwa iye mulibe chinyengo.”
Iejuj kotin majani Natanael koko don i, ap majani duen i: Kilan, ol melel en Ijrael amen, me jota kin widin.
48 Natanieli anafunsa kuti, “Kodi mwandidziwa bwanji?” Yesu anayankha kuti, “Ine ndinakuona iwe utakhala pansi pamtengo wamkuyu Filipo asanakuyitane.”
Natanael potoan on i: Re kotin mani ia jan ia? Iejuj kotin japen majani on i: Mon Pilipuj a eker uk edo, ni om mod pan tuka pik o, I kilan uk ada.
49 Kenaka Natanieli ananena kuti, “Rabi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu; Inu ndinu Mfumu ya Israeli.”
Natanael japen potoan on i: Rapi, ir me Japwilim en Kot, ir me Nanmarki en Ijrael.
50 Yesu anati, “Ukukhulupirira chifukwa chakuti ndakuwuza kuti Ine ndinakuona iwe uli pansi pamtengo wamkuyu? Iwe udzaona zinthu zazikulu kuposa izo.”
Iejuj kotin japen majani on i: Pweki I indai on uk, me I kilan uk ada pan tuka pik o, iei me koe pojonki, a koe nok kilan me lapa jan mepukat.
51 Ndipo Iye anapitirira kuti, “Zoonadi, Ine ndikuwuza kuti iwe udzaona kumwamba, kutatsekuka ndi angelo a Mulungu akukwera ndi kutsika pa Mwana wa Munthu.”
A kotin majani on i: Melel, melel I indai on komail, jan met komail pan kilan nanlan a ritida o tounlan en Kot akan dauda o daudi pwarado ren Nain aramaj.

< Yohane 1 >