< Yobu 35 >

1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
Therfor Helyu spak eft these thingis, Whethir thi thouyt semeth euene,
2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
`ether riytful, to thee, that thou schuldist seie, Y am riytfulere than God?
3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
For thou seidist, That, that is good, plesith not thee; ethir what profitith it to thee, if Y do synne?
4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
Therfor Y schal answere to thi wordis, and to thi frendis with thee.
5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
Se thou, and biholde heuene, and biholde thou the eir, that God is hiyere than thou.
6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
If thou synnest `ayens hym, what schalt thou anoye hym? and if thi wickidnessis ben multiplied, what schalt thou do ayens hym?
7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
Certis if thou doist iustli, what schalt thou yyue to hym; ether what schal he take of thin hond?
8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
Thi wickidnesse schal anoie a man, which is lijk thee; and thi riytfulnesse schal helpe the sone of a man.
9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
Thei schulen cry for the multitude of fals chalengeris, and thei schulen weile for the violence of the arm of tirauntis.
10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
And Joob seide not, Where is God, that made me, and that yaf songis in the nyyt?
11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
Which God techith vs aboue the beestis of erthe, and he schal teche vs aboue the briddis of heuene.
12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
There thei schulen crye, and God schal not here, for the pride of yuele men.
13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
For God schal not here with out cause, and Almyyti God schal biholde the causis of ech man.
14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
Yhe, whanne thou seist, He biholdith not; be thou demed bifor hym, and abide thou hym.
15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
For now he bryngith not in his strong veniaunce, nether vengith `greetli felonye.
16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”
Therfor Joob openith his mouth in veyn, and multiplieth wordis with out kunnyng.

< Yobu 35 >