< Yobu 3 >

1 Pambuyo pake Yobu anatsekula pakamwa pake nayamba kutemberera tsiku limene iyeyo anabadwa.
Potom otvori usta svoja Jov i stade kleti dan svoj.
2 Ndipo Yobu anati:
I progovoriv Jov reèe:
3 “Tsiku limene ine ndinabadwa litembereredwe ndi usiku umene ananena kuti, ‘Mwana wamwamuna wabadwa!’
Ne bilo dana u koji se rodih, i noæi u kojoj rekoše: rodi se djetiæ!
4 Tsiku limenelo lisanduke mdima; Mulungu wa kumwambako asalilabadirenso; kuwala kusaonekenso pa tsikulo.
Bio taj dan tama, ne gledao ga Bog ozgo, i ne osvjetljavala ga svjetlost!
5 Mdima ndi mthunzi wa imfa zikhale pa tsiku limeneli; mtambo uphimbe tsikuli; mdima wandiweyani udetse kuwala kwake.
Mrak ga zaprznio i sjen smrtni, oblak ga obastirao, bio strašan kao najgori dani!
6 Usiku umenewo ukutidwe ndi mdima wandiweyani; usawerengedwenso pamodzi ndi masiku a chaka, kapena kukhala pa mwezi wina uliwonse.
Noæ onu osvojila tama, ne radovala se meðu danima godišnjim, ne brojila se u mjesece!
7 Usiku umenewo usabweretse chilichonse chabwino; kusamvekenso nthungululu za chikondwerero.
Gle, noæ ona bila pusta, pjevanja ne bilo u njoj!
8 Odziwa kutemberera masiku alitemberere tsikulo, iwo amene akonzekera kuwutsa Leviyatani.
Kleli je koji kunu dane, koji su gotovi probuditi krokodila!
9 Nyenyezi zake za mʼbandakucha zikhale mdima; tsikulo liyembekezere kucha pachabe ndipo lisaonenso kuwala koyamba kwa mʼbandakucha.
Potamnjele zvijezde u sumraèje njezino, èekala vidjelo i ne doèekala ga, i ne vidjela zori trepavica;
10 Pakuti tsiku limenelo ndiye ndinatuluka mʼmimba ya amayi anga ndipo ndi limene linandionetsa zovuta.
Što mi nije zatvorila vrata od utrobe i nije sakrila muku od mojih oèiju.
11 “Bwanji ine sindinawonongeke pamene ndinkabadwa ndi kufa pamene ndimatuluka mʼmimba?
Zašto ne umrijeh u utrobi? ne izdahnuh izlazeæi iz utrobe?
12 Chifukwa chiyani panali mawondo wondilandirirapo ndi mawere woti andiyamwitsepo?
Zašto me prihvatiše koljena? zašto sise, da sem?
13 Pakuti tsopano bwenzi ndili gone mwamtendere; ndikanakhala nditagona tulo ndili pa mpumulo
Jer bih sada ležao i poèivao; spavao bih, i bio bih miran,
14 pamodzi ndi mafumu ndi aphungu a dziko lapansi, amene anadzimangira nyumba zikuluzikulu zimene tsopano ndi mabwinja,
S carevima i savjetnicima zemaljskim, koji zidaše sebi pustoline,
15 pamodzi ndi olamulira amene anali ndi golide, amene anadzaza nyumba zawo ndi siliva.
Ili s knezovima, koji imaše zlata, i kuæe svoje puniše srebra.
16 Kapena, bwanji sindinakwiriridwe pansi monga mwana wobadwa wakufa kale, ngati khanda limene silinaone kuwala kwa dzuwa?
Ili zašto ne bih kao nedonošèe sakriveno, kao dijete koje ne ugleda vidjela?
17 Ku mandako anthu oyipa sakhalanso pa mavuto, ndipo kumeneko anthu otopa ali pa mpumulo.
Ondje bezbožnici prestaju dosaðivati, i ondje poèivaju iznemogli,
18 A mʼndende kumeneko akusangalala ndi mtendere; sakumvanso mawu ofuwula a kapitawo wa akapolo.
I sužnji se odmaraju i ne èuju glasa nastojnikova.
19 Anthu wamba ndi anthu apamwamba ali kumeneko, ndipo kapolo ndi womasuka kwa mbuye wake.
Mali i veliki ondje je, i rob slobodan od svoga gospodara.
20 “Chifukwa chiyani dzuwa limawalira iwo amene ali pa mavuto, ndipo moyo umapatsidwa kwa owawidwa mtima,
Zašto se daje vidjelo nevoljniku i život onima koji su tužna srca,
21 kwa iwo amene amalakalaka imfa imene sibwera, amene amayifunafuna imfayo kupambana chuma chobisika,
Koji èekaju smrt a nje nema, i traže je veæma nego zakopano blago,
22 amene amakondwa ndi kusangalala akamalowa mʼmanda?
Koji igraju od radosti i vesele se kad naðu grob?
23 Chifuwa chiyani moyo umaperekedwa kwa munthu amene njira yake yabisika, amene Mulungu wamuzinga ponseponse?
Èovjeku, kojemu je put sakriven i kojega je Bog zatvorio otsvuda?
24 Mʼmalo moti ndidye, ndimalira, ndi kubuwula kwanga nʼkosalekeza.
Jer prije jela mojega dolazi uzdah moj, i kao voda razljeva se jauk moj.
25 Chimene ndinkachiopa chandigwera; chimene ndinkachita nacho mantha chandichitikira.
Jer èega se bojah doðe na mene, i èega se strašah zadesi me.
26 Ndilibe mtendere kapena bata, ndilibe mpumulo, koma mavuto okhaokha.”
Ne poèivah niti imah mira niti se odmarah, i opet doðe strahota.

< Yobu 3 >