< Yesaya 9 >

1 Anthu amene anali ndi nkhawa, sadzakhalanso otaya mtima. Masiku amakedzana Mulungu ananyozetsa dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, koma kutsogolo kuno dera lonse la Galileya, limene lili dziko la anthu a mitundu ina, kuyambira ku nyanja yayikulu, mʼmbali mwa Yorodani, adzalisandutsa laulemu.
Ali neæe se onako zamraèiti pritiješnjena zemlja kao prije kad se dotaèe zemlje Zavulonove i zemlje Neftalimove, ili kao poslije kad dosaðivaše na putu k moru s one strane Jordana Galileji neznabožaèkoj.
2 Anthu oyenda mu mdima awona kuwala kwakukulu; kwa iwo okhala mʼdziko la mdima wandiweyani kuwunika kwawafikira.
Narod koji hodi u tami vidjeæe vidjelo veliko, i onima koji sjede u zemlji gdje je smrtni sjen zasvijetliæe vidjelo.
3 Inu mwauchulukitsa mtundu wanu ndipo mwawonjezera chimwemwe chawo. Iwo akukondwa pamaso panu, ngati mmene anthu amakondwera nthawi yokolola, ngatinso mmene anthu amakondwera pamene akugawana zolanda ku nkhondo.
Umnožio si narod, a nijesi mu uvelièao radosti; ali æe se radovati pred tobom kao što se raduju o žetvi, kao što se vesele kad dijele plijen.
4 Monga munachitira pogonjetsa Amidiyani, inu mwathyola goli limene limawalemera, ndodo zimene amamenyera mapewa awo, ndiponso mikwapulo ya anthu owazunza.
Jer si slomio jaram u kom vucijaše, i štap kojim ga bijahu po pleæima i palicu nasilnika njegova kao u dan Madijanski.
5 Nsapato iliyonse ya munthu wankhondo, ndiponso chovala chilichonse chodonthekera magazi zidzatenthedwa pa moto ngati nkhuni.
Jer æe obuæa svakoga ratnika koji se bije u graji i odijelo u krv uvaljano izgorjeti i biti hrana ognju.
6 Chifukwa mwana watibadwira, mwana wamwamuna wapatsidwa kwa ife, ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake. Ndipo adzamutcha dzina lake lakuti Phungu Wodabwitsa, Mulungu Wamphamvu, Atate Amuyaya, ndi Mfumu ya Mtendere.
Jer nam se rodi dijete, sin nam se dade, kojemu je vlast na ramenu, i ime æe mu biti: divni, savjetnik, Bog silni, otac vjeèni, knez mirni.
7 Ulamuliro ndi mtendere wake zidzakhala zopanda malire. Iye adzalamulira ufumu wake ali pa mpando waufumu wa Davide, ndipo adzawukhazikitsa ndi kuwuchirikiza mwa chiweruzo cholungama ndi pochita zachilungamo kuyambira nthawi imeneyo mpaka muyaya. Ndi mtima wake wonse, Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza kuchita zimenezi.
Bez kraja æe rasti vlast i mir na prijestolu Davidovu i u carstvu njegovu da se uredi i utvrdi sudom i pravdom otsada dovijeka. To æe uèiniti revnost Gospoda nad vojskama.
8 Ambuye atumiza mawu otsutsa Yakobo; ndipo mawuwo agwera pa Israeli.
Gospod posla rijeè Jakovu, i ona pade u Izrailju.
9 Anthu onse okhala mu Efereimu ndi okhala mu Samariya, adzadziwa zimenezi. Iwo amayankhula modzikuza kuti,
I znaæe sav narod, Jefrem i stanovnici Samarijski, koji oholo i ponosita srca govore:
10 “Ngakhale njerwa zagumuka, koma ife tidzamanga ndi miyala yosema. Mitanda ya mkuyu yagwetsedwa, koma ife tidzayika mitanda ya mkungudza mʼmalo mwake.”
Padoše opeke, ali æemo mi zidati od tesana kamena; dudovi su posjeèeni, ali æemo mi zamijeniti kedrima.
11 Koma Yehova wadzutsa adani kuti alimbane nawo ndipo wawafulumiza adani awo kuti amenyane nawo.
Ali æe Gospod podignuti protivnike Resinove na nj, i skupiæe neprijatelje njegove,
12 Asiriya ochokera kummawa ndi Afilisti ochokera kumadzulo ndipo ayasama pakamwa kuti adye a Israeli. Komabe, mkwiyo wake sunawachokere, mkono wake uli chitambasulire.
Sirce s istoka i Filisteje sa zapada, te æe ždrijeti Izrailja na sva usta. Kod svega toga neæe se odvratiti gnjev njegov, nego æe ruka njegova još biti podignuta.
13 Koma anthu sanabwerere kwa amene anawakantha uja, ngakhale kufunafuna Yehova Wamphamvuzonse.
Jer se narod neæe obratiti k onomu ko ga bije, i neæe tražiti Gospoda nad vojskama.
14 Choncho Yehova adzadula mutu wa Israeli pamodzi ndi mchira womwe, nthambi ya kanjedza ndi bango lomwe tsiku limodzi;
Zato æe otsjeæi Gospod Izrailju glavu i rep, granu i situ u jedan dan.
15 mutuwo ndiye akuluakulu ndi olemekezeka, mchira ndiye aneneri ophunzitsa zabodza.
Starješina i ugledan èovjek to je glava, a prorok koji uèi laž to je rep.
16 Amene amatsogolera anthuwa ndiwo amawasocheretsa, ndipo otsogoleredwa amatayika.
Jer koji vode taj narod, oni ga zavode, a koje vode, oni su propali.
17 Nʼchifukwa chake Ambuye adzakondwera nawo achinyamata, ngakhale kuwachitira chifundo ana amasiye ndi akazi amasiye, pakuti aliyense ndi wosapembedza Mulungu ndiponso ndi wochimwa ndipo aliyense amayankhula zopusa. Komabe, mkwiyo wake sunawachokere, mkono wake uli chitambasulire.
Zato se Gospod neæe radovati mladiæima njegovijem, i na sirote njegove i na udovice njegove neæe se smilovati, jer su svikoliki licemjeri i zlikovci, i svaka usta govore nevaljalstvo. Kod svega toga neæe se odvratiti gnjev njegov, nego æe ruka njegova još biti podignuta.
18 Ndithu kuyipa kwa anthuwo kumayaka ngati moto; moto wake umanyeketsa mkandankhuku ndi minga, umayatsa nkhalango yowirira, ndipo utsi wake umachita kuti toloo ngati mtambo.
Jer æe se razgorjeti bezbožnost kao oganj, koji sažeže èkalj i trnje, pa upali gustu šumu, te otide u dim visoko.
19 Dziko lidzatenthedwa ndi ukali wa Yehova Wamphamvuzonse, dziko lidzatenthedwa ndipo anthu adzakhala ngati nkhuni zosonkhera moto; palibe munthu amene adzachitire chifundo mʼbale wake.
Od gnjeva Gospoda nad vojskama zamraèiæe se zemlja i narod æe biti kao hrana ognju, niko neæe požaliti brata svojega.
20 Kudzanja lamanja adzapeza chakudya nʼkudya, koma adzakhalabe ndi njala; kudzanja lamanzere adzapeza chakudya nʼkudya, koma sadzakhuta. Aliyense azidzadya ana ake omwe.
I zgrabiæe s desne strane, pa æe opet biti gladan, i ješæe s lijeve strane, pa se opet neæe nasititi; svaki æe jesti meso od mišice svoje,
21 Manase adzadya Efereimu ndipo Efereimu adzadya Manase; onsewa pamodzi adzadya Yuda. Komabe pa zonsezi, mkwiyo wake sunawachokere, mkono wake uli chitambasulire.
Manasija Jefrema, i Jefrem Manasiju, a obojica æe se složiti na Judu. Kod svega toga neæe se odvratiti gnjev njegov, nego æe ruka njegova još biti podignuta.

< Yesaya 9 >