< Yesaya 20 >

1 Mʼchaka chimene mkulu wankhondo wotumidwa ndi mfumu ya ku Asiriya, anabwera ku Asidodi ndi kuwuthira nkhondo ndi kuwulanda,
Godine koje doðe Tartan na Azot, kad ga posla Sargon car Asirski, te bi Azot i uze ga,
2 nthawi imeneyo Yehova anawuza Yesaya mwana wa Amozi kuti, “Pita kavule chiguduli ndi nsapato zako.” Ndipo iye anaterodi, ankangoyenda wamaliseche ndiponso wopanda nsapato.
U to vrijeme reèe Gospod preko Isaije sina Amosova govoreæi: idi, skini kostrijet sa sebe, i izuj obuæu s nogu svojih. I uèini tako i iðaše go i bos.
3 Kenaka Yehova anati, “Monga momwe mtumiki wanga Yesaya wakhala akuyendera wamaliseche ndiponso wopanda nsapato kwa zaka zitatu ngati chizindikiro ndi chenjezo kwa dziko la Igupto ndi Kusi,
Tada reèe Gospod: kako ide sluga moj Isaija go i bos za znak i èudo što æe biti do tri godine Misiru i Etiopskoj,
4 momwemonso mfumu ya ku Asiriya idzatenga ukapolo anthu a ku Igupto ndi a ku Kusi, anyamata ndi okalamba. Iwo adzakhala amaliseche ndi opanda nsapato, matako ali pa mtunda. Zimenezi zidzachititsa manyazi Igupto.
Tako æe odvesti car Asirski u ropstvo Misirce, i Etiopljane u sužanjstvo, djecu i starce, gole i bose i golijeh zadnjica, na sramotu Misircima.
5 Amene ankadalira Kusi, ndiponso amene ankadzitukumula chifukwa cha Igupto adzakhumudwa ndi kuchita manyazi.
I prepašæe se i posramiæe se od Etiopske, uzdanice svoje, i od Misira, ponosa svojega.
6 Tsiku limenelo anthu amene amakhala mʼmbali mwa nyanja adzati, ‘Taonani zomwe zawachitikira amene ife tinkawadalira, amene ife tinkathawirako kuti atithandize ndi kutipulumutsa kwa mfumu ya ku Asiriya! Nanga ife tidzapulumuka bwanji?’”
I reæi æe tada koji žive na ovom ostrvu: gle, to je uzdanica naša, ka kojoj pritjecasmo za pomoæ da se saèuvamo od cara Asirskoga; kako æemo se izbaviti?

< Yesaya 20 >