< Yesaya 12 >

1 Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati: “Ndikukuyamikani, Inu Yehova; chifukwa ngakhale munandipsera mtima, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mwanditonthoza.
I reæi æeš u ono vrijeme: hvalim te, Gospode, jer si se bio razgnjevio na me, pa se odvratio gnjev tvoj, i utješio si me.
2 Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga; ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha. Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.”
Gle, Bog je spasenje moje, uzdaæu se i neæu se bojati, jer mi je sila i pjesma Gospod Bog, on mi bi spasitelj.
3 Mudzakondwera popeza Yehova ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
S radošæu æete crpsti vodu iz izvora ovoga spasenja.
4 Tsiku limenelo mudzati: “Yamikani Yehova, tamandani dzina lake; mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu, ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
I tada æete reæi: hvalite Gospoda, glasite ime njegovo, javljajte po narodima djela njegova, napominjite da je visoko ime njegovo.
5 Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu; zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
Pojte Gospodu, jer uèini velike stvari, neka se zna po svoj zemlji.
6 Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni; pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”
Klikuj i pjevaj, koja sjediš u Sionu, jer je svetac Izrailjev velik posred vas.

< Yesaya 12 >