< Hoseya 5 >

1 “Ansembe inu, imvani izi! Inu Aisraeli, tcherani khutu! Inu nyumba yaufumu, mvetserani! Chiweruzo ichi ndi chotsutsa inu: Inu munali ngati msampha ku Mizipa, munali ngati ukonde woyalidwa pa phiri la Tabori.
Èujte, sveštenici, i pazi, dome Izrailjev, i slušaj, dome carev, jer je vama sud, jer ste zamka u Mispi i mreža razapeta na Tavoru.
2 Owukira azama mʼmoyo wakupha, Ine ndidzawalanga onsewo.
Iz potaje klaše one koji zalaze; ali æu ih ja pokarati sve.
3 Ndimadziwa zonse za Efereimu; Aisraeli ndi osabisika kwa Ine. Efereimu wayamba tsopano kuchita zachiwerewere; Israeli wadziyipitsa.
Ja poznajem Jefrema i Izrailj nije sakriven od mene; jer se sada kurvaš, Jefreme, Izrailj se oskvrni.
4 “Ntchito zawo siziwalola kubwerera kwa Mulungu wawo. Mʼmitima mwawo muli mzimu wachiwerewere; Iwo sadziwa Yehova.
Ne upravljaju djela svojih da se vrate k Bogu svojemu; jer je duh kurvarski u njima i ne znaju Gospoda.
5 Kudzikuza kwa Israeli kwakhala umboni womutsutsa; Aisraeli, ngakhale Aefereimu, anagwa mʼmachimo awo; Yudanso anagwa nawo pamodzi.
I ponositost Izrailjeva svjedoèi mu u oèi; zato æe Izrailj i Jefrem pasti za bezakonje svoje, pašæe i Juda s njima.
6 Pamene adzapita ndi nkhosa zawo ndi ngʼombe zawo kukapereka nsembe kwa Yehova, iwo sadzamupeza; Iye wawachokera.
Iæi æe s ovcama svojim i s govedima svojim da traže Gospoda, ali ga neæe naæi; uklonio se je od njih.
7 Iwo ndi osakhulupirika kwa Yehova; amabereka ana amʼchigololo ndipo chikondwerero chawo cha mwezi watsopano chidzawawononga pamodzi ndi minda yawo.
Iznevjeriše Gospoda, jer izrodiše tuðe sinove; zato æe ih proždrijeti mjesec dana s dostojanjem njihovijem.
8 “Womba lipenga mu Gibeya, liza mbetete mu Rama. Fuwulani mfuwu wankhondo mu Beti-Aveni; iwe Benjamini tsogolera.
Trubite u rog u Gavaji, u trubu u Rami; vièite u Vetavenu: za tobom, Venijamine!
9 Efereimu adzasanduka bwinja pa tsiku la chilango. Ine ndikulengeza zomwe zidzachitikadi pakati pa mafuko a Israeli.
Jefrem æe opustjeti u dan kara; objavih meðu plemenima Izrailjevijem što æe zacijelo biti.
10 Atsogoleri a Yuda ali ngati anthu amene amasuntha miyala ya mʼmalire. Ndidzawakhutulira ukali wanga ngati madzi a chigumula.
Knezovi su Judini kao oni koji premještaju meðu; izliæu na njih kao vodu jarost svoju.
11 Efereimu waponderezedwa, akulangidwa chifukwa chotsatira mafano.
Jefremu se èini nasilje, satrven je sudom, jer od svoje volje otide za zapoviješæu.
12 Ine ndili ngati njenjete kwa Efereimu, ngati chinthu chowola kwa anthu a ku Yuda.
Zato æu ja biti Jefremu kao moljac i kao crv domu Judinu.
13 “Efereimu ataona nthenda yake, ndi Yuda ataona zilonda zake, pamenepo Efereimu anatembenukira kwa Asiriya, ndipo anawatumizira mfumu yayikulu kudzawathandiza. Koma mfumuyo singathe kukuchizani, singathe kuchiritsa mabala anu.
I Jefrem vidje bolest svoju i Juda svoju ranu, i otide Jefrem k Asircu, i Juda posla k caru koji bi ga branio; ali vas on ne može iscijeliti niti æe vas oprostiti rane vaše.
14 Pakuti Ine ndidzakhala ngati mkango kwa Efereimu. Ngati mkango wamphamvu kwa Yuda. Ndidzawakhadzula nʼkuchokapo; ndidzawatenga ndipo palibe amene adzawalanditse.
Jer æu ja biti kao lav Jefremu, kao laviæ domu Judinu; ja, ja æu zgrabiti, i otiæi æu, odnijeæu i niko neæe izbaviti.
15 Ndipo ndidzabwerera ku malo anga mpaka anthu anga atavomereza kulakwa kwawo. Ndipo iwo adzafunafuna nkhope yanga; mʼmasautso awo adzandifunitsitsa Ine.”
Otiæi æu i vratiæu se na svoje mjesto dokle ne priznadu svoju krivicu i potraže lice moje; kad budu u nevolji tražiæe me.

< Hoseya 5 >