< Genesis 9 >

1 Ndipo Mulungu anadalitsa Nowa ndi ana ake aamuna nati kwa iwo, “Berekanani ndipo muchulukane ndi kudzaza dziko lapansi.
I Bog blagoslovi Noja i sinove njegove, i reèe im: raðajte se i množite se, i napunite zemlju;
2 Nyama zonse za dziko lapansi, ndi mbalame zonse za mlengalenga, ndi chamoyo chilichonse chokwawa, ndiponso nsomba zonse za ku nyanja; zidzakuopani ndipo ndazipereka kuti muzilamulire.
I sve zvijeri zemaljske i sve ptice nebeske i sve što ide po zemlji i sve ribe morske neka vas se boje i straše; sve je predano u vaše ruke.
3 Tsopano chamoyo chilichonse chidzakhala chakudya chanu. Monga momwe ndinakupatsirani ndiwo zamasamba, tsopano ndikupatsaninso nyama iliyonse.
Što se god mièe i živi, neka vam bude za jelo, sve vam to dadoh kao zelenu travu.
4 “Koma musamadye nyama imene ikanali ndi magazi oyenda.
Ali ne jedite mesa s dušom njegovom, a to mu je krv.
5 Aliyense wopha munthu adzaphedwa, nyama iliyonse yopha munthu idzaphedwa, munthu aliyense wopha munthu mnzake, adzaphedwa.
Jer æu i vašu krv, duše vaše, iskati; od svake æu je zvijeri iskati; iz ruke samoga èovjeka, iz ruke svakoga brata njegova iskaæu dušu èovjeèiju.
6 “Aliyense wopha munthu, adzaphedwanso ndi munthu; pakuti Mulungu analenga munthu mʼchifanizo chake.
Ko prolije krv èovjeèiju, njegovu æe krv proliti èovjek; jer je Bog po svojemu oblièju stvorio èovjeka.
7 Inu muberekane ndi kuchulukana kuti mudzaze dziko lonse lapansi ndi kuligonjetsa.”
Raðajte se dakle i množite se; narodite se veoma na zemlji i namnožite se na njoj.
8 Mulungu anawuza Nowa ndi ana ake kuti,
I reèe Bog Noju i sinovima njegovijem s njim, govoreæi:
9 “Tsopano Ine ndapangana ndi iwe ndi zidzukulu zako zamʼtsogolomo,
A ja evo postavljam zavjet svoj s vama i s vašim sjemenom nakon vas,
10 pamodzi ndi zamoyo zonse, mbalame, ziweto ndi nyama zonse za kuthengo, ndi zonse zimene zinatuluka mʼchombo pamodzi ndi iwe.
I sa svijem životinjama, što su s vama od ptica, od stoke i od svega zvijerja zemaljskoga što je s vama, sa svaèim što je izašlo iz kovèega, i sa svijem zvijerjem zemaljskim.
11 Pangano langa ndi ili: Ine ndilonjeza kuti sindidzawononganso zamoyo ndi madzi a chigumula. Chigumula sichidzawononganso dziko lapansi.”
Postavljam zavjet svoj s vama, te otsele neæe nijedno tijelo poginuti od potopa, niti æe više biti potopa da zatre zemlju.
12 Ndipo Mulungu anati, “Ine ndikupereka chizindikiro ichi cha pangano langa la pakati pa Ine ndi iwe, ana ako, zamoyo zonse, pamodzi ndi mibado ya mʼtsogolo.
I reèe Bog: evo znak zavjeta koji postavljam izmeðu sebe i vas i svake žive tvari, koja je s vama dovijeka:
13 Ndayika utawaleza wanga mʼmitambo, ndipo chidzakhala chizindikiro cha pangano langa ndi dziko lapansi.
Metnuo sam dugu svoju u oblake, da bude znak zavjeta izmeðu mene i zemlje.
14 Nthawi zonse pakakhala mitambo mu mlengalenga ndipo utawaleza uwoneka,
Pa kad oblake navuèem na zemlju, vidjeæe se duga u oblacima,
15 ndizikumbukira pangano langa pakati pa Ine ndi inu ndi zolengedwa zonse. Madzi sadzakhalanso chigumula chowononga dziko lapansi.
I opomenuæu se zavjeta svojega koji je izmeðu mene i vas i svake duše žive u svakom tijelu, i neæe više biti od vode potopa da zatre svako tijelo.
16 Utawaleza ukamadzaoneka mʼmitambo, ndidzawuona ndi kukumbukira pangano losatha pakati pa Mulungu ndi zamoyo zonse pa dziko lapansi.”
Duga æe biti u oblacima, pa æu je pogledati, i opomenuæu se vjeènoga zavjeta izmeðu Boga i svake duše žive u svakom tijelu koje je na zemlji.
17 Choncho Mulungu anati kwa Nowa, “Ichi ndiye chizindikiro cha pangano limene ndalichita pakati pa Ine ndi zamoyo zonse pa dziko lapansi.”
I reèe Bog Noju: to je znak zavjeta koji sam uèinio izmeðu sebe i svakoga tijela na zemlji.
18 Ana aamuna a Nowa amene anatuluka mʼchombo muja anali Semu, Hamu ndi Yafeti. Hamu anali abambo ake a Kanaani.
A bijahu sinovi Nojevi koji izidoše iz kovèega: Sim i Ham i Jafet; a Ham je otac Hanancima.
19 Ana aamuna a Nowa amenewa ndiwo anali makolo a anthu onse pa dziko lapansi.
To su tri sina Nojeva, i od njih se naseli sva zemlja.
20 Nowa anali munthu woyamba kulima munda wamphesa.
A Noje poèe raditi zemlju, i posadi vinograd.
21 Tsiku lina pamene Nowa anamwako vinyo wa zipatso za mʼmundawo analedzera ndipo anavula zovala zake zonse ndi kugona mu tenti yake ali maliseche.
I napiv se vina opi se, i otkri se nasred šatora svojega.
22 Hamu, abambo ake a Kanaani ataona kuti abambo ake ali maliseche anakawuza abale ake awiri aja omwe anali panja.
A Ham, otac Hanancima, vidje golotinju oca svojega, i kaza obojici braæe svoje na polju.
23 Koma Semu ndi Yafeti anatenga chofunda nachiyika pa mapewa awo; ndipo anayenda chamʼmbuyo naphimba umaliseche wa abambo awo. Anafulatira kuti asaone umaliseche wa abambo awo.
A Sim i Jafet uzeše haljinu, i ogrnuše je obojica na ramena svoja, i iduæi natraške pokriše njom golotinju oca svojega, licem natrag okrenuvši se da ne vide golotinje oca svojega.
24 Nowa atadzuka, kuledzera kutatha, ndikudziwa zimene mwana wake wamngʼono wamwamuna uja anamuchitira,
A kad se Noje probudi od vina, dozna šta mu je uèinio mlaði sin,
25 anati, “Atembereredwe Kanaani! Adzakhala kapolo wa pansi kwenikweni kwa abale ake.”
I reèe: proklet da je Hanan, i da bude sluga slugama braæe svoje!
26 Anatinso, “Atamandike Yehova, Mulungu wa Semu! Kanaani akhale kapolo wa Semu.
I još reèe: blagosloven da je Gospod Bog Simov, i Hanan da mu bude sluga!
27 Mulungu akulitse dziko la Yafeti; Yafeti alandire madalitso pamodzi ndi Semu, ndipo Kanaani akhale kapolo wawo.”
Bog da raširi Jafeta da živi u šatorima Simovijem, a Hanan da im bude sluga!
28 Chitatha chigumula, Nowa anakhala ndi moyo zaka 350.
I poživje Noje poslije potopa trista i pedeset godina.
29 Anamwalira ali ndi zaka 950.
A svega poživje Noje devet stotina i pedeset godina; i umrije.

< Genesis 9 >