< Genesis 37 >

1 Yakobo ankakhala mʼdziko la Kanaani kumene abambo ake ankakhala.
Forsothe Jacob dwellide in the lond of Canaan, in which his fadir was a pilgrym; and these weren the generaciouns of hym.
2 Mbiri ya banja la Yakobo ndi iyi: Yosefe, mnyamata wa zaka 17 ankaweta nkhosa ndi abale ake, pamodzi ndi ana a Biliha ndi Zilipa, akazi a abambo ake. Tsono Yosefe ankabwera kudzawuza abambo ake zoyipa za abale ake.
Joseph whanne he was of sixtene yeer, yit a child, kepte a flok with hise britheren, and was with the sones of Bala and Zelfa, wyues of his fadir; and he accuside his britheren at the fadir of `the worste synne.
3 Tsono Israeli ankakonda Yosefe koposa ana ake ena onse, chifukwa anali mwana wobadwa muukalamba wake. Ndipo anamusokera mkanjo wa manja aatali.
Forsothe Israel louyde Joseph ouer alle hise sones, for he hadde gendrid hym in eelde; and he made to Joseph a cote of many colours.
4 Pamene abale ake anaona kuti abambo awo ankakonda Yosefe kuposa aliyense wa iwo, anayamba kumuda Yosefe ndipo sankayankhula naye zamtendere.
Forsothe hise britheren sien that he was loued of the fader more than alle, and thei hatiden hym, and myyten not speke ony thing pesibli to hym.
5 Tsiku lina Yosefe analota maloto ndipo pamene anawuza abale ake za malotowo, iwo anawonjeza kumuda.
And it bifelde that he telde to hise britheren a sweuene seyn, which cause was `the seed of more hatrede.
6 Iye anawawuza kuti, “Tamvani maloto amene ndinalota:
And Joseph seide to his britheren, Here ye the sweuene which Y seiy,
7 Ife timamanga mitolo ya tirigu ku munda ndipo mwadzidzidzi mtolo wanga unayimirira chilili, pamene mitolo yanu inazungulira mtolo wangawo nʼkumawugwadira.”
Y gesside that we bounden to gidere handfuls, and that as myn handful roos, and stood, and that youre handfuls stoden aboute and worschipiden myn handful.
8 Abale ake aja anamufunsa nati, “Kodi ukuyesa kuti ungakhale mfumu yathu? Ungadzatilamuliredi iweyo?” Ndipo anamuda kuposa kale chifukwa cha maloto ake ndi zimene ankakonda kunena kwa abambo awo.
Hise britheren answerden, Whether thou shalt be oure kyng, ethir we shulen be maad suget to thi lordschip? Therfor this cause of sweuenys and wordis mynystride the nurschyng of enuye, and of hatrede.
9 Tsiku lina analotanso maloto ena, ndipo anafotokozera abale ake za malotowo. Iye anati, “Tamverani, ndinalotanso maloto ena. Ulendo uno dzuwa ndi mwezi pamodzi ndi nyenyezi khumi ndi imodzi zimandigwadira.”
Also Joseph seiy another sweuene, which he telde to the britheren, and seide, Y seiy bi a sweuene that as the sunne, and moone, and enleuen sterris worschipiden me.
10 Atawuza abambo ake ndi abale ake malotowa, abambo ake anamukalipira nati, “Ndi maloto anji umalotawa? Kodi uganiza kuti ine, amayi ako pamodzi ndi abale ako onsewa tingadzabwere kudzakugwandira iwe?”
And whanne he hadde teld this sweuene to his fadir, and britheren, his fadir blamyde him, and seide, What wole this sweuene to it silf which thou hast seyn? Whether Y and thi modir, and thi britheren, schulen worschipe thee on erthe?
11 Abale ake anamuchitira nsanje, koma abambo ake anasunga nkhaniyi mu mtima.
Therfor hise britheren hadden enuye to hym. Forsothe the fadir bihelde pryuely the thing,
12 Tsono abale ake anapita kukadyetsa ziweto za abambo awo ku Sekemu,
and whanne his britheren dwelliden in Sichem, aboute flockis of the fadir `to be kept,
13 ndipo Israeli anati kwa Yosefe, “Tsono, ndikufuna kukutuma kwa abale ako.” Iye anayankha nati, “Chabwino.”
Israel seide to Joseph, Thi britheren kepen scheep in Sichymys; come thou, Y schal sende thee to hem.
14 Choncho anati kwa iye, “Pita ukaone ngati abale ako ali bwino. Ukaonenso nkhosa ngati zili bwino. Kenaka ubwere udzandiwuze.” Choncho Israeli anatuma Yosefe kuchokera ku chigwa cha Hebroni. Yosefe atafika ku Sekemu,
And whanne Joseph answerde, Y am redi, Israel seide, Go thou, and se whether alle thingis ben esi anentis thi britheren, and scheep; and telle thou to me what is doon. He was sent fro the valey of Ebron, and cam into Sichem;
15 munthu wina anamupeza akungozungulirazungulira mʼmunda ndipo anamufunsa, “Ukufunafuna chiyani?”
and a man foond hym errynge in the feeld, and `the man axide, what he souyte.
16 Iye anayankha, “Ndikufuna abale anga. Mungandiwuze kumene akudyetsa ziweto zawo?”
And he answerde, Y seke my britheren, schewe thou to me where thei kepten flockis.
17 Munthuyo anayankha nati, “Anasamukako kuno. Ndinawamva akuti, ‘Tiyeni tipite ku Dotani.’” Choncho Yosefe analondola abale ake ndipo anakawapeza ku Dotani.
And the man seide to hym, Thei yeden awei fro this place; forsothe Y herde hem seiynge, Go we into Dothaym. And Joseph yede aftir his britheren, and foond hem in Dothaym.
18 Abale ake aja anamuonera patali. Ndipo asanafike nʼkomwe kumene kunali iwo kuja, anayamba kale kumupangira chiwembu choti amuphe.
And whanne thei hadden seyn hym afer, bifor that he neiyede to hem,
19 Iwo anawuzana nati, “Uyo akubwera apo wamaloto uja.
thei thouyten to sle hym, and spaken to gidere, Lo! the dremere cometh, come ye,
20 Tsono tiyeni timuphe ndi kuponya thupi lake mu chimodzi mwa zitsime izi ndipo tidzati anadyedwa ndi nyama zakuthengo zolusa. Tsono timuonera zomwe ziti zichitike ndi maloto ake aja.”
sle we hym, and sende we into an eld sisterne, and we schulen seie, A wielde beeste ful wickid hath deuourid hym; and thanne it schal appere what hise dremes profiten to hym.
21 Koma Rubeni atamva izi, anapulumutsa Yosefe. Iye anati kwa abale ake, “Ayi, tisamuphe,
Sotheli Ruben herde this, and enforside to delyuere hym fro her hondis,
22 tisakhetse magazi. Tiyeni timuponye mʼchitsime ku chipululu konkuno. Koma tisamuvulaze nʼkomwe. Rubeni ananena zonsezi kuti apulumutse Yosefe ndi kuti pambuyo pake akamupereke kwa abambo awo.”
and seide, Sle we not the lijf of hym, nether schede we out his blood, but caste ye hym into an eeld cisterne, which is in the wildirnesse, and kepe ye youre hondis gilteles. Forsothe he seide this, willynge to delyuere hym fro her hondis, and to yelde to his fadir.
23 Choncho Yosefe atafika kwa abale ake, iwo anamuvula mkanjo wake wamanja aatali uja umene anavala
Therfor anoon as Joseph cam to hise britheren, thei dispuyliden hym of the coote, doun to the heele, and of many colours, and senten into the eeld cisterne,
24 ndipo anamutenga namuponya mʼchitsime chopanda madzi komanso mopanda chilichonse.
that hadde no water.
25 Atakhala pansi kuti adye chakudya, anatukula maso naona gulu la Aismaeli akubwera kuchokera ku Giliyadi. Ngamira zawo zinanyamula zonunkhiritsa bwino zakudya zamitundumitundu, ndipo zimenezi ankapita nazo ku Igupto.
And thei saten `to ete breed; and thei sien that Ismaelitis weigoers camen fro Galaad, and that her camels baren swete smellynge spiceries, and `rosyn, and stacten, into Egipt.
26 Yuda anafunsa abale ake nati, “Kodi tidzapindula chiyani tikapha mʼbale wathuyu ndi kuphimbitsa magazi ake?
Therfor Judas seide to hise britheren, What schal it profite to vs, if we schulen sle oure brother, and schulen hide his blood?
27 Bwanji timugulitse kwa Aismaeliwa, koma ife tisamuchite kanthu kalikonse. Ameneyu ndi mʼbale wathu thupi limodzi ndi ife.” Abale ake anavomereza zimenezi.
It is betere that he be seeld to Ismalitis, and oure hondis be not defoulid, for he is oure brother and fleisch. The britheren assentiden to these wordis;
28 Amalonda ena a ku Midiyani ankadutsa pomwepo. Tsono abale ake a Yosefe anamutulutsa Yosefe uja mu chitsime chija ndipo anamugulitsa kwa Aismaeli aja pamtengo wa masekeli makumi awiri. Choncho anapita naye Yosefe ku Igupto.
and whanne marchauntis of Madian passiden forth, thei drowen hym out of the cisterne, and seelden hym to Ismaelitis, for thriytti platis of siluer; whiche ledden hym in to Egipt.
29 Rubeni atabwerera ku chitsime kuja anapeza kuti Yosefe mulibe mʼchitsimemo. Pamenepo iye anangʼamba zovala zake
And Ruben turnede ayen to the cisterne, and foond not the child;
30 nabwerera kwa abale ake nati, “Mnyamata uja mulibemo! Nanga ndilowere kuti ine tsopano?”
and he to-rente his closis, and he yede to hise britheren, and seide, The child apperith not, and whidir schal Y go?
31 Tsono anapha kamwana ka mbuzi, natenga mkanjo wa Yosefe ndi kuwunyika mʼmagazi ake.
Forsothe thei token his coote, and dippiden in the blood of a kide, which thei hadden slayn; and senten men that baren to the fadir,
32 Iwo anatenga mkanjo uja nabwerera nawo kwa abambo awo nati, “Ife tapeza mkanjowu. Tawuyangʼanitsitsani muone ngati uli wa mwana wanu.”
and seiden, We han founde this coote, se, whether it is the coote of thi sone, ether nai.
33 Iye anawuzindikira ndipo anati, “Ndi mkanjo wa mwana wanga umenewu! Nyama yakuthengo yolusa yamudya. Mosakayika, mwana wanga Yosefe wakhadzulidwa.”
And whanne the fader hadde knowe it, he seide, It is the coote of my sone, a wielde beeste ful wickid hath ete hym, a beeste hath deuourid Joseph.
34 Pamenepo Yakobo anangʼamba zovala zake, navala chisaka mʼchiwuno mwake. Iye analira maliro a mwana wake masiku ambiri.
And he to-rente his clothis, and he was clothid with an heire, and biweilide his sone in myche tyme.
35 Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
Sothely whanne hise fre children weren gaderid to gidere, that thei schulden peese the sorewe of the fadir, he nolde take counfort, but seide, Y schal go doun in to helle, and schal biweile my sone. And the while Jacob contynude in wepyng, (Sheol h7585)
36 Amidiyani aja anagulitsa Yosefe kwa Potifara, mmodzi mwa nduna za Farao ku Igupto. Potifarayu anali mkulu wa asilikali olonda nyumba ya Farao.
Madianytis seelden Joseph into Egipt to Putifar, chast `and onest seruaunt of Farao, maistir of the chyualrie.

< Genesis 37 >