< Genesis 17 >

1 Pamene Abramu anali ndi zaka 99, Yehova anamuonekera nati, “Ine ndine Mulungu Wamphamvuzonse. Ukhale munthu wochita zolungama nthawi zonse.
A kad Avramu bi devedeset i devet godina, javi mu se Gospod i reèe mu: ja sam Bog svemoguæi, po mojoj volji živi i budi pošten.
2 Ndipo Ine ndikulonjeza kuti ndidzakupatsa zidzukulu zambiri.”
I uèiniæu zavjet izmeðu sebe i tebe, i vrlo æu te umnožiti.
3 Pomwepo Abramu anadziponya pansi ndipo Mulungu anati kwa iye,
A Avram pade nièice. I Gospod mu još govori i reèe:
4 “Pangano langa ndi iwe ndi ili: Udzakhala kholo la mitundu yambiri ya anthu.
Od mene evo zavjet moj s tobom da æeš biti otac mnogim narodima.
5 Sudzatchedwanso Abramu; dzina lako lidzakhala Abrahamu, chifukwa ndakusandutsa kukhala kholo la mitundu yambiri ya anthu.
Zato se više neæeš zvati Avram, nego æe ti ime biti Avraam, jer sam te uèinio ocem mnogih naroda;
6 Ndidzakupatsa zidzukulu zambiri motero kuti mitundu yambiri ya anthu idzatuluka mwa iwe. Mafumunso adzatuluka mwa iwe.
Daæu ti porodicu vrlo veliku, i naèiniæu od tebe narode mnoge, i carevi æe izaæi od tebe.
7 Pangano langa ndi iwe pamodzi ndi zidzukulu za mibado ya mʼtsogolo lidzakhala la muyaya. Ndidzakhala Mulungu wako ndi Mulungu wa zidzukulu zako.
A postavljam zavjet svoj izmeðu sebe i tebe i sjemena tvojega nakon tebe od koljena do koljena, da je zavjet vjeèan, da sam Bog tebi i sjemenu tvojemu nakon tebe;
8 Dziko lonse la Kanaani, limene iwe ukukhala tsopano, ndalipereka kwa iwe ndi kwa zidzukulu zako kuti likhale chuma chanu mpaka muyaya. Ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wa zidzukulu zako.”
I daæu tebi i sjemenu tvojemu nakon tebe zemlju u kojoj si došljak, svu zemlju Hanansku u državu vjeènu, i biæu im Bog.
9 Kenaka Mulungu anati kwa Abrahamu, “Koma iwe pamodzi ndi zidzukulu zako zobwera pambuyo pako mʼmibado ya mʼtsogolomo, sungani pangano langali.
I reèe Bog Avramu: ti pak drži zavjet moj, ti i sjeme tvoje nakon tebe od koljena do koljena.
10 Iwe pamodzi ndi zidzukulu zako zobwera pambuyo pako muzisunga pangano ili loti mwamuna aliyense pakati panupa azichita mdulidwe.
A ovo je zavjet moj izmeðu mene i vas i sjemena tvojega nakon tebe, koji æete držati: da se obrezuje izmeðu vas sve muškinje.
11 Kuyambira tsopano muzichita mdulidwe ndipo ichi chidzakhala chizindikiro cha pangano langa ndi iwe.
A obrezivaæete okrajak tijela svojega, da bude znak zavjeta izmeðu mene i vas.
12 Kuyambira tsopano mpaka mibado ya mʼtsogolomo mwana wamwamuna aliyense pakati panu amene wakwana masiku asanu ndi atatu ayenera kuchita mdulidwe. Awa ndi ana obadwa mʼbanja lako, kapena akapolo ochita kugula ndi ndalama, mlendo osakhala wa mʼmbumba yako.
Svako muško dijete kad mu bude osam dana da se obrezuje od koljena do koljena, rodilo se u kuæi ili bilo kupljeno za novce od kojih god stranaca, koje ne bude od sjemena tvojega.
13 Achite mdulidwe ndithu mwana wamwamuna aliyense, mbadwa ngakhale kapolo wochita kugula ndi ndalama, ndipo ichi chidzakhala chizindikiro pa thupi lanu cha pangano langa lamuyaya.
Da se obrezuje koje se rodi u kuæi tvojoj i koje se kupi za novce tvoje; tako æe biti zavjet moj na tijelu vašem zavjet vjeèan.
14 Mwamuna aliyense amene adzakhala wosachita mdulidwe adzachotsedwa pakati pa anthu ake chifukwa sanasunge pangano langa.”
A neobrezano muško, kojemu se ne obreže okrajak tijela njegova, da se istrijebi iz naroda svojega, jer pokvari zavjet moj.
15 Mulungu anatinso kwa Abrahamu, “Sarai mkazi wako, sudzamutchanso Sarai; dzina lake lidzakhala Sara.
I još reèe Bog Avramu: a Saru ženu svoju ne zovi je više Sara nego neka joj bude ime Sara.
16 Ndidzamudalitsa ndipo adzakubalira mwana wamwamuna. Ndidzamudalitsa kuti akhale mayi wa mitundu ya anthu; mafumu a anthuwo adzachokera mwa iye.”
I ja æu je blagosloviti, i daæu ti sina od nje; blagosloviæu je, i biæe mati mnogim narodima, i carevi narodima izaæi æe od nje.
17 Abrahamu anadzigwetsa pansi pamaso pa Yehova, Iye anaseka nati, “Kodi munthu wa zaka 100 nʼkubala mwana? Kodi Sara adzabereka mwana pa msinkhu wa zaka makumi asanu ndi anayi?”
Tada pade Avram nièice, i nasmija se govoreæi u srcu svojem: eda æe se èovjeku od sto godina roditi sin? i Sari? eda æe žena od devedeset godina roditi?
18 Ndipo Abrahamu anati kwa Mulungu, “Bwanji mumudalitse Ismaeli.”
I Avram reèe Bogu: neka živ bude Ismailo pred tobom!
19 Koma Mulungu anati, “Ayi, koma mkazi wako Sara adzakubalira mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha Isake. Ndidzasunga pangano langa losatha ndi iyeyu komanso ndi zidzukulu zobwera pambuyo pake.
I reèe Bog: zaista Sara žena tvoja rodiæe ti sina, i nadjeæeš mu ime Isak; i postaviæu zavjet svoj s njim da bude zavjet vjeèan sjemenu njegovu nakon njega.
20 Koma za Ismaeli, ndamva. Ndidzamudalitsadi, ndipo adzakhala ndi zidzukulu zambiri. Iye adzakhala kholo la mafumu khumi ndi awiri ndipo mwa iye mudzatuluka mtundu waukulu wa anthu.
A i za Ismaila uslišio sam te; evo blagoslovio sam ga, i daæu mu porodicu veliku, i umnožiæu ga veoma; i rodiæe dvanaest knezova, i uèiniæu od njega velik narod.
21 Koma ndidzasunga pangano langali ndi Isake amene Sara adzakubalira pofika nthawi ngati ino chaka chamawa.”
A zavjet svoj uèiniæu s Isakom kad ti ga rodi Sara, do godine u ovo doba.
22 Atatha kuyankhula, Mulungu anamuchokera Abrahamu.
I Bog izgovorivši otide od Avrama gore.
23 Tsono Abrahamu anachita mdulidwe mwana wake Ismaeli ndi onse amene anali mʼbanja lake, mbadwa ngakhale kapolo ochita kugula ndi ndalama, monga mmene Mulungu analamulira.
I Avram uze Ismaila sina svojega i sve koji se rodiše u domu njegovu i koje god bješe kupio za svoje novce, sve muškinje od domaæih svojih; i obreza okrajak tijela njihova u isti dan, kao što mu kaza Bog.
24 Abrahamu anali ndi zaka 99 pamene anachita mdulidwe,
A bješe Avramu devedeset i devet godina kad obreza okrajak tijela svojega.
25 ndipo mwana wake Ismaeli anali ndi zaka khumi ndi zitatu;
A Ismailu sinu njegovu bješe trinaest godina kad mu se obreza okrajak tijela njegova.
26 Onse, Abrahamu ndi mwana wake Ismaeli, anachita mdulidwe tsiku limodzi.
U jedan dan obreza se Avram i sin mu Ismailo,
27 Aliyense wamwamuna wa pa banja pa Abrahamu, kuphatikizapo iwo amene anabadwira pa banja pomwepo kapena akapolo ogula ndi ndalama kwa alendo, anachita mdulidwe.
I svi domašnji njegovi, roðeni u kuæi i kupljeni za novce od stranaca, biše obrezani s njim.

< Genesis 17 >