< Ezekieli 11 >

1 Pamenepo Mzimu wa Mulungu unandinyamula ndi kubwera nane ku chipata cha kummawa cha Nyumba ya Yehova. Kumeneko pa khomo la chipata panali anthu 25, ndipo ndinaona pakati pawo atsogoleri awa: Yaazaniya mwana wa Azuri ndi Pelatiya mwana wa Benaya.
Tada me podiže duh, i odnese me na istoèna vrata doma Gospodnjega koja gledaju na istok, i gle, na vratima bijaše dvadeset i pet ljudi, i meðu njima vidjeh Jazaniju sina Azurova i Felatiju sina Venajina, poglavare narodne.
2 Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, awa ndi anthu amene akukonza zoyipa ndi kupereka malangizo oyipa mu mzindamo.
I reèe mi: sine èovjeèji, ovi ljudi smišljaju bezakonje, i zlo svjetuju u tom gradu,
3 Iwo amawuza anthu kuti, ‘Nthawi sinafike yoti timange Nyumba? Mzindawu uli ngati mʼphika umene uli pa moto ndipo ife tili ngati nyama mu mʼphikamo.
Govoreæi: nije blizu; da gradimo kuæe; ovaj je grad lonac a mi meso.
4 Choncho iwe mwana wa munthu, unenere mowadzudzula. Nenera ndithu.’”
Zato prorokuj protiv njih, prorokuj, sine èovjeèji.
5 Ndipo Mzimu wa Yehova unandigwera ndipo unandiwuza kuti, “Unene kuti zimene akunena Yehova ndi izi. Iye akuti. ‘Izi ndi zimene mukunena, Inu Aisraeli, koma Ine ndikudziwa zimene zili mu mtima mwanu.’
I pade na me duh Gospodnji i reèe mi: reci: ovako veli Gospod: dome Izrailjev, tako govoriste, i znam misli srca vašega.
6 Mwapha anthu ambiri mu mzinda muno ndipo mwadzaza misewu yake ndi mitembo.
Mnoge pobiste u tom gradu, i napuniste ulice njihove pobijenijeh.
7 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mitembo imene mwayiponya mʼmisewuyo ndiyo nyama ndipo mzinda uno ndiwo mʼphika, koma Ine ndidzakuthamangitsanimo.
Zato ovako veli Gospod Gospod: koje pobiste i pobacaste usred njega, oni su meso, a on je lonac, a vas æu izvesti iz njega.
8 Inu mumaopa lupanga, koma lupangalo ndi limene ndidzakubweretsereni, akutero Ambuye.
Bojite se maèa; maè æu pustiti na vas, govori Gospod Gospod.
9 Ine ndidzakuthamangitsani mu mzinda ndipo ndidzakuperekani mʼdzanja la alendo kuti akulangeni.
I izvešæu vas iz njega, i daæu vas u ruke tuðincima, i izvršiæu na vama sudove.
10 Mudzaphedwa ndi lupanga ndipo ndidzakulangani mpaka kumalire a Israeli. Pamenepo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Od maèa æete pasti, na meði Izrailjevoj sudiæu vam, i poznaæete da sam ja Gospod.
11 Mzinda uno sudzakhala ngati mʼphika wokutetezani ndipo simudzakhalanso ngati nyama ya mʼmenemo. Ndidzakulangani mpaka kumalire a Israeli.
Ovaj grad neæe vam biti lonac niti æete vi biti u njemu meso; na meði Izrailjevoj sudiæu vam.
12 Ndipo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova. Inu simunatsatire malangizo anga kapena kusunga malamulo anga koma mwakhala mukutsata zochita za mitundu ina ya anthu imene yakuzungulirani.’”
I poznaæete da sam ja Gospod, jer po uredbama mojim ne hodiste niti zakona mojih izvršivaste, nego èiniste po zakonima tijeh naroda što su oko vas.
13 Tsono pamene ndinkanenera, Pelatiya mwana wa Benaya anafa. Pomwepo ndinadzigwetsa pansi chafufumimba ndipo ndinafuwula ndi mawu aakulu kuti “Mayo, Ambuye Yehova! Kodi mudzawatheratu Aisraeli onse otsala?”
A kad prorokovah, umrije Felatija sin Venajin; tada padoh na lice svoje i povikah iza glasa i rekoh: jaoh Gospode Gospode! hoæeš li da istrijebiš ostatak Izrailjev?
14 Yehova anayankhula nane kuti,
A glas Gospodnji doðe mi govoreæi:
15 “Anthu okhala ku Yerusalemu akuwanena abale ako, anthu a ku ukapolo, onse a banja la Israeli, kuti, ‘Anthu onse amene anatengedwa ukapolo ali kutali ndi Yehova. Dziko lanu Yehova anatipatsa kuti likhale lathulathu.’”
Sine èovjeèji, braæa su tvoja, braæa tvoja, rodbina tvoja i dom Izrailjev vaskoliki, kojima govoriše Jerusalimljani: idite daleko od Gospoda, nama je data zemlja u našljedstvo.
16 “Nʼchifukwa chake nena kwa anzako a ku ukapolo kuti, ‘Ambuye Yehova akuti: Ine ndinawatumiza kutali pakati pa anthu a mitundu ina. Ndinawabalalitsa ku mayiko ambiri. Komabe ndakhala ndikuwasunga ku mayiko kumene anapitako!’
Zato reci: ovako veli Gospod Gospod: ako ih i odagnah daleko meðu narode, ako ih i rasijah po zemljama, opet æu im biti svetinja za malo u zemljama u koje otidoše.
17 “Nʼchifukwa chake uwawuze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena kuti, Ndidzawasonkhanitsa kuchokera kwa anthu a mitundu inayo ndi kuwasonkhanitsira pamodzi kuchokera ku mayiko kumene ndinawabalalitsirako. Pambuyo pake ndidzawapatsa dziko la Israeli.
Zato reci: ovako veli Gospod Gospod: sabraæu vas iz naroda i pokupiæu vas iz zemalja u koje se rasijaste, i daæu vam zemlju Izrailjevu.
18 “Akadzalowa mʼdzikomo adzachotsa mafano awo onse oyipa ndi onyansa.
I kad doðu u nju, izbaciæe iz nje sve gadove njezine i sve gnusobe njezine.
19 Ndidzawapatsa mtima watsopano ndipo ndidzayika mzimu watsopano mwa iwo. Ndidzachotsa mtima wowuma ngati mwala mwa iwo, ndipo ndidzawapatsa mtima wofewa ngati mnofu.
I daæu im jedno srce i nov duh metnuæu u njih, i izvadiæu iz tijela njihova kameno srce i daæu im srce mesno,
20 Motero adzatsata malamulo anga ndipo adzasunga mosamala malamulo anga. Adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo.
Da bi hodili po mojim uredbama i držali moje zakone i izvršivali ih; i biæe mi narod, i ja æu im biti Bog.
21 Koma kunena za amene akupembedza mafano oyipa ndi onyansa, ndidzawalanga chifukwa cha zimene achita. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.”
A kojima srce ide po želji gnusoba njihovijeh i gadova njihovijeh, njihov æu put obratiti na njihovu glavu, govori Gospod Gospod.
22 Tsono akerubi aja anatambasula mapiko awo kuyamba kuwuluka, mikombero ili mʼmbali mwawo. Ulemerero wa Mulungu wa Israeli unali pamwamba pawo.
Potom mahnuše heruvimi krilima svojim, i toèkovi otidoše prema njima, i slava Boga Izrailjeva bješe ozgo nad njima.
23 Ulemerero wa Yehova unakwera ndi kusiya mzindawo ndipo unakayima pa phiri cha kummawa kwake kwa mzindawo.
I podiže se slava Gospodnja isred grada, i stade na gori koja je s istoka gradu.
24 Pambuyo pake Mzimu wa Mulungu unandinyamula ndi kukandifikitsa. Zimenezi zinkachitika mʼmasomphenya monga mmene Mzimu wa Mulungu unkandionetsera. Kenaka masomphenya amene ndinkawaonawo anayamba kuzimirira.
A mene duh podiže i odnese u utvari duhom Božjim u Haldejsku k roblju; i utvara koju vidjeh otide od mene.
25 Ndipo ndinafotokozera akapolowo zonse zimene Yehova anandionetsa.
I kazah roblju sve rijeèi Gospodnje što mi pokaza.

< Ezekieli 11 >