< Eksodo 37 >

1 Bezaleli anapanga Bokosi la Chipangano lamatabwa amtengo wa mkesha. Kutalika kwake kunali masentimita 114, mulifupi mwake munali masentimita 69, msinkhu wake masentimita 69.
I naèini Veseleilo kovèeg od drveta sitima, dva i po lakta dug i podrug lakta širok i podrug lakta visok.
2 Iye analikuta bokosilo ndi golide wabwino kwambiri mʼkati mwake ndi kunja komwe. Anapanganso mkombero wagolide kuzungulira bokosilo.
I pokova ga èistijem zlatom iznutra i spolja; i naèini mu zlatan vijenac unaokolo.
3 Iye anapanga mphete zinayi zagolide ndi kuzimangirira ku miyendo yake inayi ija, mbali ina ziwiri ndi mbali inanso ziwiri.
I sali mu èetiri bioèuga od zlata na èetiri ugla njegova: dva bioèuga s jedne strane a dva s druge.
4 Kenaka anapanga mizati yamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide.
I naèini poluge od drveta sitima, i okova ih zlatom.
5 Ndipo analowetsa nsichizo mʼmphete zija za mbali zonse ziwiri za bokosilo kuti azinyamulira.
I provuèe poluge kroz bioèuge s obje strane kovèegu, da se može nositi kovèeg.
6 Iye anapanga chivundikiro cha bokosilo cha golide wabwino kwambiri, kutalika kwake masentimita 114, mulifupi mwake masentimita 69.
I naèini zaklopac od èistoga zlata, u dužinu od dva i po lakta, a u širinu od podrug lakta.
7 Ndipo anapanga Akerubi awiri agolide osula ndi nyundo ndi kuwayika mbali ziwiri za chivundikirocho.
I naèini dva heruvima od zlata, jednostavne naèini ih, na dva kraja zaklopcu,
8 Iye anapanga kerubi mmodzi mbali ina ndi wina mbali inayo. Akerubiwa anawapangira limodzi ndi chivundikirocho mʼmapeto mwa mbali ziwirizo.
Jednoga heruvima na kraju odovud, a drugoga heruvima na kraju odonud; zaklopcu na oba kraja naèini heruvime.
9 Mapiko a Akerubiwo anatambasukira pamwamba pa chivundikiro cha bokosilo kuti achiphimbe. Akerubiwo anakhala choyangʼanana, aliyense kuyangʼana chivundikirocho.
I u heruvima bjehu krila raširena u vis, i zaklanjahu krilima svojim zaklopac, i licem bjehu okrenuti jedan drugom, i gledahu prema zaklopcu heruvimi.
10 Iwo anapanga tebulo la matabwa amtengo wa mkesha, mulitali mwake masentimita 91, mulifupi mwake masentimita 46, msinkhu wake masentimita 69.
I naèini sto od drveta sitima, u dužinu od dva lakta a u širinu od lakta, i od podrug lakta u visinu.
11 Kenaka analikuta ndi golide wabwino kwambiri, ndipo anapanga mkombero wagolide mʼmbali mwake.
I pokova ga èistim zlatom, i naèini mu vijenac zlatan unaokolo.
12 Iwo anapanga feremu yozungulira tebulo, mulifupi mwake ngati chikhatho cha dzanja, ndipo anayika mkombero wagolide kuzungulira feremuyo.
I naèini mu oplatu s podlanice unaokolo, i naèini vijenac zlatan uz oplatu unaokolo.
13 Iwo anapanga mphete zinayi zagolide ndipo anazilumikiza ku ngodya zake zinayi, kumene kunali miyendo yake inayi.
I sali mu èetiri bioèuga od zlata, i metnu bioèuge na èetiri ugla, koji mu bijahu na èetiri noge.
14 Mphetezo anaziyika kufupi ndi feremu kuti azikolowekamo nsichi zonyamulira tebuloyo.
Prema oplati bijahu bioèuzi, a u njima poluge, da se može nositi sto.
15 Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide kuti azinyamulira tebulolo.
A poluge naèini od drveta sitima, i okova ih zlatom, da se može nositi sto.
16 Ndipo anapanga ziwiya za pa tebulolo zagolide wabwino, mbale ndi zipande, mitsuko ndi mabeseni zogwiritsa ntchito popereka nsembe za chakumwa.
I naèini od èistoga zlata posuðe što se meæe na sto: zdjele i èaše i kutliæe i vijedra, kojim æe se preljevati.
17 Iwo anapanga choyikapo nyale chagolide wabwino kwambiri. Tsinde lake ndi mphanda zake zinasulidwa ndi nyundo. Zikho zake zokhala ndi mphukira ndi maluwa ake zinapangidwa kumodzi.
I naèini svijetnjak od èistoga zlata, jednostavan naèini svijetnjak; stup mu i grane, èašice i jabuke i cvjetovi izlažahu iz njega.
18 Mʼmbali mwake munali mphanda zisanu ndi imodzi, zitatu mbali iliyonse.
Šest grana izlažahu mu sa strana; tri grane svijetnjaka s jedne strane a tri grane svijetnjaka s druge strane;
19 Zikho zitatu zokhala ngati za maluwa amtowo, mphukira ndi duwa zinali pa mphanda yoyamba. Pa mphanda yachiwiri panalinso zikho zitatu zokhala ngati za maluwa amtowo, mphukira ndi duwa. Ndipo mphanda zonse zisanu ndi imodzi zinali chimodzimodzi ndipo zinatuluka mʼchoyikapo nyalecho.
Tri èašice kao badem na jednoj grani i jabuka i cvijet, a tri èašice kao badem na drugoj grani i jabuka i cvijet; tako na svijeh šest grana koje izlažahu iz svijetnjaka.
20 Pa choyikapo nyalecho panali zikho zinayi zokhala ngati maluwa amtowo, mphukira ndi maluwa ake.
A na samom svijetnjaku bjehu èetiri èašice kao badem sa svojim jabukama i cvjetovima,
21 Mphukira yoyamba inali mʼmunsi mwa nthambi ziwiri zoyamba za pa choyikapo nyale. Mphukira yachiwiri inali mʼmunsi mwa nthambi ziwiri zinazo. Mphukira yachitatu inali mʼmunsi mwa nthambi zina ziwirinso. Zonse pamodzi zinali nthambi zisanu ndi imodzi
Jedna jabuka bješe pod dvije grane iz njega, i jedna jabuka pod druge dvije grane iz njega, i jedna jabuka pod druge dvije grane iz njega; tako pod šest grana koje izlažahu iz njega.
22 Mphukira ndi nthambi zonse zinasulidwa kumodzi ndi choyikapo nyalecho ndi golide wabwino kwambiri.
Jabuke njihove i grane im izlažahu iz njega, sve bješe od èistoga zlata jednostavno.
23 Iwo anapanga nyale zisanu ndi ziwiri, mbaniro ndi zowolera phulusa, zonse zinali zagolide wabwino kwambiri.
I naèini mu sedam žižaka i usekaèe i spremice za gar od èistoga zlata.
24 Iwo anapanga choyikapo nyale ndi zipangizo zake zonse zagolide wabwino kwambiri wolemera makilogalamu 34.
Od talanta èistoga zlata naèini ga sa svijem spravama njegovijem.
25 Iwo anapanga guwa lamatabwa amtengo wa mkesha lofukizirapo lubani. Linali lofanana mbali zonse, mulitali masentimita 46, mulifupi masentimita 46, ndipo msinkhu masentimita 91, ndipo nyanga zake zinapangidwa kumodzi ndi guwalo.
I naèini oltar kadioni od drveta sitima u dužinu od jednoga lakta, i u širinu od jednoga lakta, èetvorouglast, i od dva lakta u visinu; iz njega izlažahu mu rogovi.
26 Iwo anakuta guwa lonse ndi golide wabwino kwambiri, pamwamba pake, mbali zonse ndi nyanga zake, ndipo anapanga mkombero wagolide kuzungulira guwalo.
I pokova ga èistijem zlatom ozgo i sa strane unaokolo, i rogove; i naèini mu vijenac od zlata unaokolo.
27 Anapanga mphete ziwiri pansi pa mkomberowo ndi kulumikiza ku mbali zonse ziwiri kuti apisemo nsichi zonyamulira.
I dva bioèuga od zlata naèini mu ispod vijenca na dva ugla njegova s obje strane, da u njima stoje poluge da se može nositi o njima.
28 Anapanga mizati yamtengo wa mkesha ndipo anayikuta ndi golide.
A poluge naèini od drveta sitima, i okova ih zlatom.
29 Iwo anapanganso mafuta opatulika odzozera ndi zofukiza za fungo lokoma kwambiri. Iyi inali ntchito ya mʼmisiri waluso lopanga zonunkhiritsa.
I naèini ulje za sveto pomazanje i èisti kad mirisni vještinom apotekarskom.

< Eksodo 37 >