< Deuteronomo 27 >

1 Mose ndi akuluakulu a Israeli analamula anthu kuti, “Sungani malamulo onse amene ndikukupatsani lero lino.
Forsothe Moyses comaundide, and the eldre men, to the puple of Israel, and seiden, Kepe ye ech `comaundement which Y comaunde to you to dai.
2 Mukawoloka mtsinje wa Yorodani kulowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, muyimiritse miyala ingapo ikuluikulu ndi kuyikulungiza.
And whanne ye han passid Jordan, in to the lond which thi Lord God schal yyue to thee, thou schalt reyse grete stoonus, and thou schalt make tho pleyn with chalk,
3 Mulembepo mawu onse a malamulo amenewa pamene muwoloka kulowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, dziko loyenda mkaka ndi uchi, monga momwe Yehova Mulungu wa makolo anu anakulonjezerani.
that thou mow write in tho alle the wordis of this lawe, whanne Jordan is passid, that thou entre in to the lond which thi Lord God schal yyue to thee, the lond flowynge with mylke and hony, as he swoor to thi fadris.
4 Ndipo mukawoloka Yorodani muyimike miyala iyi pa Phiri la Ebala monga momwe ndikukulamulirani lero lino ndipo muyikulungize.
Therfor whanne thou hast passid Jordan, reise thou the stonus whiche Y comaunde to dai to thee, in the hil of Hebal; and thou schalt make tho pleyn with chalk.
5 Pamenepo mumange guwa lansembe la miyala la Yehova Mulungu wanu. Musagwiritse ntchito chida chilichonse chachitsulo pa miyalapo.
And there thou schalt bilde an auter to thi Lord God, of stoonys whiche yrun touchide not,
6 Mumange guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu ndi miyala yakutchire ndi kuperekerapo nsembe yopsereza kwa Yehova Mulungu wanu.
and of stonys vnformed and vnpolischid; and thou schalt offre theron brent sacrifices to thi Lord God; and thou schalt offre pesible sacrifices,
7 Muperekerepo nsembe zopereka za chiyanjano, muzidye ndi kukondwera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.
and thou schalt ete there, and thou schalt make feeste bifor thi Lord God.
8 Ndipo pa miyalapo mudzalembepo mawu onse a malamulo ndi malemba akuluakulu.”
And thou schalt write pleynli and clereli on the stoonys alle the wordis of this lawe.
9 Kenaka Mose ndi ansembe, amene ndi Alevi anati kwa Aisraeli onse, “Khalani chete Aisraeli inu ndipo mumvetsere! Tsopano inu ndinu anthu a Yehova Mulungu wanu.
And Moises and the preestis of the kynde of Leuy seiden to al Israel, Israel, perseyue thou, and here; to day thou art maad the puple of thi Lord God;
10 Muzimvera Yehova Mulungu wanu ndi kutsata malamulo ake ndi malangizo ake omwe ndikukupatsani lero lino.”
thou schalt here his vois, and thou schalt do `the comaundementis, and riytfulnessis, whiche Y comaunde to thee to dai.
11 Tsiku lomwelo Mose analamula anthu kuti:
And Moises comaundide to the puple in that day,
12 Mukawoloka Yorodani, mafuko awa akayimirire pa Phiri la Gerizimu ndi kudalitsa anthu: Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Yosefe ndi Benjamini.
and seide, These men schulen stonde on the hil of Garizym to blesse the Lord, whanne Jordan `is passid; Symeon, Leuy, Judas, Isachar, Joseph, and Benjamyn.
13 Ndipo mafuko awa akayimirire pa Phiri la Ebala ndi kutchula matemberero: Rubeni, Gadi, Aseri, Zebuloni, Dani ndi Nafutali.
And euene ayens these men schulen stonde in the hil of Hebal to curse, Ruben, Gad, and Aser, Zabulon, Dan, and Neptalym.
14 Alevi adzayankhula mokweza kwa Aisraeli onse kuti:
And the dekenes schulen pronounce, and schulen seie `with hiy vois to alle the men of Israel,
15 “Ndi wotembereredwa munthu amene asema chifanizo kapena kupanga fano, ndi kuchiyika mobisa, pakuti chimenechi ndi chinthu chodetsedwa pamaso pa Yehova, ntchito za manja a anthu.”
Cursid is the man that makith a grauun ymage and yotun togidere, abhomynacioun of the Lord, the werk of `hondis of crafti men, and schal sette it in priuey place; and al the puple schal answere, and schal seie, Amen!
16 “Ndi wotembereredwa munthu amene sachitira ulemu abambo ake kapena amayi ake.”
He is cursid that onoureth not his fadir and modir; and al the puple schal seie, Amen!
17 “Ndi wotembereredwa munthu amene amasuntha mwala wa malire wa mnzake.”
Cursid is he that `berith ouer the termes of his neiybore; and al the puple schal seie, Amen!
18 “Ndi wotembereredwa munthu amene amasocheretsa munthu wosaona pa msewu.”
Cursid is he that makith a blynde man to erre in the weie; and al the puple schal seie, Amen!
19 “Ndi wotembereredwa munthu amene sachitira chilungamo mlendo, ana amasiye kapena mkazi wamasiye.”
He is cursid that peruertith the doom of a comelyng, of a fadirles, ethir modirles child, and of a widewe; and al the puple schal seie, Amen!
20 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi mkazi wa abambo ake pakuti iye sachitira ulemu pogona pa abambo ake.”
Cursid is he that slepith with `the wijf of his fadir, and schewith the hiling of his bed; and al the puple schal seie, Amen!
21 “Ndi wotembereredwa munthu amene achita chigololo ndi nyama ya mtundu uli wonse.”
Cursid is he that slepith with ony beeste; and al the puple schal seie, Amen!
22 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi mlongo wake, mwana wamkazi wa abambo ake kapena mwana wamkazi wa amayi ake.”
Cursid is he that slepith with his sistir, the douytir of his fadir, ethir of his modir; and al the puple schal seie, Amen!
23 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi apongozi ake.”
Cursid is he that slepith with his wyues modir; and al the puple schal seye, Amen!
24 “Ndi wotembereredwa munthu amene apha mnzake mwachinsinsi.”
Cursid is he that sleeth pryueli his neiybore; and al the puple schal seie, Amen!
25 “Ndi wotembereredwa munthu amene alandira chiphuphu kuti aphe munthu wosalakwa.”
Cursid is he that slepith with `the wijf of his neiybore; and al the puple schal seie, Amen!
26 “Ndi wotembereredwa aliyense amene sachita kapena sasunga mawu a malamulo awa.”
Cursid is he that takith yiftis, that he smyte the lijf of innocent blood; and al the puple schal seie, Amen! Cursid is he that dwellith not in the wordis of this lawe, nethir `parfourmeth tho in werk; and al the puple schal seie, Amen!

< Deuteronomo 27 >