< Deuteronomo 13 >

1 Ngati mneneri kapena wina aliyense amene amanena zamʼtsogolo mwa maloto atuluka pakati panu, nalengeza za chizindikiro chozizwitsa kapena chodabwitsa,
Ako ustane meðu vama prorok ili koji sne sanja, i kaže ti znak ili èudo,
2 chinthu nʼkuchitikadi, tsono iyeyo nʼkunena kuti, “Tiyeni titsatire milungu ina, tiyeni tiyipembedze,” (kunena milungu imene simunayidziwe),
Pa se zbude taj znak ili èudo koje ti kaže, i on ti reèe: hajde da idemo za drugim bogovima, kojih ne znaš, i njima da služimo,
3 musamumvere mneneriyo kapena wolotayo. Yehova Mulungu wanu afuna akuyeseni kuti aone ngati mumamukonda ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
Nemoj poslušati što ti kaže taj prorok ili sanjaè, jer vas kuša Gospod Bog vaš da bi se znalo ljubite li Gospoda Boga svojega iz svega srca svojega i sve duše svoje.
4 Muyenera kutsatira Yehova Mulungu wanu, ndipo ndi Iyeyo amene muyenera kumuopa. Muzisunga malamulo ake ndi kumamumvera, muzimutumikira ndipo kumukangamira Iyeyo.
Za Gospodom Bogom svojim idite, i njega se bojte; njegove zapovijesti èuvajte, i glas njegov slušajte, i njemu služite i njega se držite.
5 Mneneri kapena wolotayo ayenera kuphedwa, popeza analalikira zopandukira Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto ndi kukupulumutsani ku dziko la ukapolo. Wolalikirayo anafuna kukupatutsani pa njira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani kuti muyitsatire. Muzichotsa choyipa pakati panu.
A onaj prorok ili sanjaè da se pogubi, jer vas je nagovarao da se odmetnete Gospoda Boga svojega, koji vas izvede iz zemlje Misirske i iskupi vas iz kuæe ropske, i odvraæao od puta koji ti je zapovjedio Gospod Bog tvoj da ideš njim; tako istrijebi zlo iz sebe.
6 Ngati mʼbale wanu weniweni kapena mwana wanu wamwamuna kapena wamkazi, kapena mkazi wanu wokondedwa, kapena mnzanu wapamtima akukakamizani mwachinsinsi, nʼkumati, “Tiyeni tipite tikapembedze milungu ina” (milungu imene inuyo kapena makolo anu sanayidziwe,
Ako bi te podbadao brat tvoj, sin matere tvoje, ili sin tvoj ili kæi tvoja, ili žena tvoja mila, ili prijatelj tvoj koji ti je kao duša tvoja, govoreæi ti tajno: hajde da služimo drugim bogovima, kojih nijesi znao ni ti ni oci tvoji,
7 milungu ya anthu okuzungulirani, kaya ndi apafupi kapena akutali, kuchokera kumapeto mpaka kumapeto kwina kwa dziko lapansi),
Izmeðu bogova drugih naroda koji su oko vas, blizu ili daleko od tebe, od jednoga kraja zemlje do drugoga,
8 musamugonjere kapena kumumvera. Musamumvere chisoni. Musamuleke kapena kumutchinjiriza.
Ne pristaj s njim niti ga poslušaj; neka ga ne žali oko tvoje, i nemoj mu se smilovati niti ga taji,
9 Mumuphe ndithu. Dzanja lanu likhale loyambirira kumupha, kenaka manja a anthu ena onse.
Nego ga ubij: tvoja ruka nek se prva digne na nj da ga ubiješ, pa onda ruka svega naroda.
10 Mumuponye miyala mpaka kumupha, chifukwa anafuna kukupatutsani pa njira ya Yehova Mulungu amene anakutulutsani ku Igupto, dziko la ukapolo.
Zaspi ga kamenjem da pogine; jer te šæaše odvratiti od Gospoda Boga tvojega, koji te je izveo iz zemlje Misirske, iz kuæe ropske;
11 Tsono Aisraeli onse adzamva nachita mantha, ndipo palibe mmodzi pakati panu amene adzachitenso choyipa chotere.
Da sav Izrailj èuje i boji se, i da se više ne uèini tako zlo meðu vama.
12 Ngati mumvetsedwa kuti ku umodzi mwa mizinda imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mukhalemo,
Ako za kakav grad svoj, koji ti Gospod Bog tvoj da da u njemu živiš, èuješ gdje govore:
13 kwapezeka anthu ena oyipa pakati panu ndipo asocheretsa anthu ambiri mʼmizinda yanu, pomanena kuti, “Tiyeni tikapembedze milungu ina” (milungu imene simunayidziwe),
Izidoše ljudi nevaljali izmeðu tebe i otpadiše sve koji žive u gradu njihovu, govoreæi: hajde da služimo drugim bogovima, kojih ne poznajete,
14 mukuyenera kufunsa, kulondola ndi kufufuza bwino nkhaniyo. Ndipo ngati zitatsimikizikadi kuti ndi zoona kuti chinthu chonyansa chotere chachitikadi pakati panu,
Tada istraži i raspitaj, izvidi dobro, pa ako bude istina i doista se uèinila ona gadna stvar meðu vama,
15 muyenera kuwapha onse okhala mu mzinda umenewo. Muwonongeretu kwathunthu mzindawo, anthu ake ndi ziweto zake zomwe.
Pobij maèem sve koji žive u gradu onom, i zatri i njega i sve što bi u njemu bilo, i stoku maèem pobij.
16 Katundu yense wa anthu mu mzindawo mumuwunjike pamodzi pakatikati pa bwalo losonkhanako ndipo mutenthe mzindawo pamodzi ndi katundu wake yense monga nsembe yathunthu yopsereza ya kwa Yehova Mulungu wanu. Mzinda umenewo ukhale bwinja mpaka muyaya, usadzamangidwenso.
I sav plijen iz njega skupi nasred ulice njegove, spali ognjem i onaj grad i sav plijen iz njega Gospodu Bogu svojemu, da bude gomila dovijeka i da se više ne sazida.
17 Musapezeke ndi kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa kuti Yehova abweze mkwiyo wake wochititsa manthawu. Adzakuchitirani chifundo ndi kukumverani chisoni, ndipo adzakuchulukitsani monga analonjeza mwa lumbiro kwa makolo anu,
I neka ti od prokletijeh stvari ne prione ništa za ruku, eda bi se Gospod povratio od žestine gnjeva svojega, uèinio ti milost i smilovao se na te, i umnožio te, kao što se zakleo ocima tvojim,
18 chifukwa mumamvera Yehova Mulungu wanu, kusunga malamulo ake onse amene ndikukupatsani lero lino ndi kuchita zoyenera pamaso pake.
Kad slušaš glas Gospoda Boga svojega držeæi sve zapovijesti njegove, koje ti ja danas zapovijedam, da bi èinio što je pravo pred Gospodom Bogom tvojim.

< Deuteronomo 13 >