< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam, Seth, Enosh,
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Cainan, Mahalaleel, Jared,
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch, Methushelah, Lemech,
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noah; Shem, Ham, and Japheth.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
The sons of Japheth: Gomer, and Magog, and Madai, and Javan, and Tubal, and Meshech, and Tiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
— And the sons of Gomer: Ashkenaz, and Diphath, and Togarmah.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
And the sons of Javan: Elishah and Tarshish, Kittim and Rodanim.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
The sons of Ham: Cush and Mizraim, Phut and Canaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
— And the sons of Cush: Seba and Havilah, and Sabta, and Raama, and Sabtecha. And the sons of Raamah: Sheba and Dedan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
And Cush begot Nimrod: he began to be mighty on the earth.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
— And Mizraim begot the Ludim, and the Anamim, and the Lehabim, and the Naphtuhim,
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
and the Pathrusim, and the Casluhim out of whom came the Philistines, and the Caphtorim.
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
— And Canaan begot Zidon his firstborn, and Heth,
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
and the Jebusite, and the Amorite, and the Girgashite,
15 Ahivi, Aariki, Asini
and the Hivite, and the Arkite, and the Sinite,
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
and the Arvadite, and the Zemarite, and the Hamathite.
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
The sons of Shem: Elam, and Asshur, and Arphaxad, and Lud, and Aram, and Uz, and Hul, and Gether, and Meshech.
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
— And Arphaxad begot Shelah, and Shelah begot Eber.
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
And to Eber were born two sons: the name of the one was Peleg, for in his days was the earth divided; and his brother's name was Joktan.
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
And Joktan begot Almodad, and Sheleph, and Hazarmaveth, and Jerah,
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
and Hadoram, and Uzal, and Diklah,
22 Obali, Abimaeli, Seba,
and Ebal, and Abimael, and Sheba,
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
and Ophir, and Havilah, and Jobab: all these were sons of Joktan.
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Shem, Arphaxad, Shelah,
25 Eberi, Pelegi, Reu
Eber, Peleg, Reu,
26 Serugi, Nahori, Tera
Serug, Nahor, Terah,
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
Abram: the same is Abraham.
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
The sons of Abraham: Isaac and Ishmael.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
These are their generations: the firstborn of Ishmael, Nebaioth; and Kedar, and Adbeel, and Mibsam;
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
Mishma and Dumah; Massa, Hadad, and Tema;
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
Jetur, Naphish, and Kedmah: those are the sons of Ishmael.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
— And the sons of Keturah, Abraham's concubine: she bore Zimran, and Jokshan, and Medan, and Midian, and Ishbak, and Shuah. And the sons of Jokshan: Sheba and Dedan.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
And the sons of Midian: Ephah, and Epher, and Enoch, and Abida, and Eldaah. All these were sons of Keturah.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
And Abraham begot Isaac. The sons of Isaac: Esau and Israel.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
The sons of Esau: Eliphaz, Reuel, and Jeush, and Jaalam, and Korah.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
— The sons of Eliphaz: Teman and Omar, Zephi and Gatam, Kenaz, and Timna, and Amalek.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
The sons of Reuel: Nahath, Zerah, Shammah, and Mizzah.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
And the sons of Seir: Lotan, and Shobal, and Zibeon, and Anah, and Dishon, and Ezer, and Dishan.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
— And the sons of Lotan: Hori and Homam. And Lotan's sister, Timna.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
— The sons of Shobal: Alian, and Manahath, and Ebal, Shephi and Onam. — And the sons of Zibeon: Ajah and Anah.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
— The sons of Anah: Dishon. — And the sons of Dishon: Hamran, and Eshban, and Jithran, and Cheran.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
— The sons of Ezer: Bilhan, and Zaavan, [and] Jaakan. — The sons of Dishan: Uz and Aran.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
And these are the kings that reigned in the land of Edom before there reigned a king over the children of Israel: — Bela the son of Beor; and the name of his city was Dinhabah.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
And Bela died; and Jobab the son of Zerah of Bozrah reigned in his stead.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
And Jobab died; and Husham of the land of the Temanites reigned in his stead.
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
And Husham died; and Hadad the son of Bedad, who smote Midian in the fields of Moab, reigned in his stead: and the name of his city was Avith.
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
And Hadad died; and Samlah of Masrekah reigned in his stead.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
And Samlah died; and Saul of Rehoboth on the river reigned in his stead.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
And Saul died; and Baal-hanan the son of Achbor reigned in his stead.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
And Baal-hanan died; and Hadad reigned in his stead: and the name of his city was Pai; and his wife's name was Mehetabel the daughter of Matred, daughter of Mezahab.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
And Hadad died. And the chiefs of Edom were: chief Timna, chief Aliah, chief Jetheth,
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
chief Oholibamah, chief Elah, chief Pinon,
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
chief Kenaz, chief Teman, chief Mibzar,
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
chief Magdiel, chief Iram. These were the chiefs of Edom.

< 1 Mbiri 1 >