< Псалми 8 >

1 За първия певец на гетския инструмент. Давидов псалом. Иеова, Господи наш, Колко е превъзходно Твоето име по цялата земя; Ти си поставил славата Си над небесата.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
2 Из устата на младенците и сучещите Укрепил си сила поради противниците Си, За да накараш да млъкне врагът и отмъстителят.
Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
3 Като гледам Твоите небеса, делото на Твоите пръсти, Луната и звездите, които Ти си отредил,
Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
4 Казвам си: Що е човек та да го помниш? Или човешки син та да го посещаваш?
munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
5 А Ти си го направил само малко по-долен от ангелите, И със слава и чест си го увенчал.
Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
6 Поставил си го господар над делата на ръцете Си; Всичко си подчинил под нозете му,
Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
7 Всичките овци и говеда, Още и животните на полето,
nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
8 Въздушните птици, морските риби, И всичко що минава през морските пътища.
mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
9 Иеова, Господи наш, Колко е превъзходно Твоето име по цялата земя!
Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

< Псалми 8 >