< Yoube 8 >

1 Bilida: de da amane sia: i,
Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 “Dia sia: da udigili fo agoane ahoa. Amo sia: da dagobela: ?
“Kodi udzakhala ukuyankhula zoterezi mpaka liti? Mawu ako ali ngati mphepo yamkuntho.
3 Gode da moloidafa hou hamedafa giadofasa. E da eso huluane moloidafa hou fawane hamosa.
Kodi Mulungu amapotoza chiweruzo cholungama? Kodi Wamphamvuzonse amalephera kuchita zachilungamo?
4 Amabela: ? Dia mano ilia Godema wadela: le hamobeba: le, E da ilia hamobe defele se iasu dabe ilima i.
Pamene ana ako anamuchimwira Mulungu, Iye anawapereka kuti alangidwe chifukwa cha tchimo lawo.
5 Amaiba: le, di sinidigili, Gode Bagadedafa Ema edegema.
Koma utayangʼana kwa Mulungu, ndi kudandaulira Wamphamvuzonse,
6 Dia hou da moloidafa amola ledo hamedei, di da sia: sa. Amai galea, Gode da di fidima: ne misunu. Amola E da dia liligi fisi amo huluane dima bu imunu.
ngati uli wangwiro ndi wolungama mtima ngakhale tsopano Iye adzachitapo kanthu mʼmalo mwako ndipo adzakubwezeretsa pa malo ako oyenera.
7 Dia liligi bagadedafa da fisi dagoi. Be di da Godema bu sinidigisia, E da dima imunu liligi da dia musa: gagui fisi, amo bagadewane baligimu.
Chiyambi chako chidzaoneka ngati chochepa koma chimaliziro chako chidzakhala chopambana.
8 Di wahadafa, ninia aowalali ilia bagade asigi dawa: su ba: ma. Ilia da bagadewane hogolalu, asigi dawa: su noga: i lai dagoi.
“Funsa kwa anthu amvulazakale ndipo upeze zimene makolo awo anaziphunzira
9 Bai ninia esalusu da dunumuni, hedolo dagomu. Ninia da asigi dawa: su hame gala. Ninia da udigili baba agoane osobo bagadega ahoa.
pakuti ife ndife ana adzulodzuloli ndipo sitidziwa chilichonse, ndipo moyo wathu pa dziko lapansi uli ngati chithunzithunzi.
10 Be ninia siba aowalalia olelesu lamu da defea. Ilia musa: fada: i sia: su noga: le nabima!
Kodi iwo sadzakulangiza ndi kukufotokozera? Kodi sadzakuwuza mawu ochokera pa zimene amazidziwa?
11 Hano da hame galea, saga: da hame heda: sa. Saga: da heahai soge ganodini fawane ba: sa.
Kodi bango nʼkumera pa nthaka yopanda chinyontho? Nanga mawango nʼkukula bwino popanda madzi?
12 Be hano da hafoga: sea, saga: fonobahadi hame damui liligi da hedolowane biosa.
Popanda madzi, zimenezi zimafota zikanali zaziwisi ndi zosadula; zimawuma msangamsanga kuposa bango.
13 Gode Ea hou hame lalegagui dunu da amo saga: agoai gala. Ilia da Gode Ea hou hedolowane gogoleba: le, ilia dafawane hamoma: beyale dawa: su da fisi dagoi ba: sa.
Ndimo mmene amachitira anthu onse amene amayiwala Mulungu; ndi mmene chiyembekezo cha munthu wosapembedza Mulungu chimathera.
14 Ilia da ogome diasu gou momoge afae fawane dafawaneyale dawa: sa.
Kulimba mtima kwake kumafowoka; zimene iye amadalira zili ngati ukonde wa kangawude.
15 Ilia da gou momoge afae amoba: le heda: sea, dafama: bela: ? Ilia da ogome gou momoge afae galiamo agoai gagusia, noga: le leloma: bela: ? Hame mabu!
Iye amatsamira ukonde wake, koma umaduka; amawugwiritsitsa koma sulimba.
16 Eso masea, wadela: i gagalobo da osoboga hedolo heda: le, ifabi huluane wadela: sa. Wadela: le hamosu dunu da amo defele heda: sa.
Munthu woyipayo ali ngati chomera chothiriridwa bwino chimene chili pa dzuwa, nthambi zake zimatambalala pa munda wake;
17 Wadela: i gagalobo difi da igi huluane ha: giwane idinigilisili lala: bolosa.
mizu yake imayanga pa mulu wa miyala ndi kufunafuna malo woti izikike pa miyalapo.
18 Be dunu da amo gagalobo a: le fasisia, ilia da musa: amo sogebi dialu, dunu ilia da hamedafa dawa: mu.
Koma pamene yachotsedwa pamalo pakepo, pamalopo pamakana chomeracho ndi kuti, ‘Ine sindinakuonepo.’
19 Dafawane! Wadela: le hamosu dunu da fonobahadi hahawane esalu, fa: no bu hamedafa ba: mu. Eno wadela: le hamosu dunu da ilia sogebi lamu.
Ndithudi chomeracho chimafota, ndipo pa nthakapo pamatuluka zomera zina.
20 Be Gode da Ea fa: no bobogesu dunu hamedafa yolesimu. Amola E da wadela: le hamosu dunu hamedafa fidimu.
“Ndithudi, Mulungu sakana munthu amene alibe cholakwa kapena kulimbikitsa anthu ochita zoyipa.
21 E da logo doasimuba: le, di da bu oumu amola hahawane wele sia: mu.
Iye adzadzaza mʼkamwa mwako ndi phwete ndipo milomo yako idzafuwula ndi chimwemwe.
22 Be Gode da dia ha lai dunuma se dabe imunuba: le, ilia da gogosiamu. Amola wadela: le hamosu dunu ilia diasu da bu hamedafa ba: mu.”
Adani ako adzachita manyazi, ndipo malo okhalamo anthu oyipa sadzaonekanso.”

< Yoube 8 >