< Uruyan Yuhana 9 >

1 Itunna gono kadura kan taune wulsuno kulan tun me. In yene fiyini na fi deo kutyen unuzu kitene kani. I wa ni fiyini imoon pumi kibulung kuu kucomcom kun sali ligang. (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
2 A puno kuu ku comcom ku sali liganghe, libut ncin nuzu nan kuu kusali liganghe nafo ncin mongo na mi nuzu nan nya nla libut nakunti. Uwui nin niyini ta leibit bara ngutunu ncin mone nan nya kuu kone. (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
3 Nan nya ncighe ficin nuzu nan nya udu uyii, iwa ni nani timung nafo tin ninan kitene in yie.
Ndipo mʼkati mwa utsimo munatuluka dzombe kukalowa mʼdziko lapansi ndipo linapatsidwa mphamvu zoluma ngati za zinkhanira pa dziko lapansi.
4 Iwa belin nani na iwa lanza ukpi kutyene sa imomong ishifii sa kuca ba, se alenge cas na iwa di nin kulap Kutelle ni tin mine ba.
Dzombelo linalamulidwa kuti lisawononge udzu wa pa dziko lapansi, kapena chomera chilichonse, kapena mtengo uliwonse, koma anthu okhawo amene analibe chizindikiro cha Mulungu pa mphumi zawo.
5 Na iwa yinnin nani imolsu anite ba, ama iyoani udu tipui ti tauna. Ukonu mine ma yittu nafo timun finang na fi wa tii.
Silinapatsidwe mphamvu yowapha koma yowazunza kwa miyezi isanu. Ndipo ululu umene anthuwo anawumva unali ngati wa chinkhanira chikaluma munthu.
6 Nan nya nayiri ane anit ma piziru ukul, ama na ima se ba, ima yittu nin sun woru i wadi imal kuzu, ukule na cun nani.
Masiku amenewo anthu adzafunafuna imfa koma sadzayipeza. Adzalakalaka kufa koma imfa izidzawathawa.
7 Ficinghe masin nafo nibark nanga na ikyele nani udu likum. Nitin mine imonmong diku nafo titappa nizinariya a timoro mine nafo timuro nani asurne.
Dzombe linkaoneka ngati akavalo okonzekera nkhondo. Pamitu pawo panali ngati zipewa zaufumu zagolide ndipo nkhope zawo ngati za anthu.
8 Titi mine nafo tin nawani, a ayini mine nafo an ku pwi.
Tsitsi lawo linali ngati la amayi, mano awo ngati a mikango.
9 Iwa di nin nimon kessuzu nigiri nafo nnikoro, a kuculu nagilit mine nafo kuchulu nakparkatu nibark ucindu likum.
Dzombelo linavala za pachifuwa zachitsulo. Phokoso la mapiko awo linali ngati phokoso la magaleta ankhondo ambiri okokedwa ndi akavalo othamangira ku nkhondo.
10 Idi nin tidu tuzu nafo ato ninang; tiduewe dinin na gang lanzu nanit tikul udui tipuei ti taun.
Linali ndi michira ngati zinkhanira ndi mbola. Mʼmichira yake munali mphamvu yozunza nayo anthu kwa miyezi isanu.
11 Idi nin mong nafo Ugo mine nafo gono kadura unan kuu kucomcom kun sali igang. Lisa me nin ti Ibrananie idin yicighe Abaddon, a Hiliniawe yicaghe Apollyon. (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
12 Uneu ncizunghe kata. Yenjen! yenjen uimoin ipazaza iba din cinu tutung.
Tsoka loyamba lapita; matsoka ena awiri akubwerabe.
13 Gono kadura kan tocine wulsuno kulantung me, nmini wa lanza liwui nnuzu nan nya liwulu fizinariya kitene nbagade nbun Kutelle.
Mngelo wachisanu ndi chimodzi anayimba lipenga lake, ndipo ndinamva liwu lochokera ku ngodya zinayi za guwa lansembe lagolide lija lokhala pamaso pa Mulungu.
14 Liwuiye woro ngono kadura Kutelle na awa min Kulantunghe, a woro, “Suna nono kadura ninasse na i terin nan nya kurawan Afaratis.”
Liwulo linati kwa mngelo wachisanu ndi chimodzi amene anali ndi lipenga uja, “Masula angelo anayi amene anamangidwa pa mtsinje waukulu wa Yufurate.”
15 Nono kadura ni nasse na iwa malu uciu nani bara koni kube, lilone, npui une, likus lone, iwa sun nani imolu nkashi utat nanit asurne.
Ndipo anamasulidwadi angelo anayi aja amene anasungidwa kukonzekera ora ili, tsiku ili, mwezi uwu ndi chaka ichi kuti aphe limodzi la magawo atatu a anthu.
16 Ngbardang na nan likum alenge na iwa di kitene ni bark wa duru amui akalt akut aba. Nwa lanza ngbardang mine.
Ndinamva chiwerengero cha ankhondo a pa akavalo aja, kuti chinali 200 miliyoni.
17 Nanere nwa yene nibarke nan nya namoro nwui nighe nin na lenge na iwa di kitene nibarke. Imong kesuzu nigiri mine wa shigizin, mein bula nin mien tilung. Ati nibarke wa di nafo ati na zakki, nya tinu mine ula wa nucu ku, ncin a ulon nla.
Akavalo ndi okwerapo amene ndinaona mʼmasomphenya anga ankaoneka motere: Zovala za pachifukwa pawo zinali zofiira ngati moto, zobiriwira ngati utsi, ndi zachikasu ngati miyala ya sulufule. Mitu ya akavalowo inali ngati ya mikango ndipo mʼkamwa mwawo munkatuluka moto, utsi ndi sulufule.
18 Uwusu ntat na nite wa kuzu nin na naleli aluban ntate: ule, ncing a ulon nle na uwa nucu nan nya tinuu mine.
Gawo limodzi la magawo atatu a anthu linaphedwa ndi miliri yamoto, utsi ndi sulufule zimene zinkachoka mʼkamwa mwawo.
19 Bara akara nibarke wadi nan nya tinnu a tidu mine, bara tidu mine wa di nafo iyii, iwa di nin nati na iwa lanza anit ukul mung.
Mphamvu za akavalowo inali mʼkamwa mwawo ndi mʼmichira mwawo; pakuti michira yawo inali ngati njoka; ndi mitu imene inkalumira.
20 Ngissin nani asurne, alenge na iwa molu nani na alube ba, a na iwa sun usu nagbergenu usajada nin ticil nizinariya, azurfa, fikoro fi shine, litala, nin cil kuca, imon ile na iwa sa iyene kiti ba, ilanza ba, sa icina ba.
Anthu ena onse amene sanaphedwe ndi miliri imeneyi sanalapebe kuti asiye ntchito zawo zoyipa. Iwo sanasiye kupembedza ziwanda ndi mafano agolide, asiliva, amkuwa, amwala ndi amtengo, mafano amene sangathe kuona, kumva kapena kuyankhula.
21 A na iwa sun alapi nmolsu nanit ba, iwu mine, sa ipiru na wani mine sa adu likiri mine.
Sanalapenso kuleka zakupha, zamatsenga awo, zachigololo zawo kapena umbava wawo.

< Uruyan Yuhana 9 >