< 2 Timotawus 2 >

1 Fe bara nani gono ning, se likara nanyan bolu Kutelle ulenge na udi nanyan Kristi Yesu.
Tsono iwe, mwana wanga, limbika mʼchisomo chimene chili mwa Khristu Yesu.
2 Nin nimon ilenge na uwa lanza kiti ning nanya niyizi iba gbardang, na inin nanya nacara nanit acine alenge na ima yinnu udursuze wang.
Ndipo zinthu zimene unamva ine ndikuziyankhula pamaso pa mboni zambiri, uziphunzitse kwa anthu odalirika amene akaphunzitsenso ena.
3 Pira inniu nin mi nafo kusojan Kristi Yesu kucine.
Umve nane zowawa, monga msilikali wa Khristu Yesu.
4 Na kusoja duku ko nakudi katwa akuyita nanya lanzun mang yii ulele, bara anan na una ubun me nmang.
Palibe msilikali amene ali pa ntchito amagwiranso ntchito za anthu wamba, iye amafuna kukondweretsa bwana wolamulira.
5 Tutung, andi umon cum nafo anan cum sesun nduk, na asa inaghe uduke ba se adofino tiduka ncume.
Chimodzimodzinso, munthu amene ali pa mpikisano waliwiro, salandira mphotho ya wopambana pokhapokha atatsiriza monga mwa malamulo a mpikisanowo.
6 Uso gbas ame unan katwa kune na adin su kang seru uduk nimon kunene nin cizunu.
Mlimi wolimbika ndi amene amayembekezereka kukhala woyambirira kulandira gawo la zokolola.
7 Kpiliza kitene nimon ile na ndin bellu, bara Kutelle manifi uyinnun vat nimon.
Lingalira zimene ndikunenazi, pakuti Ambuye adzakuzindikiritsa zonsezi.
8 Lizinon Yesu Kristi ku, Ucizunun fimus in Dauda, urika na iwa fyghe nanyan kul. Ulele di cot nin liru ulau nighari,
Kumbukira Yesu Khristu wochokera ku mtundu wa Davide kuti anauka kwa akufa. Uwu ndiye uthenga wanga wabwino
9 Urika na ndin niu udun terii nafo unan molsu nanit. Ama na ina teru uliru Kutelle ba.
umene ndikuwuvutikira choterewu mpaka kumangidwa ndi maunyolo ngati wakuba. Koma mawu a Mulungu sanamangidwe ndi maunyolo.
10 Bara nani ndin teru nayi nanya nimon vat bara alenge na ina fere, inung wang nan se utucu ulenge na udin Kristi Yesu, nin gongon sa ligan. (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
11 Ulengee ubelle un yinnuari: “Andi ti kuu ninghe, tima kuru titi ulai ninghe.
Mawu oyenera kuwadalira ndi awa: Ngati ife tinafa naye pamodzi, tidzakhalanso moyo pamodzi naye.
12 Andi ti tere nibinayi, tima kuru tisu tigo ninghe. Andi tinarighe, ame wang manari nari.
Ngati tinapirira, tidzalamuliranso naye pamodzi. Ngati ife timukana, Iye adzatikananso.
13 Asa ti di nin diru kidegen ame wang baso sa kidegen, bara na awasa anari litime ba.”
Ngati ndife osakhulupirika, Iye adzakhalabe wokhulupirika popeza sangathe kudzikana.
14 Leu ubun lizunu nani nin nimong ilele. Wunno nani atuf nbun Kutelle na iwa su kabun kitene tigbula ba. Bara ilenge imone na imon duku icine ba. Bara ilenge imone ukul duku nalenge na idin lanzu.
Uziwakumbutsa anthu a Mulungu zinthu izi. Uwachenjeze pamaso pa Mulungu kuti asamakangane pa za mawu. Zimenezi nʼzopanda phindu ndipo zimangowononga amene akumvawo.
15 Fo kidowo udak nin litife ubun Kutelle imon seru nafo unit katwa sa ncin. Mino tigbulang kidegene gegeme.
Uyesetse kukhala wovomerezeka pamaso pa Mulungu monga wantchito wopanda chifukwa chochitira manyazi amene amalalikira mawu achoonadi molondola.
16 Suna uliru bidibidi, na udin du nin diru Kutelle.
Upewe nkhani zopanda pake, zosalemekeza Mulungu, chifukwa anthu oyankhula zotere amanka napotokerapotokera.
17 Uliru mine din malu kiti nafo ukul tijii kidowo. Nanya mine Himenes nin Piletus duku.
Chiphunzitso chawo chidzafalikira ngati chilonda. Mwa anthuwa muli Humenayo ndi Fileto.
18 Alele anitari na wuro kidegene. Idin ufitu nanan kulen mal katu. Ina kpilya uyinnu sa uyenu namong.
Iwowa apatuka pa choonadi. Iwo amaphunzitsa kuti kuuka kwa akufa kunachitika kale, motero amawononga chikhulupiriro cha anthu ena.
19 Vat nin nani, likara litino Kutelle yissin. Lidi nin nile imone: “Cikilare yiru alenge na idi anme” ni “Vat nlenge na idin yiccughe nin lissa Kutelle ama sunu katwa kanangzang gbas.”
Komabe maziko olimba, amene Mulungu anawayika ngokhazikika, ndipo mawu olembedwapo ndi awa: “Yehova amadziwa amene ndi ake,” ndiponso, “Aliyense amene amavomereza dzina la Ambuye ayenera kusiya zoyipa.”
20 Kilari nikurfu, na niti cinsu tizinariya nin azurfari duku cas ba. Kitin cisu nakatu duku nin tiwin. Nanya nalele in katwa kalau duku, a in katwa kanangzang ku.
Mʼnyumba yayikulu simukhala ziwiya zagolide ndi zasiliva zokha, koma mumakhalanso zamtengo ndi zadothi. Zina zimakhala za ntchito yapamwamba, zina za ntchito wamba.
21 Asa umong wese litime unuzu katwa kanangzang, ame kitin cisu nimon icinari. Ina kalaghe iceu ugan, ama yitu imon katwan Cikilari, inin kyeleghe bara kokame katwa kacine.
Munthu akadziyeretsa nʼkusiya ntchito za wambazi, adzakhala chiwiya cha ntchito yapamwamba, woyeretsedwa, ndi waphindu kwa Ambuye wake, wokonzeka kugwira ntchito iliyonse yabwino.
22 Cong inuzu nanya kunaniyizi nfitu. Dorton katwa kacine nin cum, uyinnu sa uyenu, usuu, a lissosin limang nin nalenge na idin yiccu Cikilare ku nanya nibinayi nilau.
Thawa zilakolako zoyipa zachinyamata. Funafuna chilungamo, chikhulupiriro, chikondi ndi mtendere pamodzi ndi amene akuyitanira pa dzina la Ambuye ndi mtima osadetsedwa.
23 Ama narin utirinu tilalan nin dirun nonku liti. Uyiru nwo asa uda nin mayardang.
Ukane matsutsano oyipa ndi opusa, chifukwa amayambitsa mikangano.
24 Na kucin Kutelle nwasu kabun ba. Ama na yitu sheuwari kitin kogha, awasa adursuzo anin yita seng.
Ndiponso mtumiki wa Ambuye asamakangane ndi anthu, koma azikhala wachifundo kwa aliyense, wodziwa kuphunzitsa, osati wokalipakalipa.
25 Amasu nin nonku liti udursuzu nalenge na inari uliru me. Nbata Kutelle nani ukpilu nanya yinnun liru kidegen.
Otsutsana naye awalangize mofatsa, mwina Mulungu adzawapatsa mwayi woti asinthike ndi kuzindikira choonadi.
26 Iwasa iyita nin kpilu tutun inin suna libardang shintan, kimal nkifu mine na awa kifo bari katwa me.
Motero nzeru zawo zidzabweramo, ndipo adzathawa msampha wa mdierekezi, amene anawagwira ukapolo kuti azichita zofuna zake.

< 2 Timotawus 2 >