< 1 Korinth 3 >

1 Ka lâibungngei le sarnungei, ratha mingei kôma ki misîr angin nin kôm thurchi misîr thei mu-unga; hi rammuol mi, khrista taksônna tieng nâitengei kôma misîr angin kêng nangni ki misîr pe.
Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu.
2 Burum niloiin, runutuiin nangni ka vâi ani hi, bu nin la nêk theiloi sikin. Male atûn khom la nêk theiloi dên nin nia,
Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe.
3 rammuol mingei om anghan nin la om tit sikin. Nin lâia innarsana le inkhat le inkhat inkhalna aom kâr chu rammuol ta nin ni tiin minlangin aoma, anni angdêna la om nin ni tina nimak mo?
Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba?
4 Nin lâia, “Kei chu Paul pâl ki ni,” a dangin “Kei chu Apollos pâl ki ni,” ti ngei nin la om kâr chu rammuol mingei angin nan la om bang nimak mo?
Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?
5 Apollos hah tumo ani? Paul khom tumo ani? Pathien tîrlâmngei, nin iem theina ranga sinthopu papai kêng kin ni. Pathien'n tho rang mi pêk chit kêng kin sin:
Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake.
6 Keiman chimu ker thea, Apollos'n tui a buoka, aniatachu chimukung a minsônpu chu Pathien ani.
Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa.
7 A minsônpu Pathien ni loiin chu chimu rethepu le tui buokpu hah ite nimak ngei.
Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu.
8 A lingpu le tui buokpu hah ite an teina om mak. An sintho lam angtakin Pathien'n râisânman pêk ngei atih.
Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake.
9 Pathien ta ranga munkhata sintho kin nia, nangni hih Pathien loimân nin ni. Pathien in nin ni sa.
Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.
10 Pathien'n manboipêk ni pêk mangin in sinpu theitak angin keiman lungphûm ku phûma, midangin in an sin ani. Aniatachu mitinin an sin rang lam angtakin indîn thei rese ngei.
Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira.
11 Pathien lungphûm a lei phûm sai Jisua Khrista pêna chu tutên lungphûm dang phûm thei noni ngei.
Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu.
12 Ma lungphûm chunga han senkhatin rângkachakin mini, sumdârin mini, lung mantam mini mangin sin an ta; senkhatin thingin mini, sûlbuon mini, sapôl mini mangin sin an tih.
Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu,
13 Khrista Nikhuo han meiin ânlâr rang sikin mei ngêt han mitin sintho hah phuol a ta; anina tak inlang atih.
ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense.
14 Lungphûm chunga sin hah akâng nônchu a sinpu'n râisânman man atih.
Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake.
15 Aniatachu tutu sintho khom akângin chu dok atih; hannirese, ama ha chu mei rakân angdôrin sanminjôkin om atih.
Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.
16 Pathien in nin ni le Pathien Ratha nin kôma aom ngâi ti nin riet minthâr khet mo?
Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu?
17 Masikin tutu khom Pathien biekin hah a sietin chu Pathien'n ama hah siet atih. Pathien biekin chu ânthieng kêng, male nangni ngei hah a biekin nin ni.
Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.
18 Tutên athenin inhuong no rese. Nin lâia tutu khom hi rammuol balama avârin ân bên chu a vâr tatak theina rangin amo chang bak rese. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
19 Hi rammuolin vârna ati hih Pathien mitmûn chu achâng ani sikin, Pathien lekhabu'n, “Pathien'n mivârngei chu kin vâr an intina han a min ôk ngei ngâi,” ati anghan;
Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,”
20 male Pathien lekhabu dangin, “Pumapa'n chu mivârngei mindonna hah mangmunboi ani ti a riet,” ati sa anghan.
ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.”
21 Masika han tutên miriemngei song no rese ngei. Adikin chu neinun nâm nin ta ani:
Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu,
22 Paul khom, Apollos khom, Peter khom; hi rammuol khom, ringna le thina khom, neinun omsai le ala hong om rang ngei khom anrêngin nin ta riempet an ni,
kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu,
23 male nangni khom Khrista ta nin nia, Khrista khom Pathien ta ani.
ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.

< 1 Korinth 3 >