< Men Korint I 3 >

1 ARI ri ai kan i jota kak padaki on komail dueta on aramaj wenin, a on me uduken o kijin jeri en Krijtuj akan.
Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu.
2 I kamana kin komail pil en didi, a kaidin kijin mana, pwe komail jaikenta kak on, o komail pil jota kak on anjau wet.
Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe.
3 Pwe komail non uduken pwe iaduen, ma peirin o akamai, mi re omail, komail jo uduken o weweid ni tiak en aramaj akan?
Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba?
4 Pwe amen kin inda: Nai nain Pauluj amen, a amen: Nai nain Apoloj amen. Komail jo kin mi nin tiak en aramaj?
Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?
5 Pwe ij Apoloj? O ij Pauluj, kaidin papa kai, me komail aja janer lamalam duen Kaun o kotin pan on amen amen?
Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake.
6 Nai me padukedier, a Apoloj me kalamu ir adar, a Kot me kotin kaparadar. wiaw.
Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa.
7 Ari kaidin i meakot, me padukedi, pil kaidin i, me kalamu ir adar, a Kot eta, me kotikidar wa kan.
Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu.
8 Ari, me kin padukedi o me kin kalamu ir adar, ira dupeneta, o amen pan katinki iran ara dodok.
Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake.
9 Pwe kit me jauaj pan dodok en Kot, a komail japajap en Kot, o japwilim en Kot a kakau im.
Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.
10 Nai me wiadar pajon ki mak en Kot me i aleer duen jauje lolekon amen, a amen ujewei kakau poa, a amen amen en kalaka duen a kakau pon pajon wet!
Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira.
11 Pwe jota me pan kak wia eu pajon, me pan toror jan me wiauier, i eta: Iejuj Krijtuj.
Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu.
12 Ari, ma amen pan kauada pon pajon wet kold, jilper, takai, kajampwal, tuka, ra, pain kit akan,
Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu,
13 Nan wiawia en amen amen pan janjaleda, pwe ran o pan kapareda due, pwe a pan kadiarok kida kijiniai. Pwe kijiniai pan kaialeda wiawia en amen amen.
ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense.
14 Ma wiawia en amen, me a kauadar poa, pan mimieta, a pan katin.
Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake.
15 A ma wiawia en amen pan ronala, a jota pan katin. A pein i pan dorela duen amen, me pitila jan nan kijiniai.
Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.
16 Komail jota aja, me komail tanpaj en Kot, o Nen en Kot kotikot lol omail?
Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu?
17 A ma amen kawela tanpaj en Kot, nan Kot pan kawela i, pwe tanpaj en Kot me jaraui, ari iei komail.
Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.
18 Jota amen en kotaue pein i! Ma amen nan pun omail lamelame anjau wet, me a lolekon, mak eta, en wiala ol pweipwei men, pwen wiala lolekon amen. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
19 Pwe lolekon en jappa et me jon en pweipwei ren Kot, pwe a intinidier: A kin kaloe kidi me aklolekon pein ar widiwidin.
Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,”
20 Pil eu! Kaun o kotin mani, lamalam en me aklolekon kan, me mal.
ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.”
21 Ari, jota amen en akkeleki aramaj akan, pwe omail meakaroj;
Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu,
22 Ma Pauluj, de Apoloj, de Kepaj, de jappa, de memaur, de mela, de ma men met, de men mur, pwe karoj me omail.
kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu,
23 A komail japwilim en Krijtuj, a Krijtuj japwilim en Kot.
ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.

< Men Korint I 3 >