< نحمیا 7 >

و چون حصار بنا شد و درهایش را برپانمودم و دربانان و مغنیان و لاویان ترتیب داده شدند، ۱ 1
Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
آنگاه برادر خود حنانی و حننیارئیس قصر را، زیرا که او مردی امین و بیشتر ازاکثر مردمان خداترس بود، بر اورشلیم فرمان دادم. ۲ 2
Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
و ایشان را گفتم دروازه های اورشلیم را تاآفتاب گرم نشود باز نکنند و مادامی که حاضرباشند، درها را ببندند و قفل کنند و از ساکنان اورشلیم پاسبانان قرار دهید که هر کس به پاسبانی خود و هر کدام به مقابل خانه خویش حاضرباشند. ۳ 3
Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
و شهر وسیع و عظیم بود و قوم در اندرونش کم و هنوز خانه‌ها بنا نشده بود. ۴ 4
Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
و خدای من دردلم نهاد که بزرگان و سروران و قوم را جمع نمایم تا برحسب نسب نامه‌ها ثبت کردند و نسب نامه آنانی را که مرتبه اول برآمده بودند یافتم و در آن بدین مضمون نوشته دیدم: ۵ 5
Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
اینانند اهل ولایتها که از اسیری آن اشخاصی که نبوکدنصر پادشاه بابل به اسیری برده بود، برآمده بودند و هر کدام از ایشان به اورشلیم و یهودا به شهر خود برگشته بودند. ۶ 6
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
اما آنانی که همراه زربابل آمده بودند: یسوع و نحمیا و عزریا و رعمیا و نحمانی و مردخای و بلشان و مسفارت و بغوای و نحوم و بعنه. و شماره مردان قوم اسرائیل: ۷ 7
Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
بنی فرعوش، دوهزار و یک صد وهفتاد و دو. ۸ 8
Zidzukulu za Parosi 2,172
بنی شفطیا، سیصد و هفتاد و دو. ۹ 9
Zidzukulu za Sefatiya 372
بنی آرح، ششصد و پنجاه و دو. ۱۰ 10
Zidzukulu za Ara 652
بنی فحت موآب از بنی یشوع و یوآب، دو هزار و هشتصد وهجده. ۱۱ 11
Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
بنی عیلام، هزار و دویست و پنجاه وچهار. ۱۲ 12
Zidzukulu za Elamu 1,254
بنی زتو، هشتصد و چهل و پنج. ۱۳ 13
Zidzukulu za Zatu 845
بنی زکای، هفتصد و شصت. ۱۴ 14
Zidzukulu za Zakai 760
بنی بنوی، ششصد و چهل و هشت. ۱۵ 15
Zidzukulu za Binuyi 648
بنی بابای، ششصد وبیست و هشت. ۱۶ 16
Zidzukulu za Bebai 628
بنی عزجد، دو هزار و سیصد وبیست و دو. ۱۷ 17
Zidzukulu za Azigadi 2,322
بنی ادونیقام، ششصد و شصت وهفت. ۱۸ 18
Zidzukulu za Adonikamu 667
بنی بغوای، دو هزار و شصت و هفت. ۱۹ 19
Zidzukulu za Abigivai 2,067
بنی عادین، ششصد و پنجاه و پنج. ۲۰ 20
Zidzukulu za Adini 655
بنی آطیراز (خاندان ) حزقیا، نود و هشت. ۲۱ 21
Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
بنی حاشوم، سیصد و بیست و هشت. ۲۲ 22
Zidzukulu za Hasumu 328
بنی بیصای، سیصد وبیست و چهار. ۲۳ 23
Zidzukulu za Bezayi 324
بنی حاریف، صد و دوازده. ۲۴ 24
Zidzukulu za Harifu 112
بنی جبعون، نود و پنج. ۲۵ 25
Zidzukulu za Gibiyoni 95.
مردمان بیت لحم ونطوفه، صد و هشتاد و هشت. ۲۶ 26
Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
مردمان عناتوت، صد و بیست و هشت. ۲۷ 27
Anthu a ku Anatoti 128
مردمان بیت عزموت، چهل و دو. ۲۸ 28
Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
مردمان قریه یعاریم و کفیره و بئیروت، هفتصد و چهل و سه. ۲۹ 29
Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
مردمان رامه و جبع، ششصد و بیست و یک. ۳۰ 30
Anthu a ku Rama ndi Geba 621
مردمان مکماس، صد و بیست و دو. ۳۱ 31
Anthu a ku Mikimasi 122
مردمان بیت ایل و عای، صد و بیست و سه. ۳۲ 32
Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
مردمان نبوی دیگر، پنجاه و دو. ۳۳ 33
Anthu a ku Nebo winayo 52
بنی عیلام دیگر، هزارو دویست و پنجاه و چهار. ۳۴ 34
Ana a Elamu wina 1,254
بنی حاریم، سیصدو بیست. ۳۵ 35
Zidzukulu za Harimu 320
بنی اریحا، سیصد و چهل و پنج. ۳۶ 36
Zidzukulu za Yeriko 345
بنی لود و حادید و اونو، هفتصد و بیست و یک. ۳۷ 37
Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
بنی سنائه، سه هزار و نه صد و سی. ۳۸ 38
Zidzukulu za Senaya 3,930.
و اماکاهنان: بنی یدعیا از خاندان یشوع، نه صد و هفتادو سه. ۳۹ 39
Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
بنی امیر، هزار و پنجاه و دو. ۴۰ 40
Zidzukulu za Imeri 1,052
بنی فشحور، هزار و دویست و چهل و هفت. ۴۱ 41
Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
بنی حاریم، هزار و هفده. ۴۲ 42
Zidzukulu za Harimu 1,017.
و اما لاویان: بنی یشوع از (خاندان ) قدمیئیل و از بنی هودویا، هفتاد و چهار. ۴۳ 43
Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
و مغنیان: بنی آساف، صد وچهل و هشت. ۴۴ 44
Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
و دربانان: بنی شلوم و بنی آطیرو بنی طلمون و بنی عقوب و بنی حطیطه وبنی سوبای، صد و سی و هشت. ۴۵ 45
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
و اما نتینیم: بنی صیحه، بنی حسوفا، بنی طبایوت. ۴۶ 46
Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
بنی فیروس، بنی سیعا، بنی فادون. ۴۷ 47
Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
بنی لبانه، بنی حجابه، بنی سلمای. ۴۸ 48
Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
بنی حانان، بنی جدیل، بنی جاحر. ۴۹ 49
Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
بنی رآیا، بنی رصین، بنی نقودا. ۵۰ 50
Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
بنی جزام، بنی عزا، بنی فاسیح. ۵۱ 51
Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
بنی بیسای، بنی معونیم، بنی نفیشسیم. ۵۲ 52
Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
بنی بقبوق، بنی حقوفا، بنی حرحور. ۵۳ 53
Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
بنی بصلیت، بنی محیده، بنی حرشا. ۵۴ 54
Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
بنی برقوس، بنی سیسرا، بنی تامح. ۵۵ 55
Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
بنی نصیح، بنی حطیفا. ۵۶ 56
Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
و پسران خادمان سلیمان: بنی سوطای، بنی سوفرت، بنی فریدا. ۵۷ 57
Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
بنی یعلا، بنی درقون، بنی جدیل. ۵۸ 58
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
بنی شفطیا، بنی حطیل، بنی فوخره حظبائیم، بنی آمون. ۵۹ 59
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
جمیع نتینیم و پسران خادمان سلیمان، سیصدو نود و دو. ۶۰ 60
Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
و اینانند آنانی که از تل ملح و تل حرشاکروب و ادون و امیر برآمده بودند، اماخاندان پدران و عشیره خود را نشان نتوانستندداد که آیا از اسرائیلیان بودند یا نه. ۶۱ 61
Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
بنی دلایا، بنی طوبیا، بنی نقوده، ششصد و چهل و دو. ۶۲ 62
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
و ازکاهنان: بنی حبایا، بنی هقوص، بنی برزلای که یکی از دختران برزلایی جلعادی را به زنی گرفته بود، پس به نام ایشان مسمی شدند. ۶۳ 63
Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
اینان انساب خود را در میان آنانی که در نسب نامه هاثبت شده بودند طلبیدند، اما نیافتند، پس ازکهانت اخراج شدند. ۶۴ 64
Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
پس ترشاتا به ایشان امر فرمود که تا کاهنی با اوریم و تمیم برقرار نشود، از قدس اقداس نخورند. ۶۵ 65
Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
تمامی جماعت با هم چهل و دو هزارو سیصد و شصت نفر بودند. ۶۶ 66
Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
سوای غلامان وکنیزان ایشان که هفت هزار و سیصد و سی و هفت نفر بودند و مغنیان و مغنیات ایشان دویست وچهل و پنج نفر بودند. ۶۷ 67
Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
و اسبان ایشان، هفتصدو سی و شش و قاطران ایشان، دویست و چهل وپنج. ۶۸ 68
Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
و شتران، چهار صد و سی و پنج وحماران، ششهزار و هفتصد و بیست بود. ۶۹ 69
Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
و بعضی از روسای آبا هدایا به جهت کاردادند. اما ترشاتا هزار درم طلا و پنجاه قاب وپانصد و سی دست لباس کهانت به خزانه داد. ۷۰ 70
Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
وبعضی از روسای آبا، بیست هزار درم طلا و دوهزار و دویست منای نقره به خزینه به جهت کاردادند. ۷۱ 71
Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
و آنچه سایر قوم دادند این بود: بیست هزار درم طلا و دو هزار منای نقره و شصت وهفت دست لباس کهانت. ۷۲ 72
Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
پس کاهنان و لاویان و دربانان و مغنیان و بعضی از قوم و نتینیم و جمیع اسرائیل، در شهرهای خود ساکن شدند و چون ماه هفتم رسید، بنی‌اسرائیل در شهرهای خودمقیم بودند. ۷۳ 73
Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.

< نحمیا 7 >