< 1 Korintusi 3 >

1 Én sem szólhattam nektek, atyámfiai, mint lelkieknek, hanem mint testieknek, mint a Krisztusban kiskorúaknak.
Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu.
2 Tejjel tápláltalak titeket és nem kemény eledellel, mert ezt nem bírtátok volna el, sőt még most sem bírnátok el,
Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe.
3 mert még testiek vagytok. Amikor irigykedés, viszálykodás, és egyenetlenkedés van közöttetek, vajon nem testiek vagytok-e és nem emberi módon viselkedtek-e?
Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba?
4 Mert amikor az egyik ezt mondja: „Én Pálé vagyok“, a másik meg: „Én Apollósé“nem emberi módon viselkedtek-e?
Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?
5 Hát kicsoda Pál? És kicsoda Apollós? Csak szolgák, akik által hívőkké lettetek, mégpedig úgy, amint kinek-kinek az Úr megadta.
Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake.
6 Én ültettem, Apollós öntözött, de az Isten adta a növekedést.
Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa.
7 Azért nem az számít, aki ültet, sem az, aki öntöz, hanem a növekedést adó Isten.
Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu.
8 Az ültető és az öntöző egyformák, és mindegyik a maga jutalmát kapja meg munkája szerint.
Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake.
9 Mert Isten munkatársai vagyunk, ti pedig Isten szántóföldje és épülete vagytok.
Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.
10 Az Istennek nekem adott kegyelme szerint, mint bölcs építőmester fundamentumot vetettem, de más épít rá. Vigyázzon azonban mindenki, hogy mit épít rá.
Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira.
11 Mert más fundamentumot senki sem vethet azonkívül, amely vettetett, amely a Jézus Krisztus.
Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu.
12 Ha pedig valaki aranyat, ezüstöt, drágakövet, fát, szénát, szalmát épít erre a fundamentumra,
Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu,
13 kinek-kinek a munkája nyilvánvaló lesz, mert az (Úr) napja majd nyilvánvalóvá teszi, mert tűzzel jön el, és azt tűz fogja megvizsgálni.
ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense.
14 Ha valakinek megmarad munkája, amelyet ráépített, jutalmát veszi.
Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake.
15 De ha valakinek munkája megég, kárt vall. Ő azonban megmenekül, de csak úgy, mint aki tűzön ment át.
Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.
16 Nem tudjátok, hogy ti az Isten temploma vagytok, és az Isten Lelke lakik bennetek?
Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu?
17 Ha valaki az Isten templomát beszennyezi, elveszti azt az Isten, mert Isten temploma szent, és az a templom ti vagytok.
Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.
18 Senki se csalja meg magát. Ha valaki azt hiszi, hogy bölcs ti köztetek e világon, bolond legyen, hogy bölccsé lehessen. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
19 Mert e világ bölcsessége bolondság Isten előtt. Mert meg van írva: „Megfogja a bölcseket csalárdságukban“.
Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,”
20 És ismét: „Tudja az Úr, hogy a bölcsek gondolatai hiábavalók“.
ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.”
21 Azért senki se dicsekedjék emberekkel, mert minden a tiétek:
Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu,
22 akár Pál, akár Apollós, akár Kéfás, akár a világ, akár az élet, akár a halál, akár a jelenvalók, akár a következendők, minden a tiétek.
kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu,
23 Ti pedig a Krisztusé, Krisztus pedig Istené.
ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.

< 1 Korintusi 3 >