< Psalm 83 >

1 Ein Gesang, ein Lied, von Asaph. Gott, sei nicht still! Schweig nicht! Bleib nicht so ruhig, Gott!
Nyimbo. Salimo la Asafu. Inu Mulungu musakhale chete; musangoti phee, Mulungu musangoti duu.
2 Denn siehe, Deine Feinde sind geschäftig; das Haupt erheben Deine Hasser.
Onani adani anu akuchita chiwawa, amene amadana nanu autsa mitu yawo.
3 Sie halten, Deinem Volk zuwider, listig Rat, beraten gegen Deine Schutzbefohlenen.
Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu; Iwo akukonzekera kutsutsana ndi omwe mumawakonda.
4 Sie sprechen: "Auf, wir wollen sie als Volk vernichten. Nie werde mehr des Namen Israels gedacht!"
Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu kuti dzina la Israeli lisakumbukikenso.”
5 Einmütig halten Rat und schließen gegen Dich ein Bündnis
Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu; Iwo achita mgwirizano kutsutsana nanu:
6 Edoms und Ismaels Gezelte, Moabs und die der Agarener,
Matenti a Edomu ndi Aismaeli, Mowabu ndi Ahagiri,
7 Gebal, Ammon und Amalek, Philisterland und Tyrier.
Agebala, Aamoni ndi Aamaleki, Afilisti, pamodzi ndi anthu a ku Turo.
8 Auch Assur schließt sich ihnen an; sie leihen ihren Arm den Söhnen Lots. (Sela)
Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo kupereka mphamvu kwa ana a Loti. (Sela)
9 Behandle sie wie Midian, wie Sisara, wie Jabin an dem Kisonsbach!
Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani, monga munachitira Sisera ndi Yabini ku mtsinje wa Kisoni.
10 Zu Endor wurden sie vertilgt; sie wurden Dünger für das Ackerfeld.
Amene anawonongedwa ku Endori ndi kukhala ngati zinyalala.
11 Tu ihren Edlen wie Oreb und Zeeb, wie Zeba und Salmunna, allen ihren Fürsten!
Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu ana a mafumu muwachite zomwe munachita Zeba ndi Zalimuna,
12 Sie sprechen: "Lasset Gottes Auen uns erobern!"
amene anati, “Tiyeni tilande dziko la msipu la Mulungu.”
13 Mein Gott! Mach sie dem Wirbellaube gleich, den Stoppeln vor dem Winde!
Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo.
14 Wie Feuer, das den Wald verzehrt, wie Flammen, Berge sengend,
Monga moto umatentha nkhalango, kapena malawi a moto kuyatsa phiri,
15 jag ihnen nach mit Deinem Wetter! Und schreckt sie mit Deinem Sturme!
kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho, ndi kuwachititsa mantha ndi namondwe.
16 Füll an ihr Angesicht mit Schmach, auf daß sie Deinen Namen fürchten, Herr!
Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi kuti adzafunefune dzina lanu Yehova.
17 Sie sollen schämen sich, für immerdar verwirrt, mit Schanden untergehen!
Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.
18 Dann merken sie, daß Du mit Deinem Namen heißest
Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova, ndinu nokha Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi.

< Psalm 83 >