< 1 Chronik 1 >

1 Adam, Set, Enos.
Adamu, Seti, Enosi
2 Kenan, Mahalalel, Jered.
Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
3 Chanok, Metuselach, Lemek.
Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
4 Noë, Sem, Cham, Japhet.
Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
5 Japhets Söhne sind Gomer, Magog, Madai, Javan, Tubal, Mosek und Tiras.
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
6 Gomers Söhne sind Askenaz, Riphat und Togarma.
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
7 Javans Söhne sind Elisa, Tarsis, Kittim und Rodanim.
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
8 Chams Söhne sind Kusch und Misraim, Put und Kanaan.
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
9 Des Kusch Söhne sind Seba, Chavila, Sabta, Regma und Sabteka, Regmas Söhne sind Seba und Dedan.
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
10 Und Kusch zeugte Nimrod. Dieser fing an, auf Erden ein Held zu werden.
Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
11 Und Misraim zeugte die Luditer, die Anamiter, die Lehabiter, die Naphtuchiter,
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
12 die Patrusiter und die Kasluchiter sowie die Kaphtoriter, von denen die Philister auszogen.
Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
13 Und Kanaan zeugte Sidon als seinen Erstgeborenen und Chet,
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
14 sodann die Jebusiter, Amoriter, Girgasiter,
Ayebusi, Aamori, Agirigasi
15 Chiviter, Arkiter, Siniter,
Ahivi, Aariki, Asini
16 Arvaditer, Semariter und Chamatiter
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
17 Sems Söhne sind Elam, Assur, Arphaksad, Lud, Aram, Us, Chul, Geter und Mesek.
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
18 Und Arphaksad zeugte den Selach und Selach den Eber.
Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
19 Zwei Söhne wurden Eber geboren. Des einen Name war Peleg. Denn in seinen Tagen ward die Erde zerteilt. Sein Bruder hieß Joktan.
Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
20 Und Joktan zeugte Almodad, Seleph, Chazarmavet, Jerach,
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
21 Hadoram, Uzal, Dikla,
Hadoramu, Uzali, Dikila
22 Ebal, Abimael, Seba,
Obali, Abimaeli, Seba,
23 Ophir, Chavila und Jobab. All diese sind Joktans Söhne.
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
24 Sem, Arphaksad, Selach,
Semu, Aripakisadi, Sela
25 Eber, Peleg, Rëu,
Eberi, Pelegi, Reu
26 Serug, Nachor, Terach,
Serugi, Nahori, Tera
27 Abram, das ist Abraham.
ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
28 Abrahams Söhne waren Isaak und Ismael.
Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
29 Dies sind ihre Geschlechtsfolgen: Ismaëls Erstgeborener ist Nebajot. Dann folgen Kedar, Adbeel, Mibsam,
Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
30 Misma, Duma, Massa, Chadad, Tema,
Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
31 Jetur, Naphis und Kedma. Dies sind die Söhne Ismaëls.
Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
32 Keturas, des Nebenweibes Abrahams, Söhne sind Zimran, Joksan, Medan, Midian, Isbak und Suach; diese hat sie geboren. Joksans Söhne sind Seba und Dedan.
Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
33 Midians Söhne sind Epha, Epher und Chanok, Abida und Eldaa. Alle diese sind Söhne der Ketura.
Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
34 Und Abraham zeugte den Isaak. Isaaks Söhne sind Esau und Israel.
Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
35 Esaus Söhne sind Eliphaz, Rëuel, Jeus, Jalam und Korach.
Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
36 Des Eliphaz Söhne sind Teman, Omar, Sephi, Gatam, Kenaz, Timna und Amalek.
Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
37 Rëuels Söhne sind Nachat, Zerach, Samma und Mizza.
Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
38 Und Seïrs Söhne sind Lotan, Sobal, Sibon, Ana, Dison, Eser und Disan.
Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
39 Lotans Söhne sind Chori und Homam. Timna ist Lotans Schwester.
Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
40 Sobals Söhne sind Aljan, Manachat, Ebal, Sephi und Onam. Sibons Söhne sind Ajja und Ana.
Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
41 Anas Söhne sind: Dison. Und Disons Söhne sind Chamram, Esban, Itran und Keran.
Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
42 Esers Söhne sind Bilhan, Zaavan und Jakan. Disans Söhne sind Us und Aran.
Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
43 Dies sind die Könige, die im Lande Edom herrschten, bevor ein König der Israeliten war:
Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
44 Bela, Beors Sohn, und seine Stadt hieß Dinhaba. Als Bela starb, ward des Serach Sohn, Jobab, aus Bosra an seiner Statt König.
Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
45 Als Jobab starb, ward Chusam aus dem Lande der Temaniter an seiner Statt König.
Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
46 Als Chusam starb, ward an seiner Statt König Bedads Sohn, Hadad, der Midian auf Moabs Gefilde schlug. Seine Stadt hieß Avit.
Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
47 Als Hadad starb, ward Samla aus Masreha an seiner Statt König.
Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
48 Als Samla starb, ward Saul aus Rechobot am Strom an seiner Statt König.
Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
49 Als Saul starb, ward Akbors Sohn, Baalchanan, an seiner Statt König.
Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
50 Als Baalchanan starb, ward Hadad an seiner Statt König. Seine Stadt hieß Pai, und sein Weib, Matreds Tochter und Mezahabs Enkelin, hieß Mehetabel.
Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
51 Als Hadad starb, gab es nur noch Häuptlinge in Edom: die Häuptlinge Timna, Alja, Jetet,
Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
52 Oholibama, Ela, Pinon,
Oholibama, Ela, Pinoni,
53 Kenaz, Teman, Mibsar,
Kenazi, Temani, Mibezari,
54 Magdiel und Iram. Dies sind Edoms Häuptlinge.
Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

< 1 Chronik 1 >