< Psalms 125 >

1 A song of ascents. Those who trust in the Lord are like Mount Zion, that cannot be moved, but abides forever.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2 Round Jerusalem are the mountains, and the Lord is round his people from now and for evermore.
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3 For he will not suffer the sceptre of wrong to rest on the land allotted to the righteous; else the righteous might put forth their own hand to evil.
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
4 Do good, O Lord, to the good, and to the true-hearted.
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
5 But those who swerve into crooked ways will the Lord lead away with the workers of evil. Peace be upon Israel.
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.

< Psalms 125 >