< 1 Chronicles 1 >

1 Adam, Seth, Enosh,
Adamu, Seti, Enosi
2 Kenan, Mahalalel, Jared,
Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
3 Hanokh, Methuselah, Lamech,
Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
4 Noah. The sons of Noah: Shem, Ham, and Japheth.
Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
5 The sons of Japheth: Gomer, and Magog, and Madai, and Javan, and Tubal, and Meshech, and Tiras.
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
6 The sons of Gomer: Ashkenaz, and Riphath, and Togarmah.
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
7 The sons of Javan: Elishah, and Tarshish, Kittim, and Rodanim.
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
8 The sons of Ham: Cush, and Mizraim, Put, and Canaan.
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
9 The sons of Cush: Seba, and Havilah, and Sabtah, and Raamah, and Sabteca. The sons of Raamah: Sheba, and Dedan.
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
10 Cush became the father of Nimrod; he began to be a mighty hunter on the earth.
Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
11 Mizraim became the father of Ludim, and Anamim, and Lehabim, and Naphtuhim,
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
12 and Pathrusim, and Casluhim (from whom came the Philistines), and Caphtorim.
Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
13 Canaan became the father of Sidon his firstborn, and Heth,
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
14 and the Jebusites, and the Amorites, and the Girgashites,
Ayebusi, Aamori, Agirigasi
15 and the Hivites, and the Arkites, and the Sinites,
Ahivi, Aariki, Asini
16 and the Arvadites, and the Zemarites, and the Hamathites.
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
17 The sons of Shem: Elam, and Asshur, and Arpachshad, and Lud, and Aram. And the sons of Aram: Uz, and Hul, and Gether, and Mash.
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
18 Arpachshad became the father of Kenan, and Kenan became the father of Shelah, and Shelah became the father of Eber.
Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
19 To Eber were born two sons: the name of the one was Peleg; for in his days the earth was divided; and his brother's name was Joktan.
Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
20 Joktan became the father of Almodad, and Sheleph, and Hazarmaveth, and Jerah,
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
21 and Hadoram, and Uzal, and Diklah,
Hadoramu, Uzali, Dikila
22 and Obal, and Abimael, and Sheba,
Obali, Abimaeli, Seba,
23 and Ophir, and Havilah, and Jobab. All these were the sons of Joktan.
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
24 Shem, Arpachshad, Kenan, Shelah,
Semu, Aripakisadi, Sela
25 Eber, Peleg, Reu,
Eberi, Pelegi, Reu
26 Serug, Nahor, Terah,
Serugi, Nahori, Tera
27 Abram (that is, Abraham).
ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
28 The sons of Abraham: Isaac, and Ishmael.
Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
29 These are their generations: the firstborn of Ishmael, Nebaioth; then Kedar, and Adbeel, and Mibsam,
Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
30 Mishma, and Dumah, Massa, Hadad, and Tema,
Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
31 Jetur, Naphish, and Kedemah. These are the sons of Ishmael.
Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
32 The sons of Keturah, Abraham's secondary wife: she bore Zimran, and Jokshan, and Medan, and Midian, and Ishbak, and Shuah. The sons of Jokshan: Sheba, and Dedan.
Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
33 The sons of Midian: Ephah, and Epher, and Hanoch, and Abida, and Eldaah. All these were the sons of Keturah.
Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
34 Abraham became the father of Isaac. The sons of Isaac: Esau, and Israel.
Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
35 The sons of Esau: Eliphaz, Reuel, and Jeush, and Jalam, and Korah.
Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
36 The sons of Eliphaz: Teman, and Omar, Zepho, and Gatam, Kenaz; and by Timna: Amalek.
Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
37 The sons of Reuel: Nahath, Zerah, Shammah, and Mizzah.
Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
38 The sons of Seir: Lotan, and Shobal, and Zibeon, and Anah, and Dishon, and Ezer, and Dishan.
Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
39 The sons of Lotan: Hori, and Hemam; and Timna was Lotan's sister.
Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
40 The sons of Shobal: Alvan, and Manahath, and Ebal, Shepho, and Onam. The sons of Zibeon: Aiah, and Anah.
Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
41 The sons of Anah: Dishon. The sons of Dishon: Hemdan, and Eshban, and Ithran, and Keran.
Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
42 The sons of Ezer: Bilhan, and Zaavan, and Akan. The sons of Dishan: Uz, and Aran.
Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
43 Now these are the kings who reigned in the land of Edom, before there reigned any king over the children of Israel: Bela the son of Beor; and the name of his city was Dinhabah.
Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
44 Bela died, and Jobab the son of Zerah of Bozrah reigned in his place.
Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
45 Jobab died, and Husham of the land of the Temanites reigned in his place.
Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
46 Husham died, and Hadad the son of Bedad, who struck Midian in the field of Moab, reigned in his place; and the name of his city was Avith.
Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
47 Hadad died, and Samlah of Masrekah reigned in his place.
Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
48 Samlah died, and Shaul of Rehoboth-ha-Nahar reigned in his place.
Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
49 Shaul died, and Baal Hanan the son of Achbor reigned in his place.
Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
50 Baal Hanan died, and Hadad son of Bedad reigned in his place; and the name of his city was Pau; and his wife's name was Mehetabel, the daughter of Matred, the daughter of Me-Zahab.
Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
51 Hadad died. The chiefs of Edom were: chief Timna, chief Alvah, chief Jetheth,
Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
52 chief Oholibamah, chief Elah, chief Pinon,
Oholibama, Ela, Pinoni,
53 chief Kenaz, chief Teman, chief Mibzar,
Kenazi, Temani, Mibezari,
54 chief Magdiel, chief Iram. These are the chiefs of Edom.
Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

< 1 Chronicles 1 >