< 1 Kronická 2 >

1 Tito jsou synové Izraelovi: Ruben, Simeon, Léví, Juda, Izachar a Zabulon,
Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,
2 Dan, Jozef, Beniamin, Neftalím, Gád a Asser.
Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
3 Synové Judovi: Her, Onan a Séla. Ti tři narodili se jemu z dcery Suovy Kananejské. Ale Her, prvorozený Judův, byl zlý před očima Hospodinovýma, protož zabil ho.
Ana a Yuda anali awa: Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha.
4 Támar pak nevěsta jeho porodila mu Fáresa a Záru. Všech synů Judových pět.
Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
5 Synové Fáresovi: Ezron a Hamul.
Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.
6 Synové pak Záre: Zamri, Etan, Héman, Kalkol a Dára, všech těch pět.
Ana a Zera anali awa: Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
7 A synové Zamri: Charmi, vnuk Achar, kterýž zkormoutil Izraele, zhřešiv při věci proklaté.
Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
8 Synové pak Etanovi: Azariáš.
Mwana wa Etani anali Azariya.
9 Synové pak Ezronovi, kteříž se mu zrodili: Jerachmeel, Ram a Chelubai.
Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
10 Ram pak zplodil Aminadaba, a Aminadab zplodil Názona, kníže synů Juda.
Ramu anabereka Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda.
11 Názon pak zplodil Salmona, a Salmon zplodil Bóza.
Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,
12 A Bóz zplodil Obéda, a Obéd zplodil Izai.
Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
13 Izai pak zplodil prvorozeného svého Eliaba, a Abinadaba druhého, a Sammu třetího,
Yese anabereka Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea,
14 Natanaele čtvrtého, Raddaia pátého,
wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,
15 Ozema šestého, Davida sedmého,
wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.
16 A sestry jejich: Sarvii a Abigail. Synové pak Sarvie byli: Abizai, Joáb, Azael, tři.
Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.
17 Abigail pak porodila Amazu, otec pak Amazův byl Jeter Izmaelitský.
Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
18 Kálef pak syn Ezronův zplodil s Azubou manželkou a s Jeriotou syny. Jehož tito synové byli: Jeser, Sobab a Ardon.
Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.
19 Když pak umřela Azuba, pojal sobě Kálef Efratu, kteráž mu porodila Hura.
Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.
20 A Hur zplodil Uri, a Uri zplodil Bezeleele.
Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
21 Potom všel Ezron k dceři Machira otce Galádova, kterouž on pojal, když byl v šedesáti letech. I porodila jemu Seguba.
Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.
22 Segub pak zplodil Jaira, kterýž měl třimecítma měst v zemi Galád.
Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.
23 Nebo vzal Gessurejským a Assyrským vsi Jairovy, i Kanat s městečky jeho, šedesáte měst. To všecko pobrali synové Machirovi, otce Galádova.
(Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
24 Též i po smrti Ezronově, když již pojal byl Kálef Efratu, manželka Ezronova Abia porodila jemu také Ashura, otce Tekoa.
Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
25 Byli pak synové Jerachmeele prvorozeného Ezronova: Prvorozený Ram, po něm Buna a Oren, a Ozem s Achia.
Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali: Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya.
26 Měl také manželku druhou Jerachmeel, jménem Atara. Ta jest matka Onamova.
Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
27 Byli pak synové Ramovi prvorozeného Jerachmeele: Maaz a Jamin a Eker.
Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa: Maazi, Yamini ndi Ekeri.
28 Též synové Onamovi byli: Sammai a Jáda. A synové Sammai: Nádab a Abisur.
Ana a Onamu anali awa: Shamai ndi Yada. Ana a Shamai anali awa: Nadabu ndi Abisuri.
29 Jméno pak manželky Abisurovy Abichail; kteráž porodila jemu Achbana a Molida.
Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
30 A synové Nádabovi: Seled a Appaim. Ale umřel Seled bez dětí.
Ana a Nadabu anali awa: Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
31 Synové pak Appaimovi: Jesi; a synové Jesi: Sesan; a dcera Sesanova: Achlai.
Ana a Apaimu anali awa: Isi, amene anabereka Sesani. Sesani anabereka Ahilai.
32 Synové pak Jády, bratra Sammaiova: Jeter a Jonatan. Ale umřel Jeter bez dětí.
Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa: Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
33 Synové pak Jonatanovi: Felet a Záza. Ti byli synové Jerachmeelovi.
Ana a Yonatani anali awa: Peleti ndi Zaza. Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
34 Neměl pak Sesan synů, ale dceru. A měl Sesan služebníka Egyptského jménem Jarchu.
Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.
35 Protož dal Sesan dceru svou Jarchovi služebníku svému za manželku, kteráž porodila mu Attaie.
Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
36 Attai pak zplodil Nátana, a Nátan zplodil Zabada.
Atayi anali abambo ake a Natani, Natani anali abambo ake a Zabadi,
37 Zabad pak zplodil Eflale, a Eflal zplodil Obéda.
Zabadi anali abambo a Efilali, Efilali anali abambo a Obedi,
38 Obéd pak zplodil Jéhu, a Jéhu zplodil Azariáše.
Obedi anali abambo a Yehu, Yehu anali abambo a Azariya,
39 Azariáš pak zplodil Cheleza, a Chelez zplodil Elasu.
Azariya anali abambo a Helezi, Helezi anali abambo a Eleasa,
40 Elasa pak zplodil Sismaie, a Sismai zplodil Salluma.
Eleasa anali abambo ake a Sisimai, Sisimai anali abambo a Salumu,
41 Sallum pak zplodil Jekamiáše, a Jekamiáš zplodil Elisama.
Salumu anali abambo a Yekamiya, Yekamiya anali abambo a Elisama.
42 Synové pak Kálefa, bratra Jerachmeelova: Mésa prvorozený jeho. On byl otec Zifejských i synů Marese, otce Hebronova.
Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa: Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
43 Synové pak Hebronovi: Chóre a Tapuach, a Rekem a Sema.
Ana a Hebroni anali awa: Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema.
44 Sema pak zplodil Rachama otce Jorkeamova, a Rekem zplodil Sammaie.
Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.
45 Syn pak Sammai byl Maon; kterýžto Maon byl otec Betsurských.
Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
46 Efa také, ženina Kálefova, porodila Chárana a Mozu a Gazeza. A Cháran zplodil Gazeza.
Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
47 Synové pak Johedai: Regem, Jotam, Gesan, Felet, Efa a Saaf.
Ana a Yahidai anali awa: Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
48 S ženinou Maachou Kálef zplodil Sebera a Tirchana.
Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.
49 Porodila pak Saafa otce Madmanejských, Sévu otce Makbenejských a otce Gibejských. Též dcera Kálefova Axa.
Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.
50 Ti byli synové Kálefovi, syna Hur prvorozeného Efraty: Sobal otec Kariatjeharimských,
Izi zinali zidzukulu za Kalebe. Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa: Sobala abambo a Kiriati Yearimu,
51 Salma otec Betlémských, Charef otec čeledi Betgaderských.
Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
52 Měl pak syny Sobal otec Kariatjeharimských: Haroe otce obyvatelů dílu Menuchotských.
Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,
53 A čeledi Kariatjeharimských, Jeterských, Putských, Sumatských a Misraiských. Z těch pošli Zaratští a Estaolští.
ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
54 Synové Salmy: Betlémští, Netofatští, Atarotští z čeledi Joábovy, a Zarští, kteříž užívali dílu Menuchotských,
Zidzukulu za Salima zinali izi: Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori,
55 A čeledi písařů obývajících v Jábezu, Tiratských, Simatských, Suchatských. Ti jsou Cinejští příchozí z Amata, otce čeledi Rechabovy.
ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.

< 1 Kronická 2 >