Aionian Verses

Genesis 37:35
(parallel missing)
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
Genesis 42:38
(parallel missing)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)
Genesis 44:29
(parallel missing)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol h7585)
Genesis 44:31
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol h7585)
Numbers 16:30 (Numeri 16:30)
(parallel missing)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
Numbers 16:33 (Numeri 16:33)
(parallel missing)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
Deuteronomy 32:22 (Deuteronomo 32:22)
(parallel missing)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
1 Samuel 2:6 (1 Samueli 2:6)
(parallel missing)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol h7585)
2 Samuel 22:6 (2 Samueli 22:6)
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
1 Kings 2:6 (1 Mafumu 2:6)
(parallel missing)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
1 Kings 2:9 (1 Mafumu 2:9)
(parallel missing)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol h7585)
Job 7:9 (Yobu 7:9)
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
Job 11:8 (Yobu 11:8)
(parallel missing)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
Job 14:13 (Yobu 14:13)
(parallel missing)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol h7585)
Job 17:13 (Yobu 17:13)
(parallel missing)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
Job 17:16 (Yobu 17:16)
(parallel missing)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Job 21:13 (Yobu 21:13)
(parallel missing)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
Job 24:19 (Yobu 24:19)
(parallel missing)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol h7585)
Job 26:6 (Yobu 26:6)
(parallel missing)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
Psalms 6:5 (Masalimo 6:5)
(parallel missing)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
Psalms 9:17 (Masalimo 9:17)
(parallel missing)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
Psalms 16:10 (Masalimo 16:10)
(parallel missing)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Psalms 18:5 (Masalimo 18:5)
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
Psalms 30:3 (Masalimo 30:3)
(parallel missing)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
Psalms 31:17 (Masalimo 31:17)
(parallel missing)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
Psalms 49:14 (Masalimo 49:14)
(parallel missing)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
Psalms 49:15 (Masalimo 49:15)
(parallel missing)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
Psalms 55:15 (Masalimo 55:15)
(parallel missing)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
Psalms 86:13 (Masalimo 86:13)
(parallel missing)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
Psalms 88:3 (Masalimo 88:3)
(parallel missing)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
Psalms 89:48 (Masalimo 89:48)
(parallel missing)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol h7585)
Psalms 116:3 (Masalimo 116:3)
(parallel missing)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
Psalms 139:8 (Masalimo 139:8)
(parallel missing)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol h7585)
Psalms 141:7 (Masalimo 141:7)
(parallel missing)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
Proverbs 1:12 (Miyambo 1:12)
(parallel missing)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
Proverbs 5:5 (Miyambo 5:5)
(parallel missing)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol h7585)
Proverbs 7:27 (Miyambo 7:27)
(parallel missing)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
Proverbs 9:18 (Miyambo 9:18)
(parallel missing)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
Proverbs 15:11 (Miyambo 15:11)
(parallel missing)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
Proverbs 15:24 (Miyambo 15:24)
(parallel missing)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
Proverbs 23:14 (Miyambo 23:14)
(parallel missing)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
Proverbs 27:20 (Miyambo 27:20)
(parallel missing)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
Proverbs 30:16 (Miyambo 30:16)
(parallel missing)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
Ecclesiastes 9:10 (Mlaliki 9:10)
(parallel missing)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol h7585)
Song of Solomon 8:6 (Nyimbo ya Solomoni 8:6)
(parallel missing)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
Isaiah 5:14 (Yesaya 5:14)
(parallel missing)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol h7585)
Isaiah 7:11 (Yesaya 7:11)
(parallel missing)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol h7585)
Isaiah 14:9 (Yesaya 14:9)
(parallel missing)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
Isaiah 14:11 (Yesaya 14:11)
(parallel missing)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
Isaiah 14:15 (Yesaya 14:15)
(parallel missing)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
Isaiah 28:15 (Yesaya 28:15)
(parallel missing)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
Isaiah 28:18 (Yesaya 28:18)
(parallel missing)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Isaiah 38:10 (Yesaya 38:10)
(parallel missing)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol h7585)
Isaiah 38:18 (Yesaya 38:18)
(parallel missing)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol h7585)
Isaiah 57:9 (Yesaya 57:9)
(parallel missing)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
Ezekiel 31:15 (Ezekieli 31:15)
(parallel missing)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol h7585)
Ezekiel 31:16 (Ezekieli 31:16)
(parallel missing)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol h7585)
Ezekiel 31:17 (Ezekieli 31:17)
(parallel missing)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol h7585)
Ezekiel 32:21 (Ezekieli 32:21)
(parallel missing)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol h7585)
Ezekiel 32:27 (Ezekieli 32:27)
(parallel missing)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol h7585)
Hosea 13:14 (Hoseya 13:14)
(parallel missing)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
Amos 9:2 (Amosi 9:2)
(parallel missing)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol h7585)
Jonah 2:2 (Yona 2:2)
(parallel missing)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
Habakkuk 2:5 (Habakuku 2:5)
(parallel missing)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol h7585)
Ahihang keima in hibang in kong ci hi, a kuamapo matlap nei ngawl in a suapui te tung ah a thin-uk peuma, thukhenna thuak tu hi: taciang a kuamapo in, a suapui a zawngsak sia zong thukhen upa te kung puak tu kilawm hi: a kuamapo in, a suapuipa mi ngoai a ci peuma, hell sung a theng tu kilawm hi. (Geenna g1067)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
Na ziatsang mit in hong khialsak a hile, khelkeak in vawk in: na pumpi vekpi taw hell sung ah na ki khiak tu sang in pumpi khen khat na sup tu phazaw hi. (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
Na ziatsang khut in hong khialsak le, tan in vawk in: na pumpi vekpi taw hell sung ah na ki khiak tu sang in pumpi khen khat na sup tu phazaw hi. (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
Taciang, pumpi that in, tha a that thei ngawl te lau heak vun: ahihang tha le taksa pumpi hell sung ah a lalcip khawmsak thei sia lau zaw vun. (Geenna g1067)
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna g1067)
Nang Capernaum awng! van dong in lapsang hi napi, hell sung dong khiaksuk na hi tu hi: banghangziam cile na sung ah a ki vawt nalamdang te Sodom ah ki vawt hile, tuni dong taang lai tu hi. (Hadēs g86)
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
Akua mapo in mihing Tapa sia kammal taw a do peuma, ki maisak tu hi: ahihang khatpo in Tha Thiangtho sia kammal taw a do peuma sia, tu hun le hongpai pheang tu hun sung ah zong ki maisak ngawl tu hi. (aiōn g165)
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
Lingphung sung a tak thaici te sia, thu za napi; hileitung thinngimna, leitung hauna i theamna in tua thu zapcip a, nga zo ngawl hi. (aiōn g165)
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn g165)
Mimphei cii a poai ngalpa sia doaimangpa hi; anlak hun sia leitung bo hun hi a; anla te sia vantungmi te a hihi. (aiōn g165)
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn g165)
Tua ahikom mimphei te sia khawm in, mei taw hal siat hi; tasiabangma in hileitung a bo ciang in piang tu hi. (aiōn g165)
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn g165)
Hi leitung bo ciang in tabangma hi tu hi: vantungmi te hongpai in, mipha te sung pan in mi pha ngawl te khen tu a, (aiōn g165)
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn g165)
Keima in kong son hi, nang sia Peter ni hi, hi suangpi tung ah ka pawlpi ka phut tu hi; taciang hell ngam kongpi te in a zo zo batu hi. (Hadēs g86)
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs g86)
Tua ahikom na khut a hibale na peang in hong khialsak le, tan in: khut lang ni, a hibale peang ni nei in tawntung mei sung ah khiak thuak tu sang in, pumpi cing ngawl in nuntakna sung ah tum tu phazaw hi. (aiōnios g166)
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios g166)
Taciang na mit in hong khialsak le, khel in a, vawk in: mit ni taw hell sung ah khiak suk thuak sang in, mit langkhat taw nuntakna sung ah tum tu phazaw hi. (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna g1067)
Khat hongpai in, sya pha awng, tawntung nuntakna ka nei natu in bang ngamtatpha seam tu khi ziam? ci in dong hi. (aiōnios g166)
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Khatpo in keima hang in a inn le a lo, a nu le a pa, a suapui, a zi le a ta a nusia a hile, a se zakhat in sang kik tu a, tawntung nuntakna ngamh in lua tu uh hi. (aiōnios g166)
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios g166)
Lamhui ah theikung khat a mu ciang, a tung ah a te simngawl bangma a mu ngawl hu in, Bangmahun in nga nawn heak in, ci hi. Tasia pociang tua theikung ko hi. (aiōn g165)
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
Thukhamhil te le Pharisee te, a kihitheamsak te, na mailam uh bing hi! banghangziam cile mi khat biakna lai tu in tuipi le leitung kimveal in na vak uh a, a ki kheal zawkciang note sang in a se ni tamzaw Hell ngam i ta na suaksak uh hi. (Geenna g1067)
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna g1067)
No ngul suan te, hell ngam thet natu pan bangbang suakta thei tu nu ziam? (Geenna g1067)
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna g1067)
Jesus Olive mualtung ah to a, a nungzui te kuama heak ngawl in a kung ah hongpai uh hi, hi thu te sia banghun ciang hong piang tu ziam, nangma paikik tu le leitung bo tu thu musakna sia bangbang ziam? ci hong son tan, ci uh hi. (aiōn g165)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
Tasiaciang in a veisang a to te tung ah, Topa in, no hamsiat thuak te ka kung pan in kiheam tavun, doaimangpa le a nungzui te a tu a ki vawtkhol tawntung mei sung ah pai vun: (aiōnios g166)
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
Hite sia tawntung ngim na sung ah pai tu a: mi thutang te a hile tawntung nuntakna sung ah pai tu uh hi, ci hi. (aiōnios g166)
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
Keima i kong thupiak teng theampo a vekpi zui tu in hil tavun: taciang en vun, leitung bo dong in a tawntung keima in kong ompui hi, ci hi. Amen. (aiōn g165)
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn g165)
Ahihang Tha Thiangtho a sonsiate sia, bangmahun in ki maisak ngei ngawl tu hi, banghangziam cile tawntung thukhenna dan thuak tu kilawm hi: ci hi. (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Hi leitung thinngimna, hauna i theamna, nadang tampi te lungngul nate tum in Pathian thu sia deapcip ahikom, a nga toai ngawl hi. (aiōn g165)
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
Na khut in hong khialsak le, at tan in: bangmahun in a mit ngei ngawl tu hell meisung ah khut lang ni taw pai sang in, pumpi kim ngawl in nuntakna sung ah tum tu phazaw hi: (Geenna g1067)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
Taciang na peang in hong khialsak le, at tan in: bangmahun in a mit ngei ngawl tu hell meisung ah khut lang ni taw pai sang in, pumpi kim ngawl in nuntakna sung ah tum tu phazaw hi: (Geenna g1067)
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
Taciang na mit in hong khialsak le, khel keak in: bangmahun in a mit ngei ngawl tu hell meisung ah khut lang ni taw pai sang in, pumpi kim ngawl in nuntakna sung ah tum tu phazaw hi: (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
Jesus sia lamkal ah a pai laitak in, mi khat hong tai a, khupdin in, Sya pha awng, tawntung nuntakna ka nga thei natu in bang vawt tu khi ziam? ci in dong hi. (aiōnios g166)
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Tu hun in inn le lo hi kale, nu te hi kale, u le nau hi kale, tate hi kale, vawtsiatna tatuam taw a se za in sang tu a; hongpai lai tu hun ah tawntung nuntakna sang tu hi. (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn g165, aiōnios g166)
Jesus in tua theikung sia, Kuama in bangmahun in na nga ne nawn heak tahen, ci hi. A nungzui te in zong za uh hi. (aiōn g165)
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn g165)
Ama in Jacob suan te a tawntung in uk tu a; Ama ukna sia tawp hun nei ngawl tu hi. (aiōn g165)
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn g165)
I pu i pa te kung ah a sonsa bangma in, Abraham le a suan te hu hi, ci hi. (aiōn g165)
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn g165)
Leitung kipat lai pan in kamsang thiangtho te kam zang in son zo hi: (aiōn g165)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn g165)
Doai ngilo te in Jesus kung ah, dum thukpi sung ah a hawlkhiat ngawl natu in ngen hi. (Abyssos g12)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
Taciang nang, Capernaum, van dong hong ki lamsang zo napi, hell sung dong in khiaksuk kik na hi tu hi. (Hadēs g86)
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
Taciang, en vun, thukhamhil khat hong ding a, Syapa awng, tawntung nuntakna ka lua natu bang vawt tu khi ziam? ci in ze-et hi. (aiōnios g166)
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Ahihang na lau tu uh te kidop na kong pia khol tu hi: a thalup zawkciang hell sung ah a khia thei sia na lau vun; hi hi, keima in kong son hi, lau vun. (Geenna g1067)
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
Hi a thuman ngawl neisa keampa in thimtheltak in a vawt nate a topa in pok hi: banghangziam cile, leitung mihing te sia amate hun sung, khuavak tate sang in lupil zaw uh hi. (aiōn g165)
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
Keima in kong ci hi, note hileitung pan na pusua uh ciang in tawntung omna biakbuk sung ah hong sang tu na nei thei natu uh in, leitung sum le pai taw ngualtam vawt vun. (aiōnios g166)
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
Taciang a ngim thuak na hell sung pan a tungsang a et ciang in, a khuala mama na ah Abraham mu hi, taciang a kangsung ah Lazarus om hi. (Hadēs g86)
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
Lampui khat in Jesus kung ah, Sya pha awng, tawntung nuntakna ka nga thei natu in bang vawt tu khi ziam? ci in dong hi. (aiōnios g166)
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Tu hun sung in a se tampi le hongpai lai tu hun sung ah tawntung nuntakna a nga ngawl tu om ngawl hi, ci hi. (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Jesus in amate tung ah, Hi leitung mite kipui uh a, nupa tu in ki pia uh hi: (aiōn g165)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn g165)
Ahihang tua leitang lua tu kilawm ci in ngaisut te le thina pan a thokik te sia kipui le nupa tu in ki piak om nawn ngawl tu hi. (aiōn g165)
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn g165)
A kuamapo Ama a um peuma, ki siacip ngawl tu a, tawntung nuntakna nei hi. (aiōnios g166)
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Banghangziam cile Pathian in leitung mite it mama ahikom a Tapa neisun pia hi, akuamapo Ama a um peuma kisia ngawl tu a, nuntak tawntungna nei hi. (aiōnios g166)
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Tapa a um peuma tawntung nuntakna nei hi: Tapa a um ngawl peuma in nuntakna mu ngawl tu hi; ahihang Pathian thin-ukna a tung ah om tu hi, ci in zo hi. (aiōnios g166)
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios g166)
Ahihang keima i ka piak tu tui a dawn peuma a dangtak kik nawn ngawl tu hi; ahihang ka piak tu tui sia ama sung ah tawntung nuntakna a piangsak ciktui hi tu hi, ci hi. (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Taciang anla peuma in sep thaman nga tu a, tawntung nuntakna atu in thing nga te kaikhawm tu hi: taciang thaici a poai te le anla te lungdam khawm tu uh hi. (aiōnios g166)
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
A tatak in kong ci hi, ka kammal za a, kei hong sawl pa a um peuma in, tawntung nuntakna nei hi, taciang mawsiatna sung ah theng ngawl tu hi; ahihang thina pan in nuntakna ah kantan zo hi. (aiōnios g166)
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios g166)
Tawntung nuntakna om hi, ci na ngaisut uh hang in, laithiangtho sung ah na zong uh hi; ahihang laithiangtho in keima thu tettipang hi. (aiōnios g166)
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios g166)
A kisia thei an atu in naseam heak vun, ahihang tawntung nuntakna ciangdong a kho tu, mihing Tapa in note tung ah hongpiak tu an atu in seam zaw vun: banghangziam cile Pa Pathian in ceptena khen zo hi, ci hi. (aiōnios g166)
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios g166)
Tapa a mu peuma in ama um a, tawntung nuntakna nei tu le ni tawpkhak ni ciang in keima in ka thawkiksak tu sia keima hong sawlpa i deina a hihi, ci hi. (aiōnios g166)
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios g166)
A tatak in kong ci hi, keima hong um peuma in tawntung nuntakna nei hi. (aiōnios g166)
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios g166)
Keima in vantung pan hongpai a nungta anluum ka hihi. Khat po in hi anluum a ne le nungta tawntung tu hi, taciang ka piak tu anluum zong ka taksa hi a, tua in leitung mite nuntakna atu ka piak a hihi, ci in zo hi. (aiōn g165)
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn g165)
A kuamapo in ka taksa ne a, ka thisan a dawn peuma in, tawntung nuntakna nei hi; taciang ni tawpkhak ni ciang in ka thokiksak tu hi. (aiōnios g166)
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios g166)
Hi thu sia vantung pan hong tuaksuk anluum a hihi: na pate uh mana ne a, a thi uh bang hi ngawl hi: hi anluum a ne peuma a tawntung in nungta tu hi, ci hi. (aiōn g165)
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn g165)
Simon Peter in, Topa awng, a kua kung ah pai tu khu ziam? nangma in tawntung nuntakna kammal te na nei hi. (aiōnios g166)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios g166)
Taciang sila sia a tawntung in innsung ah om tawntung ngawl hi: ahihang Tapa ahile om tawntung hi. (aiōn g165)
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn g165)
A tatak in kong ci hi, khatpo in ka kammal a zui le bangmahun in thina mu ngawl tu hi, ci hi. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn g165)
Tua zawkciang in Judah te in, tu in doai vei ni hi, ci ka he uh hi. Abraham le kamsang te thi siat zo hi; ahihang nangma in, khatpo in ka thu a zui le bangmahun in thina tep ngawl tu hi, na ci hi, ci uh hi. (aiōn g165)
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn g165)
Leitung kipat pan mittaw in a piang kuama a mit khuamusak, ci i za ngei bua hi. (aiōn g165)
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
Taciang amate tung ah, tawntung nuntakna ka pia a; bangmahun in kisia ngei nawn ngawl tu hi, kuama in zong ka khutsung pan hong sut thei ngawl tu hi. (aiōn g165, aiōnios g166)
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn g165, aiōnios g166)
Taciang in a kuamapo nungta a, keima hong um peuma sia bangmahun in thi nawn ngawl tu uh hi. Hi thu na um ziam? ci hi. (aiōn g165)
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn g165)
A nuntakna a it peuma sum tu hi; taciang hi leitung ah a nuntakna a ensan peuma tawntung nuntakna dong in keamcing tu hi. (aiōnios g166)
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
Mihonte in, Christ sia a tawntung in hong teang tu hi, ci thukham tungtawn in ka za uh hi: taciang nangsia bangbang in, mihing Tapa sia khai tu uh hi, ci ni ziam? hi mihing Tapa sia akua ziam? ci in zo uh hi. (aiōn g165)
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
Taciang a thupiak te sia tawntung nuntakna hi, ci ka he hi: tua ahikom bangpo ka pau hial zong in, Pa i hong son bang in ka pau hi, ci hi. (aiōnios g166)
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
Peter in, bangmahun in nangma in ka peang hong silsak ngei ngawl tu ni hi, ci hi. Jesus in, Na peang ka sil bua ahile, kei taw ki zopna na nei bua hi, ci in zo hi. (aiōn g165)
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
Taciang Pa kung ah ka ngen tu a, Ama in a dang Hupa note hong pia tu hi, taciang note kung ah a tawntung in hong om tu hi; (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
Tapa tung ah na piak theampo, Ama in tawntung nuntakna pia tu in mihing theampo tung ah thuneina na pia zo hi. (aiōnios g166)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
Amate in nangma bek a thuman Pathian hi, ci le na sawlkhiat Jesus Christ heak sia tawntung nuntakna hi. (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
Banghangziam cile nangma in ka tha sia hell sung ah na nusia bua hi, na Mi Thiangtho sia a muatcip tu na oai bua hi. (Hadēs g86)
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs g86)
Hi Christ thawkikna a mukhol hu in, a tha sia hell ah nusia ngawl hi, a taksa zong muat ngawl hi, ci son hi. (Hadēs g86)
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs g86)
Leitung pian pan kipan Pathian in Ama kamsang thiangtho te kam tungtawn in a sonkholsa bang in, na theampo thaksua na hun dong Jesus Christ sia vantung ah om suak tu hi. (aiōn g165)
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn g165)
Tua zawkciang in Paul le Barnabas te sia hangsan seseam uh a, Pathian thu note kong hil phot uh kul hi: ahihang note in na vawk uh a, noma le noma tawntung nuntakna nga tu kiphu ngawl in thu na khen uh hi, en vun, ko Gentile te sang ah ka kihei zo uh hi. (aiōnios g166)
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios g166)
Hi thu sia Gentile te in a zak uh ciang in, lungdam mama uh a, Topa thu poktek uh hi: taciang tawntung nuntakna nga tu in a koi sa te in um uh hi. (aiōnios g166)
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios g166)
Pathian in leitung piancil pan in a nasep theampo he siat hi, ci ki at zo hi. (aiōn g165)
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
Banghangziam cile leitung a ki bitphua pan kipan in, mit taw mu thei ngawl Pathian i tawntung vangletna le ama i hi na te sia a vawt nate tungtawn in ki tel thei hi, tua ahikom amate in paulap a nei bua uh hi: (aïdios g126)
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios g126)
Amate in Pathian thuman sia leilot thu suaksak uh a, tawntung minthanna bitphuapa Pathian sang in a bitphua sa te bia in paai zaw uh hi. Amen. (aiōn g165)
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Thinsau in napha seam paisuak a, minthanna, upatna le thi thei ngawl nuntakna a zong peuma tawntung nuntakna pia tu hi: (aiōnios g166)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
Tabang in mawna in thina dong a uk bangma in, i Topa Jesus Christ tungtawn in thuthiamna in thutang suana tungtawn in tawntung nuntakna dong uk hi. (aiōnios g166)
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Ahihang tu in mawna pan na suakta zo uh a, Pathian i sal te suakzo na hi uhkom, thianthona sang ah na phatuam uh a, a tawpna sia tawntung nuntakna a hihi. (aiōnios g166)
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Banghangziam cile mawna thaman sia thina a hihi; ahihang Pathian letsong sia i Topa Jesus Christ tungtawn in tawntung nuntakna a hihi. (aiōnios g166)
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Amate sia pu le pa te taw ki zom in, Christ zong cilesa ngeina taw amate sung pan hong theng a hihi, tua Christ sia na theampo tung ah om a, Pathian in a tawntung in thupha pia hi. Amen. (aiōn g165)
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Ahi bale, a thuk mama na mun ah akua tuaksuk tu ziam? ci na thinsung pan in ci heak in, tasia in Christ sia thina pan thokiksak tu in akua a thuk mama na mun ah tuaksuk tu ziam, cinopna a hihi. (Abyssos g12)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
Banghangziam cile mi theampo tung ah hesuakna a nei thei natu in, Pathian in amate theampo sia up ngawl na sung ah vaihuaisak siat hi. (eleēsē g1653)
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
Banghangziam cile na theampo sia Ama sung pan le Ama tungtawn in le Ama atu a hihi: Ama tung ah minthanna a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Taciang hi leitung pianzia zil in zui heak vun: ahihang na pha, a san thamman le Pathian deina kicing tetti na lak thei natu uh in, na thinsung puaphat kikna tungtawn in na nuntak zia uh lai in om tavun. (aiōn g165)
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn g165)
Keima lungdamna le Jesus Christ i thuhilna bang in Ama sung ah hong kipsak vangletna sia, tu in thuku pualak hun hi a, tua thu sia leitung piancil pan kipan in thuku in a kikoi a hihi. (aiōnios g166)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
Ahihang tu in kamsang te laithiangtho tungtawn in kilaak zo a, tawntung Pathian i thupiak bang in minam theampo tung ah upna thunitna atu in ki hesak zo h: (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
Ama bek a ciim Pathian tung ah Jesus Christ tungtawn in minthanna kip tawntung tahen! Amen. (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)
Mihing ciim koisung ah om ziam? Thukhamhil te koisung ah om ziam? hi leitung ah thu nial te e koisung ah om zia? Pathian in hi leitung pilna sia mawmawtna suaksak zo hi ngawl ziam? (aiōn g165)
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn g165)
Ahizong pilna sia a picing sa te sung bek ah ka pau uh hi: ahihang hi leitung pilna hi ngawl hi, a bokik tu hi leitung thunei te i pilna zong hi ngawl hi: (aiōn g165)
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn g165)
Ahihang hi leitung a om ma in Pathian in kote minthanna tu in a sekholsa thu ku, tua Pathian i ciimna thuku ka son uh hi: (aiōn g165)
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn g165)
Tua ciimna sia leitung thunei te kuama in he ngawl hi: banghangziam cile he uh hile, minthanna Topa sia thinglamte tung ah khai ngawl tu uh hi. (aiōn g165)
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn g165)
Kuama peuma ama le ama kitheam heak hen. Note sung ah khatpo in ama le ama mipil bang in a ki ngaisun tha le, mipil a sua thei natu in mi mawmaw suak masa tahen. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
Tua ahikom an in i suapui pa a puksak ahile, ka suapui pa ka puksak ngawl natu in, leitung a kip sung theampo sa ka ne batu hi. (aiōn g165)
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn g165)
Tu in hi thu theampo amate tung ah a piang te i ette tu a hihi: taciang amate tung ah leitung bo na a thet nate zong eite danpiak natu in a ki at a hihi. (aiōn g165)
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn g165)
Maw thina awng, na ngu koisung ziam? Maw thanmual awng, na zawna koisung ziam? (Hadēs g86)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
Pathian lim le meal a hi Christ i lungdamna thupha a vanglian khuavak sia amate tung ah a tan thei ngawl natu in, hi leitung pathian in a um ngawl te thinsung mittawsak hi. (aiōn g165)
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn g165)
Banghangziam cile ka haksatna a zaang mama sia tawmvei atu hi a, tua in a ngit mama a tuanngen tawntung minthanna suaksak hi; (aiōnios g166)
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios g166)
A kimu thei nate ka en bua uh hi, ahihang a ki mu thei ngawl nate ka en zaw uh hi: banghangziam cile a ki mu thei nate sia tawmvei atu a hihi; ahihang a ki mu thei ngawl nate sia tawntung atu a hihi. (aiōnios g166)
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios g166)
Banghangziam cile i lei inn, hi puanbuk a sia le, vantung ah mihing khut taw sak a hi ngawl Pathian i tawntung inn i nei hi, ci sia i he hi. (aiōnios g166)
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios g166)
Ama in mun theampo ah hawm a, mizawng te pia hi: a thutang suana sia a tawntung in kip hi, ci in ki at hi. (aiōn g165)
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Leilot thu son ngawl khi hi, ci sia tawntung poktak i Topa Jesus Christ i Pa le Pathian in hong he hi. (aiōn g165)
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
Tu hun hunsia kawm sung pan kote suaktasak tu in i Pa Pathian deina bang in kote mawna te atu in Ama le Ama ki pia zo hi: (aiōn g165)
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
Ama tung ah minthanna a kumtawn in om tawntung ta hen. Amen. (aiōn g165)
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Banghangziam cile ama cilesa sung ah thaici a poai sia in cilesa siatsuana at kik tu hi; ahihang Thaa sung ah thaici a poai peuma in Thaa i tawntung nuntakna at kik tu hi. (aiōnios g166)
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios g166)
Ama sia thunei na, vangletna, hatna le ukzawkna theampo ahizong, taciang tu hun le hongpai lai tu hun sung ah min theampo sang in ahizong, nasiatakin sang zaw hi: (aiōn g165)
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
A bosa hun sung ah leitung ngeina bang in ahizong, hui sung a om vangletna a ukpa ngeina bang in ahizong in, thu ni ngawl tate sung ah na a seam thaa ngeina bang in ahizong, note na nungta ngei uh hi: (aiōn g165)
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn g165)
Tua thu sia hongpai tu hun sung ah eite tung ah ama thuthiamna i a lamdang hauna sia a phatna sung ah Christ Jesus tungtawn in hong lak thei natu a hihi. (aiōn g165)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn g165)
Jesus Christ tungtawn in na theampo a bitphua Pathian sung ah, leitung piancil pan kipan a phualseal ki pawlkhopna thuku sia mi theampo tung ah hong musak tu hi: (aiōn g165)
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn g165)
Tua thu sia tawntung ngealna bangma in i Topa Christ Jesus sung ah ngealna hi a: (aiōn g165)
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn g165)
Pawlpi sung le Christ Jesus tungtawn in hun theampo sung ah tawp ni nei ngawl leitung dong in minthang tahen. Amen. (aiōn g165)
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Banghangziam cile cilesa le thisan langpan in i do bua hi, ahihang thuneina te, vangletna te, hileitung khuazing a uk te, tungsang i a man ngawl thaa te i do hi. (aiōn g165)
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn g165)
Tu in Pathian le i Pa tung ah minthanna a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Khang tampi sung a ki phualseal thuku sia tu in Ama mithiangtho te tung ah hong kilangsak zo hi: (aiōn g165)
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn g165)
Amate sia tawntung suksiatna taw Topa le a minthang vangletna mai pan in dan pia tu hi; (aiōnios g166)
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
Tu in i Topa Jesus Christ ama tatak le hong it i Pa Pathian in a tawntung henepna le lametna pha sia a thuthiamna tungtawn in hong pia zo hi, (aiōnios g166)
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios g166)
Ahihang nidang ciang in tawntung nuntakna atu a um lai tu te atu ettte tu in, keima mawneibel tung ah Jesus Christ in a thinsauna theampo hong kilangsak a, a hesuakna ka sang hi. (aiōnios g166)
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios g166)
Tu in tawntung Kumpi, a thi thei ngawl, ki mu thei ngawl, a cialcing Pathian khatbek omsun tung ah zatakna le minthanna a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Upna sung ah phatak in do in, tawntung nuntakna lenkip in, tua atu in nangma zong sap sa na hihi, taciang tetti tampi mai ah na pualak zo hi. (aiōnios g166)
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
Ama bek in thi thei ngawl na nei hi, kuama in a nai a neak thei ngawl khuavak sung ah om hi; kuama in mu ngei ngawl a, mu zong mu thei ngawl hi: Ama tung ah zatakna le vangletna a tawntung in om tawntung tahen. Amen. (aiōnios g166)
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
Hi leitung i mihau te sia amate le amate a sang mama in a ki ngaisut ngawl natu le, a kip ngawl hauna te muang ngawl in, na theampo nuamtak in i zat tu a tam mama in hong pia a nungta Pathian sia muan in a nei zawk natu uh vaitha in; (aiōn g165)
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
Ama in eite hong ngum a, a thiangtho sapna taw hong sam hi, hi thu sia eite sepna bang hi ngawl in, Ama ngeal na le thuthiamna bang in hi a, tua thu sia leitung ki pat ma in Christ Jesus sung ah hong pia zo hi, (aiōnios g166)
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Tua ahikom Pathian tealsa te in, Christ Jesus sung ah tawntung minthanna taw ngupna a nga thei natu in na theampo ka thuak hi. (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
Banghangziam cile Demas in hi leitung a it hu in hong nusia a, Thessalonica khua ah pai hi; Crescens sia Galatia ah pai a, Titus sia Dalmatia ah pai hi. (aiōn g165)
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn g165)
Taciang Topa in nasep pha ngawl theampo sung pan in hong suaktasak tu hi, taciang Ama in vantung kumpingam hong thet dong hong suaktaksak tu hi; Ama tung ah minthanna om tawntung tahen. Amen. (aiōn g165)
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn g165)
Tawntung nuntakna i lametna sung ah, leilot thu son ngawl Pathian in leitung kipatcil ma in a kamciam sa; (aiōnios g166)
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Tua Pathian i thuthiamna in Pathian nei ngawl nuntakzia le cilesa deina nial tu a, a pilvang, a thutang, Pathianmi hina taw tu hun sung ah a nungta tu in hong hil hi; (aiōn g165)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
I lamet tawntung nuntakna bangma in, ngamhlua te i hi thei natu in, Ama thuthiamna tungtawn in thutang hong suaksak hi. (aiōnios g166)
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios g166)
Hun tomno sung a tai na thu sia a tawntung in na nei kik thei natu hi zaw tu hi; (aiōnios g166)
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
Hi ni tawpkhak sung ah a Tapa tungtawn in eite tung ah thu hong hil hi, Ama sia na theampo ngamhlua tu in a kikoi hi a, Ama tungtawn in leitung zong vawt hi; (aiōn g165)
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
Ahihang Tapa tung ah, maw Pathian awng, na kumpi tokhum sia kumtawn hi a: na ukna ciangkhut sia thutang suana ciangkhut a hihi, ci hi. (aiōn g165)
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
Mundang zong ah, nangma sia Melchizedek bang in tawntung thiampi na hihi, ci hi. (aiōn g165)
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
Taciang Ama a cialcin zawkciang in, thu ni te theampo atu in tawntung ngupna i kipatna hong suak a; (aiōnios g166)
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios g166)
Tui kiphumna taw kisai hilna te le khut ngak na thu, taciang mithi te thawkikna le tawntung thukhenna, hi bitphuana thu te kan kik nawn ngawl in, picinna sang ah mainawt seseam tawng. (aiōnios g166)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios g166)
Taciang Pathian thupha le hongpai pheang tu leitung i vangletna te tep zo hi napi, (aiōn g165)
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn g165)
Tua mun ah lamlak Jesus sia eite atu in tum hi, Ama sia Melchizedek bang in tawntung thiampi sang in vawt hi. (aiōn g165)
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn g165)
Banghangziam cile, nangma sia Melchizedekk bang in tawntung thiampi na hihi, ci in ama in tettipang hi. (aiōn g165)
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
Banghangziam cile tua thiampi te sia thukham om ngawl in thiampi a ki suaksak te a hihi; ahihang Jesus sia thukham taw ahikom in, Topa in kiciam a, ki sikkik ngawl tu hi, nangma sia Melchizedek bang in tawntung thiampi na hihi, ci hi: (aiōn g165)
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn g165)
Ahihang Jesus sia nungta paisuak ahikom a ki lai thei ngawl thiampi hina nei hi. (aiōn g165)
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn g165)
Banghangziam cile thukham in thaneamna a nei mihing te thiampi sang in vawt hi; ahihang thukham pan kipan in a kiciamna thu in tawntung kicinna Tapa sia thiampi sang in vawt hi. (aiōn g165)
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn g165)
Taciang keal le khuino thisan taw zong hi ngawl hi, ahihang Ama thisan tatak taw mun thiangtho sung ah khat vei tum a, eite atu in tawntung tatna hong ngasak hi. (aiōnios g166)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
Tawntung Thaa tungtawn in Ama le Ama Pathian mai ah a nin bang ngawl in a ki pia, Christ thisan in a nungta Pathian atu naseam tu in, note i khentel theina sia a thi naseam te pan in bangza in thiangthosak seseam tu ziam? (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
Tua ahikom a masa thuciam nuai ah thukham paltan nate tatna atu in Christ hong thi a, a sap te in tawntung ngamh kamciam a lua thei natu in, Ama sia thuciam thak i palai a hihi. (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
Tabang hibale, leitung piancil pan kipan in a thuak tawntung kul tu hi: ahihang tu in, hun bo na ah Ama le ama biakpiakna a kipiakna tungtawn in, mawna vawk tu in Ama sia khatvei kilang zo hi. (aiōn g165)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
Leitung sia Pathian thu taw a ki bitphua a hihi, tua ahikom a ki mu thei nate sia a ki mu thei nate pan in a ki vawt hi ngawl hi, ci sia upna tungtawn in i he thei hi. (aiōn g165)
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn g165)
Jesus Christ sia zei ni, tu ni, le a tawntung in kibang hi. (aiōn g165)
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn g165)
Tawntung kamciam i thisan tungtawn in tuu hon a cing Tuucing lian, i Topa Jesus sia thina pan a lakhia thinnopna Pathian in, (aiōnios g166)
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios g166)
Ama deina a pha theampo na vawt thei natu uh in hong cialcingsak tahen, Jesus Christ tungtawn in note sung ah a nasepna sia Ama mai ah lungkimna tatak a hihi; tua Jesus tung ah a tawntung in minthanna om tawntung tahen. Amen. (aiōn g165)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn g165)
Taciang leii sia mei a hihi, phatngawlna i leitung a hihi: tasia bangma in leii sia i pumpi sung ah pumpikhen khat hi a, tua in i pumpi niinsak hi, cilesa hina theampo hei kakoai siat hi; taciang hell mei tung ah hong em hi. (Geenna g1067)
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna g1067)
A muat thei thaici hi ngawl, a tawntung nungta in a om tawntung Pathian thu, a muat thei ngawl thaici tungtawn in na suakkik zo uh hi. (aiōn g165)
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn g165)
Ahihang Topa thu sia a tawntung in kip hi. Taciang hi thu tungtawn in lungdamna thupha sia note tung ah hong ki hil hi. (aiōn g165)
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn g165)
Jesus Christ hang in na theampo ah Pathian a ki pok thei natu in, mi khatpo in thu a hil le, Pathian kammal te hil bang tatak in hil tahen; mi khatpo in ngualdang na a sepsak le, Pathian i hi theina a piak bang in seam tahen: Pathian tung ah pokna le ukzawkna a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Christ Jesus tungtawn in eite tawntung minthanna sung ah hongsam, thuthiamna theampo i Pathian in tawmvei haksatna na thuak zawk uh ciang in, hong cialcingsak in hong khosak tu a, tha hong hatsak in hong kipsak tu hi. (aiōnios g166)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
Vangletna le ukzawkna sia a tawntung in Ama tung ah om tahen. Amen. (aiōn g165)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Tabang in i Topa le ngumpa Jesus Christ i tawntung ukna sung ah tum thei natu a dimlet in na nga tu uh hi. (aiōnios g166)
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
Banghangziam cile mawna a vawt vantungmi te sia Pathian in koithong ngawl hi, ahihang amate sia hell sung ah khiasuk in, thukhenna ni atu in koi a, khuazing thikkol sung ah ap hi; (Tartaroō g5020)
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
Ahihang hesuakna sung ah ahizong, ka Topa le Ngumpa Jesus Christ heakna sung ah ahizong in, khang tavun. Ama tung ah minthanna sia tu le a tawntung in om paisuak tahen. Amen. (aiōn g165)
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Tua nuntakna sia hong kilang zo a, kote in ka mu uh hi, taciang tettipang in tua nuntakna thu kong lak uh hi, taciang kote tung ah hong kilang zo hi; (aiōnios g166)
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios g166)
Leitung le a iplakna te bosiat hi: ahihang Pathian deina a vawt peuma a tawntung in kip hi. (aiōn g165)
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Taciang hi thu sia Ama in hong ciamsa kamciam hi a, nuntak tawntung na hong ciam hi. (aiōnios g166)
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
Akua mapo a suapui a ensan peuma tualthat a hihi: taciang tualthat te sung ah tawntung nuntakna om ngawl hi, ci na he uh hi. (aiōnios g166)
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios g166)
Taciang tetti sia hisia a hihi, Pathian in tawntung nuntakna hong pia a, hi nuntakna sia a Tapa sung ah om hi. (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
Pathian Tapa i min a um note tawntung nuntakna ka nei uh hi, ci na heak thei natu uh in, hi thu te note tung ah kong at hi. (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Pathian Tapa hongpai a, a thutang Pathian heakna ciimna hongpia hi, ci i he hi. A thutang Pathian le a Tapa Jesus Christ sung ah i om hi. Hi thu sia a thutang Pathian le tawntung nuntakna a hihi. (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
I sung ah om in, a tawntung in a om tu thutak hang in hong it khi hi. (aiōn g165)
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
Taciang amate dinmun masa keamcing ngawl in a ommun a nusia vantungmi te sia thukhenna ni thupi atu in khuamial sung ah tawntung thikkol taw hen in khum hi. (aïdios g126)
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios g126)
Tasia bangma in Sodom, Gomorrah le a kim a om khuapite zong, a tung ah a sonsa bangma in, paktat mawna, ngualdang zi taw mawna sung ah a nuntak uh hu in, tawntung mei taw thukkikna a thuakna sia ette tu in koi hi. (aiōnios g166)
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios g166)
Tuipi sung ah tuihual ngilo a phuan suak bang in, amate maizumna tuiphuan le aksi vakthap bang hi uh a; amate atu in tawntung khuazing ngammial pi koisak khol hi. (aiōn g165)
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn g165)
Pathian itna sung ah noma le noma ki keamcing in, i Topa Jesus Christ i hesuakna sia tawntung nuntakna atu in ngak tavun. (aiōnios g166)
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios g166)
Ama bek a ciim Pathian ahi Ngumpa tung ah minthanna, vangletna, thahatna le thuneina sia, a bo sa hun theampo sung, tu le a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
A Pa Pathian mai ah kumpi le thiampi in hong vawt pa tung ah; minthanna le ukzawkna a tawntung in om tahen. Amen. (aiōn g165)
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn g165)
Keima sia a nungta pa ka hihi, ka thi ngei hi; taciang en in, Keima sia a tawntung in ka nungta zo hi, Amen; taciang hell le thina i tawtang te ka nei hi. (aiōn g165, Hadēs g86)
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn g165, Hadēs g86)
Tua nganhing te in a tawntung in nungta a, kumpi tokhum tung a to pa tung ah minthanna, upatna le pokna te a piak uh ciang in, (aiōn g165)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn g165)
Upa kul le li te zong kumpi tokhum tung a to pa i mai ah bok tek uh hi, a tawntung a nungta pa bia in, amate i kham lukhu te sia kumpi tokhum mai ah khiasuk uh a, (aiōn g165)
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn g165)
Vantung le leitung a om te ahizong, lei nuai le tuipi sung a om, a bitphuana te theampo in, thupha, upatna, minthanna le vangletna te sia kumpi tokhum tung ah a to pa le Tuuno tung ah, om tawntung tahen, a ci na ka za hi. (aiōn g165)
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn g165)
Ka et ciang in siphu puang khat ka mu hi: taciang a tung a to pa min sia thina hi a, Hell in zui hi. Amate tung ah leitung khen li sua khen khat te sia namsau, ngilkialna, thina le leitung nganhing te taw that tu in vangletna pia hi. (Hadēs g86)
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs g86)
Amen; Thupa, minthanna, ciimna, pokna, upatna, vangletna le thahatna te a tawntung in i Pathian tung ah om tahen, Amen, ci uh hi. (aiōn g165)
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn g165)
Vantungmi a nga na in a tum zawkciang in, vangtung pan in aksi khat a taksuk ka mu hi: taciang ama sia mong nei ngawl dum hon na tawtang pia hi. (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
Mong nei ngawl dum sia a hon ciang in; mong nei ngawl dum sung pan in meikhu pusuak a, meikhuk pan a pusuak meikhu in, ni le van hawmpui zong zingcipsak hi. (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
Amate zong kumpi nei uh a, tasia sia mong nei ngawl dum sung a om vantungmi a hihi, a min sia Hebrew kam in Abaddon hi a, Greek kam in Apollyon a hihi. (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
A tawntung a nungta, vantung le a sung a om na te, leitung le a sung om na te, tuipi le a sung om nate a piangsak pa min taw a hun haisang nawn ngawl tu hi, ci in kiciam hi: (aiōn g165)
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn g165)
Amate i tetti panna a man ciang in, mong nei ngawl dum sung pan hong kato nganhing in, ngal vawt in do tu a, zo in that tu hi. (Abyssos g12)
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos g12)
Vantungmi a sali na in a tum zawkciang in; vantung pan in aw ngingtak in, leitung kumpingam te sia i Topa le Christ i kumpingam suak a; Ama in a tawntung in hong uk tu hi, ci hi. (aiōn g165)
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Vankimlai ah a dang vantungmi khat a leang ka mu a, leitung a om minam, phung, kampau le mi theampo tung ah a pualak tu tawntung lungdamna thupha nei hi, (aiōnios g166)
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios g166)
Taciang amate vawtsiatna meikhu sia a tawntung in a tungsang ah kato hi: taciang sapi le a milim a bia te ahizong, a min ceptena a sang te ahizong, sun le zan in tawlnga ngawl hi, ci in aw ngingtak in ci hi. (aiōn g165)
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn g165)
A tawntung a nungta Pathian thin-ukna taw a kidim, kham kuang sali te sia, nganhing li te sung pan khat in vantungmi sali te pia hi. (aiōn g165)
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Na mu nganhing sia sia, a omsa, tu in a om ngawl; mong nei ngawl dum sung pan hong kato tu a, siatsuana sung ah theng tu hi: taciang leitung bitphua pan kipan nuntakna laibu sung ah min ki at te in a omsa, tu in om ngawl a, a om pheang tu nganhing a mu ciang in lamdangsa mama tu hi. (Abyssos g12)
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos g12)
Taciang amate in, Halelujah, ci kik uh hi, Taciang ama ki hal na meikhu sia a tawntung in kato hi. (aiōn g165)
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Sapi sia man thei uh hi, taciang sapi i ceptena zong nga a, a milim a bia te theam in sapi mai ah nalamdang a tatuam a lak leilot kamsang zong man thei uh hi. Hi te a ni in kan taw a kuang tawn tung meiliipi sung ah a nungta in khiasuk hi. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Mong nei ngawl dum tawtang le thikkol lianpi a len vantungmi khat van pan a tuaksuk ka mu hi. (Abyssos g12)
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos g12)
Kum tulkhat a bo dong, leitung minam theampo theam thei ngawl tu in, mong nei ngawl dum sung ah khiasuk a, khum in a tung pan ceptena khen hi: taciang kum tulkhat a bo ciang in tawmvei tha kik tu hi. (Abyssos g12)
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos g12)
Hi te a theam Satan zong sapi le leilot kamsang te omna mun, kan taw a ki hel meiliipi sung ah khiasuk hi, tua mun ah sun le zan in haksatak in vawtsiatna a tawntung in thuak tu hi. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Tuipi in a sung a mithi te ap hi; taciang thina le hell in zong amate sung a om mithi te ap uh hi: taciang mi theampo amate sepna bang tek in thukhen hi. (Hadēs g86)
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs g86)
Taciang thina le hell sia meiliipi sung ah khiasuk hi. Hisia sia nivei thina a hihi. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Akua mapo nuntakna laibu sung ah min a ki at a mu ngawl peuma meilipi sung ah khiasuk hi. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ahihang a lau te, a um ngawl te, a lipkhap huai te, tual that te, paktat mawna vawt te, bum le ai toai te, milim bia te le leilot thu son te theampo, kan le mei taw a kang meiliipi sia amate i lua tu hi tu hi: tasia sia nivei thina a hihi. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
Tua mun ah zan om nawn ngawl a hikom; meivak zong kisam nawn ngawl tu hi, Ni tang zong kisam nawn ngawl hi; banghangziam cile Topa Pathian in amate khuavak pia tu a: amate in a tawntung in uk tu hi. (aiōn g165)
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn g165)
Questioned verse translations do not contain Aionian Glossary words, but may wrongly imply eternal or Hell
Hi te sia tui om ngawl tuikhuk, huipi suangval i letkeak meii bang a hihi; amate atu in a sa mama tawntung khuazing koisak hi. (questioned)

CSB > Aionian Verses: 200, Questioned: 1
CHW > Aionian Verses: 264