< Luke 9 >

1 A hubat thlanghqa hlaihih ce ak khy coengawh, qaaikhqi hqek thainak ingkaw thlak tlo qoei sak thainaak ce pek khqi nawh,
Yesu atawayitana khumi ndi awiriwo pamodzi, Iye anawapatsa mphamvu ndi ulamuliro wotulutsa ziwanda zonse ndi kuchiritsa matenda.
2 Khawsa awithang leek kqawn aham ingkaw thlak tlokhqi qoei sak aham tyi khqi hy.
Ndipo Iye anawatumiza kukalalikira za ufumu wa Mulungu ndi kukachiritsa odwala.
3 A mingmih a venawh: “Lam awhkaw aham ikaw awm koeh khyn uh - sawnghqawl, sawngsa, phaihpi, tangka ingkaw angki zunghih koeh khyn uh.
Iye anawawuza kuti, “Musatenge kanthu paulendo. Musatenge ndodo, thumba, buledi, ndalama, ndi malaya apadera.
4 Nami pahnaak im a hoei awh, ce a khaw ce nami cehtaak hlan dy awm poe uh.
Nyumba iliyonse imene mulowa, mukhale momwemo kufikira mutachoka mu mzindawo.
5 Thlang ing a ma ni do khqi awhtaw, ce a khaw ce nami cehtaak awh nami khawpha awhkaw dekvai ce khawk sih uh,” tinak khqi hy.
Ngati anthu sakulandirani, sasani fumbi la kumapazi anu pomwe mukuchoka mu mzinda wawo ngati umboni owatsutsa.”
6 Cedawngawh, cet unawh khaw pynoet coeng pynoet awh awithang leek kqawn unawh thlak tlokhqi ce qoei sak uhy.
Ndipo iwo ananyamuka napita, mudzi ndi mudzi, kulalikira Uthenga Wabwino ndi kuchiritsa anthu paliponse.
7 Herod boei ing cawhkaw awithang ce za hy. Thlang vang ing, “Johan ce tho tlaih nawh ni,” ti uhy,
Tsopano Herode olamulirayo anamva zonse zimachitikazi. Ndipo iye anavutika kwambiri chifukwa ena amati Yohane waukitsidwa kwa akufa,
8 thlang vang ingtaw, “Elijah dang law tlaih nawh ni,” ti bai uhy, thlang vang bai ingtaw, “Syn awhkaw tawngha pynoet oet hqing tlaih nawh ni,” tinawh kqawn uhy.
ena amati Eliya waonekera, ndipo ena anatinso mmodzi wa aneneri akalekale waukanso.
9 Cehlai Herod ingtaw, “Johan ce a hawng tlyk hawh hlai nyng; vawhkaw awithang kang zaak ve a u bai hy voei nu?” ti hy. Cedawngawh anih ce huh aham ngaih hy.
Koma Herode anati, “Ine ndinamudula mutu Yohane. Nanga uyu ndani amene ndikumva zinthu zotere za Iye?” Ndipo iye anayesetsa kuti amuone Iye.
10 Ceityihkhqi a ming voei tlaih coengawh, ik-oeih a mi saikhqi ce Jesu a venawh kqawn pe uhy. Cekkhqi ce Bethsaida a mi ti khaw na ce ceh pyi khqi hy.
Atumwi atabwerera, anamuwuza Yesu zimene anachita. Kenaka Iye anawatenga napita kwa okha ku mudzi wa Betisaida.
11 Cehlai thlang kqeng ing sim nawh a hu awh hquut uhy. Cekkhqi ce ym nawh a mingmih a venawh Khawsa qam akawng ce kqawn pek khqi nawh, cekcoengawh thlak tlokhqi awm qoei sak khqi hy.
Koma gulu la anthu linadziwa ndipo anamutsatira. Iye anawalandira ndi kuyankhula nawo za ufumu wa Mulungu, ndi kuchiritsa amene amafuna machiritso.
12 Khaw a nung keeng awhtaw thlanghqa hlaihih tloek ce a venna law unawh, “vawhkaw thlang kqeng ve khaw ceng khaw cawi awh tyi khqi hlah, buh a an ingkaw ih a awmnaak sui na u seh, ningnih ce kqawng lakna nik awm uni,” tina uhy.
Chakumadzulo dzuwa litapita, khumi ndi awiriwo anabwera kwa Iye ndipo anati, “Uzani gulu la anthuli lichoke kuti apite ku midzi yotizungulira ndi madera a ku mudzi kuti akapeze chakudya ndi pogona, chifukwa kuno ndi kuthengo.”
13 Anih ing, “Nangmih ing ai kawi ce pe uh,” tinak khqi hy. A mingmih ing, thlang vezah aham buh a an am nik thlaih peek mantaw - phaihpi cun nga ingkaw nga pakkhih doeng ni a awm hy,” tina uhy.
Iye anayankha kuti, “Apatseni chakudya kuti adye.” Iwo anayankha kuti, “Ife tili ndi malofu a buledi asanu okha ndi nsomba ziwiri, pokhapokha titapita kukagula chakudya cha gulu la anthu onsewa.”
14 (Vawh thlang thongnga awm uhy.) Cehlai a hubatkhqi na ce, “Thlang hakip hakip awh ngawih sak hloep hloep uh,” tinak khqi hy.
(Pamenepo panali amuna pafupifupi 5,000). Koma Iye anati kwa ophunzira ake, “Akhazikeni pansi mʼmagulu a anthu pafupifupi makumi asanu.”
15 A hubatkhqi ing thlang kqeng ce ngawih sak khqi hy.
Ophunzira ake anachita zomwezo ndipo aliyense anakhala pansi.
16 Phaihpi cun nga ingkaw nga pakkhih ce lo nawh khan benna hang mang nawh, zeel awi ak kqawn coengawh ek hy. Thlang kqeng a haiawh toen peek aham a hubatkhqi venawh pehy.
Atatenga malofu a buledi asanu ndi nsomba ziwiri zija anayangʼana kumwamba, nayamika ndipo anazigawa. Kenaka anazipereka kwa ophunzira ake kuti azipereke kwa anthu.
17 A mingmih ing ai unawh a mi phyi coengawh ak ngen ce vawh hqa hlaihih na kawi uhy.
Onse anadya nakhuta, ndipo ophunzira ake anatolera madengu khumi ndi awiri odzaza ndi nyenyeswa zomwe zinatsala.
18 Hypoet taw Jesu ing amah doeng ak cykcah awh, a hubatkhqi ce a venawh awm usaw doet khqi hy, “Thlangkhqi ing kai ve u nu a mi ti?” tinak khqi hy.
Nthawi ina pamene Yesu amapemphera malo a yekha ali ndi ophunzira ake, Iye anawafunsa kuti, “Kodi anthu amati Ine ndine yani?”
19 Cekkhqi ing, “Thlang vang ing 'Baptisma ak pekung Johan,' ti unawh, thlang vang ing, 'Elijah,' ti uhy, thlang vang bai ingtaw, 'Syn awhkaw tawngha pynoet oet ak tho tlaih ni,' ti uhy,” tina uhy.
Iwo anayankha kuti, “Ena amati Yohane Mʼbatizi; ena amati Eliya; ndipo enanso amati mmodzi wa aneneri akalekale waukanso.”
20 Cawhtaw, ami venawh, “Nangmih ingtaw kai ve u nu nami ti?” tinak khqi hy. Piter ing, “Nang taw Khawsa a Khrih ni,” tina hy.
Iye anafunsa kuti, “Koma nanga inu mumati Ine ndine yani?” Petro anayankha kuti, “Mpulumutsi wolonjezedwa uja wa Mulungu.”
21 Ce akawng ce u aven awh awm amamik kqawn aham cekkhqi ce yn khqi hy.
Yesu anawachenjeza kwambiri kuti asawuze wina aliyense za izi.
22 Thlanghqing Capa ing khuikhanaak hu kawmsaw a hqamcakhqi, khawsoeih boeikhqi ingkaw anaa awi cawngpyikungkhqi ing hoet kawm uh, him kawm usaw am thum nyn awh tho tlaih kaw,” tinak khqi hy.
Ndipo Iye anati, “Mwana wa Munthu ayenera kuzunzika kwambiri ndi kukanidwa ndi akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo, Iye ayenera kuphedwa ndipo tsiku lachitatu adzauka kwa akufa.”
23 Cekcoengawh a mingmih boeih a venawh, “U ingawm ka hu awh bat ham a ngaih awhtaw, amah ingkaw amah ce hoet qu seitaw, myngawi na amah a thinglam ce kawh doena ka hu awh bat law seh.
Ndipo Iye anawuza onse kuti, “Ngati wina aliyense akufuna kutsata Ine, ayenera kudzikana yekha ndi kusenza mtanda wake tsiku ndi tsiku nʼkumanditsata Ine.
24 Ikawtih, u awm a hqingnaak hul ham ak ngaih ingtaw hlawng seitaw, u awm kai ak camawh a hqingnaak ak hlawng ingtaw a hqingnaak ce hul kaw.
Popeza aliyense amene akufuna kupulumutsa moyo wake adzawutaya, koma aliyense amene adzataya moyo wake chifukwa cha Ine adzawupulumutsa.
25 Thlang ing khawmdek pum ve ham mai seiawm a hqingnaak a hlawng awhtaw anih ham ikaw phu a taak?
Kodi chabwino ndi chiti kwa munthu, kupata zonse zapansi pano, koma ndi kutaya moyo wake kapena kudziwononga iye mwini?
26 U awm kai ingkaw kak awi ak chah pyi taw, Thlanghqing Capa ing amah a boeimangnaak, a Pa a boeimangnaak ingkaw khan ceityih ciimcaihkhqi a boeimangnaak ing ami law awh anih ce chah pyi lawt kaw.
Ngati wina aliyense achita nane manyazi ndi ndiponso mawu anga, Mwana wa Munthu adzachita naye manyazi pamene adzabwera mu ulemerero wake ndi mu ulemerero wa Atate ndi angelo oyera.
27 Awitak ka nik kqawn peek khqi, vawh ak dyi thlang vangkhqi ing Khawsa qam a huh hlan dy thihnaak amak tan hly awm uhy,” tinak khqi hy.
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti ena mwa inu amene mwayima pano simudzalawa imfa musanaone ufumu wa Mulungu.”
28 Ve ak awi ak kqawn coeng ak kqeet nyn awh, Jesu ing Piter, Johan ingkaw Jakob ce khy nawh tlang na cykcah aham van pyi khqi hy.
Patatha pafupifupi masiku asanu ndi atatu Yesu atanena izi, Iye anatenga Petro, Yohane ndi Yakobo ndi kukwera ku phiri kukapemphera.
29 Ak cykcah awh a hai ce thaw qu nawh, a hi ce khawkphlamyihna vang hy.
Pamene Iye ankapemphera, maonekedwe a nkhope yake, ndi zovala zake zinawala monyezimira kwambiri.
30 Cawh thlang pakkhih Mosi ingkaw Elijah,
Anthu awiri, Mose ndi Eliya,
31 ce boeimang soeih na dang nih nawh Jesu ingqawi awi pau uhy. Jesu a lam ceh Jerusalem awh a soep naak hly ce kqawn uhy.
anaonekera mu ulemerero opambana akuyankhulana ndi Yesu. Iwo amayankhulana za kuchoka kwake, kumene Iye anali pafupi kukakwaniritsa ku Yerusalemu.
32 Piter ingkaw a pyi qawi taw ip uhy, a ming hqyng law awhtaw a boeimangnaak ing a venawh thlang pakkhih ak dyi ce hu uhy.
Petro ndi anzake anali ndi tulo tambiri, koma atadzuka, iwo anaona ulemerero wake ndi anthu awiri atayima pamodzi ndi Iye.
33 Cawhkaw thlang qawi ing Jesu ceh taak hlah sih a ni ti awh, Piter ing, “Bawipa, vawh awmnaak ham hyn leek soeih hy, buk pakthum awh heen sih - pynoet ce nang aham seh, pynoet ce Mosi aham seitaw pynoet bai ce Elijah aham seh,” tina hy. (Kaw ak kqawn ti awm am sim hy.)
Pamene anthuwo ankamusiya Yesu, Petro anati kwa Iye, “Ambuye, ndi chabwino kwa ife kuti tikhale pano. Tiloleni kuti timange misasa itatu, umodzi wanu, umodzi wa Mose ndi umodzi wa Eliya.” (Iye sanadziwe chimene amayankhula).
34 Awi ak kqawn huili awh, myi than law nawh a mingmih ce zawl khqi khoep hy, myi ak khuina a mi lut awh kqih uhy.
Pamene Iye ankayankhula, mtambo unaonekera ndi kuwaphimba iwo, ndipo anachita mantha pamene mtambowo unawakuta.
35 Myi ak khuiawh kawng awi law nawh, “Vetaw ka Capa kak tyh ni; ak awi ngai pe uh,” tihy.
Mawu anachokera mu mtambomo nati, “Uyu ndi Mwana wanga amene ndamusankha; mumvereni Iye.”
36 Cawhkaw awi ce a sit coengawh, Jesu amah doeng caa ce hu uhy. A hubatkhqi ing cawhkaw ik-oeih ce khoem dym unawh a mi huh ik-oeih ce a u a venawh awm ap kqawn pe uhy.
Atamveka mawuwa, anaona kuti Yesu anali yekha. Ophunzirawo anazisunga izi mwa iwo okha ndipo sanawuze wina aliyense pa nthawiyi za zomwe iwo anaziona.
37 A khawngawi awh tlang nakawng a mi kqum lawawh, thlang khawzah ing amih ce do uhy.
Mmawa mwake, akutsika ku phiri, anthu ambiri anakumana naye.
38 Thlang kqeng ak khuiawh kaw thlang pynoet ing, “Cawngpyi kung, ka capa na toek law ham ni ngaih na nyng, ka capa ka taak dyn na awm nawh.
Munthu wina mʼgulu la anthulo anayitana kuti, “Aphunzitsi, ndikupemphani kuti muone mwana wangayu, pakuti ndi mmodzi yekhayu.
39 Ngai lah, qaai ing tu nawh, khy hoeih hoeih hy, a cimtui ang tlaak doena dek awh tluuk sak nawh a phep qee coengawh ceh taak hoeih hoeih hy.
Chiwanda chikamugwira amafuwula mwadzidzidzi; chimamugwedeza kolimba mpaka kutuluka thovu kukamwa. Sichimusiya ndipo chikumuwononga.
40 Na hubatkhqi venawh hqek pek a hamna thoeh hlai nyng, am hqek thai uhy,” tina hy.
Ine ndinapempha ophunzira anu kuti achitulutse, koma alephera.”
41 Jesu ing, “Aw cangnaak amak takhqi ingkaw amthin amak cak cadil tloek, iqyt nu ka ni awm pyi khqi nawh ka ning yh pyi khqi kaw? Na capa ce vena law pyi lah,” tina hy.
Yesu anayankha kuti, “Haa! Anthu osakhulupirira ndi mʼbado wokhota. Kodi Ine ndidzakhala nanu nthawi yayitali yotani ndi kukupirirani? Bweretsa mwana wako kuno.”
42 Naasen ce a law pyi hui awh qaai ing dek awh tluuk sak nawh ak tlo na phep qee hy. Cehlai Jesu ing qaai ce zyi nawh, naasen ce a qoei sak coengawh a pa a venawh pe tlaih hy.
Ngakhale pamene mnyamata amabwera kwa Yesu, chiwandacho chinamugwetsa pansi ndi kumugwedeza. Koma Yesu anadzudzula mzimu woyipawo nachiritsa mwa mnyamatayo ndi kumuperekanso kwa abambo ake.
43 Thlang boeih ing Khawsa a boeimangnaak ce kawpoek na kyi sak uhy. Jesu a them saithainaak awh a mik kawpoek a kyi hui awh, Jesu ing a hubatkhqi venawh,
Ndipo iwo onse anadabwa ndi ukulu wa Mulungu. Aliyense akudabwa ndi zimene Yesu anachita, Iyeyo anati kwa ophunzira ake,
44 Awi kqawn law vang nyng, ak nep na ngai lah uh: Thlanghqing Capa ve thlang a kut awh tu sak kawm uh,” tinak khqi hy.
“Tamvetsetsani zimene ndikufuna kukuwuzani: Mwana wa Munthu akupita kukaperekedwa mʼmanja mwa anthu.”
45 Cehlai ak kqawn ngaihnaak ce am zaksim pe uhy. A mingmih ang zaksim kawi na a ma awm a dawngawh, am khoem thai uhy, amah ce doet aham awm kqih koek uhy.
Koma iwo sanazindikire zimene amatanthauza. Izi zinawadabwitsa kotero sanathe kuzimvetsa ndipo anaopa kumufunsa.
46 A mingmih ak khuiawh u nu ak bau soeih na ak awm kaw, tinawh a hubatkhqi ak khuiawh oelh qu uhy.
Mkangano unayambika pakati pa ophunzira wa kuti wamkulu koposa akanakhala ndani mwa iwo.
47 Jesu ing a mingmih ak kawpoek ce a sim a dawngawh naasen ce lo nawh a venawh dyih sak hy.
Yesu podziwa maganizo awo, anatenga kamwana nakayimika pambali pake.
48 Cekcoengawh a mingmih a venawh, “U awm vawhkaw naasen ve kai ang ming ing ak ym taw kai a nik tyikung ce ak ym na awm hy. Nangmih boeih ak khuiawh ak zawi soeih na ak awm ce ak bau soeih na awm hy,” tinak khqi hy.
Ndipo Iye anawawuza kuti, “Aliyense wolandira bwino kamwana aka mʼdzina langa, ndiye kuti akulandiranso bwino Ine; ndipo aliyense wolandira bwino Ine, ndiye kuti akulandiranso bwino amene anandituma Ine. Pakuti amene ndi wamngʼono pakati panu, ndiye amene ali wamkulu koposa.”
49 Johan ing, “Bawipa, thlang pynoet ngawh nang ang ming ing qaai a hqek ce hu u nyngsaw kham pe u nyng, kaimih ak khuiawh kaw thlang na a ma awm a dawngawh,” tina uhy.
Yohane anati, “Ambuye, ife tinaona munthu akutulutsa ziwanda mʼdzina lanu ndipo tinayesa kumuletsa, chifukwa iyeyo si mmodzi wa ife.”
50 Jesu ing, “Koeh kham pe uh, nangmih a ma nik oelh thlang cetaw nangmih ben thlang ni,” tinak khqi hy.
Yesu anati, “Wosamuletsa, pakuti amene satsutsana nanu ali mbali yanu.”
51 Khawk khan na amah ceh pyi aham a tym a zoe law awh, Jesu taw Jerusalem na cet hy.
Nthawi itayandikira yoti Iye atengedwe kupita kumwamba, Yesu anatsimikiza zopita ku Yerusalemu,
52 Laipaikhqi ce haina tyi hy, ik-oeihkhqi qoek a bah aham a mingmih ce Samari khawk khui pynoet awh cet uhy;
ndipo anatuma nthumwi kuti zitsogole. Iwo anapita mʼmudzi wa Asamariya kuti akonzekere kumulandira,
53 cehlai Jerusalem khaw na ceh phaat aham ang cai a dawngawh cawhkaw a mik awm thlangkhqi ing anih ce am do uhy.
koma anthu kumeneko sanamulandire chifukwa Iye ankapita ku Yerusalemu.
54 A hubat qawi Jakob ingkaw Johan ing cemyihna a mi awm ce a ni huh awh, “Bawipa, a mingmih ve hqe aham khawk khan nakaw mai (Elijah ing ak khy myihna) khy sih aw?” tina hy nih.
Ophunzira awa, Yohane ndi Yakobo ataona zimenezi, anafunsa kuti, “Ambuye, kodi mukufuna ife tiyitane moto kuchokera kumwamba kuti uwawononge?”
55 Cehlai Jesu ing cekqawi ce hawi sih nawh zyi qawi hy. (Kawmih ak kawpoek nu nani taak tice am sim hy nik ti).
Koma Yesu anatembenuka ndi kuwadzudzula,
56 (Thlanghqing Capa ve thlang a hqingnaak hqe aham am law nawh, hqingnaak hul aham nani a law, tina qawi hy.) Cekcoengawh khawk chang na cet pahoei uhy.
ndipo iwo anapita ku mudzi wina.
57 Lam na a mi ceh awh thlang pynoet ing a venawh, “Na cehnaak a hoei awh bat lawt vang nyng,” tina hy.
Pamene iwo ankayenda mu msewu, munthu wina anati kwa Iye, “Inu ndikutsatirani kulikonse kumene mudzapita.”
58 Jesu ing a venawh, “Ngentangkhqi ing a mik kawk ta unawh phakhqi ingawm a ming bu ta uhy, cehlai Thlanghqing Capa ingtaw a lu a tloengnaak hun kangna awm am ta hy,” tina hy.
Yesu anayankha kuti, “Nkhandwe zili ndi mapanga ake, mbalame zili ndi zisa zake, koma Mwana wa Munthu alibe malo wogonekapo mutu wake.”
59 Thlak chang a venawh, “Ka hu awh bat law,” tina hy. Cehlai cawhkaw thlang ing, “Ka pa a qawk khoem cang vang,” tina hy.
Iye anati kwa wina, “Nditsate Ine.” Koma munthuyo anayankha kuti, “Ambuye, choyamba loleni ndipite kuti ndikayike maliro a abambo anga.”
60 Cehlai Jesu ing a venawh, “Thlak thi cetaw ak thi khqi ing khoem ngoen seh, nang taw cet nawh Khawsa ram ce kqawn lah,” tina hy.
Yesu anati kwa iye, “Aleke akufa ayikane akufa okhaokha, koma iwe pita ukalalikire ufumu wa Mulungu.”
61 Thlak chang pynoet bai ing, “Na hu awh bat bit kawng nyng, cehlai ka cakaw paqengkhqi phih a qaa cang vang nyng,” tina hy.
Koma winanso anati, “Ine ndidzakutsatani Ambuye; koma choyamba ndiloleni ndibwerere kuti ndikatsanzikane nalo banja langa.”
62 Jesu ing a venawh, “U awm laikawk thawlnaak awh a kut ta nawh hu benna ak mang taw Khawsa qam thlang nih am tlaak hy,” tina hy.
Yesu anayankha kuti, “Munthu amene akulima ndi khasu lokokedwa nʼkumayangʼana mʼmbuyo, si woyenera kugwira ntchito mu ufumu wa Mulungu.”

< Luke 9 >