< Zekariya 6 >

1 Ndinayangʼananso ndipo taonani ndinaona magaleta anayi akutuluka pakati pa mapiri awiri, mapiri amkuwa.
Potem odwróciłem się, podniosłem swoje oczy i spojrzałem, a oto cztery rydwany wychodziły spomiędzy dwóch gór, a [te] góry [były] z miedzi.
2 Galeta loyamba limakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiwiri ndi akavalo akuda,
Przy pierwszym rydwanie [były] konie rude, przy drugim rydwanie – konie kare;
3 lachitatu ndi akavalo oyera, ndipo lachinayi ndi akavalo otuwa a mawanga ofiirira, onsewa anali akavalo amphamvu kwambiri.
Przy trzecim rydwanie – konie białe, a przy czwartym rydwanie [były] konie pstrokate i gniade.
4 Ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane uja kuti, “Kodi mbuye wanga chimenechi nʼchiyani?”
Wtedy zapytałem Anioła, który rozmawiał ze mną: Co to [jest], mój Panie?
5 Mngeloyo anandiyankha kuti, “Imeneyi ndi mizimu inayi yakumwamba, imene ikuchokera pamaso pa Ambuye wa dziko lonse.
I Anioł odpowiedział mi: To [są] cztery duchy nieba, wyruszają [one] z [miejsca], gdzie stały przed Panem całej ziemi.
6 Galeta la akavalo akuda likupita ku dziko la kumpoto, galeta la akavalo oyera likutsatira, ndipo galeta la akavalo amawanga ofiirira likupita ku dziko la kummwera.”
Zaprzężone konie kare wyruszają do ziemi północnej, białe wyruszają za nimi, pstrokate zaś wyruszają do ziemi południowej.
7 Pamene akavalo amphamvuwa ankapita, anali ndi changu chofuna kuyendera dziko lapansi. Ndipo iye anati, “Pitani, kayendereni dziko lapansi!”
A te gniade [konie] wyruszyły, rwały się do biegu, aby obejść ziemię. Wtedy powiedział: Idźcie i obejdźcie ziemię! I obeszły ziemię.
8 Pamenepo anandiyitana, “Taona, akavalo amene apita ku dziko la kumpoto apumulitsa Mzimu wanga kumeneko.”
Potem zawołał mnie i powiedział: Oto te, które wyruszyły do ziemi północnej, uspokoiły mojego ducha w ziemi północnej.
9 Yehova anayankhula nane kuti,
I doszło do mnie słowo PANA mówiące:
10 “Landira mphatso kuchokera kwa anthu amene abwera ku ukapolo, Helidai, Tobiya ndi Yedaya, amene achokera ku Babuloni. Tsiku lomwelo pita ku nyumba ya Yosiya mwana wa Zefaniya.
Weź [dary] od tych, co byli w niewoli: od Cheldaja, od Tobiasza i od Jedajasza, którzy przybyli z Babilonu, i przyjdź w tym samym dniu, i wejdź do domu Jozjasza, syna Sofoniasza;
11 Tenga siliva ndi golide upange chipewa chaufumu, ndipo uchiyike pamutu pa mkulu wa ansembe, Yoswa mwana wa Yehozadaki.
Weź srebro i złoto, zrób korony i włóż je na głowę Jozuego, syna Josadaka, najwyższego kapłana.
12 Muwuze kuti zimene akunena Yehova Wamphamvuzonse ndi izi: ‘Taonani, munthu wotchedwa Nthambi ndi ameneyu, ndipo adzaphuka pomwe alipo ndi kumanga Nyumba ya Yehova.
I powiedz do niego: Tak mówi PAN zastępów: Oto mąż, którego imię brzmi Latorośl; on wyrośnie ze swego miejsca i zbuduje świątynię PANA.
13 Ndiye amene adzamange Nyumba ya Yehova, adzalandira ulemerero waufumu ndipo adzalamulira pa mpando wake waufumu. Adzakhalanso wansembe pa mpando wake waufumu. Ndipo padzakhala mtendere.’
On zbuduje świątynię PANA, będzie obdarzony chwałą, zasiądzie na swoim tronie i będzie panować na nim, i będzie on kapłanem na swoim tronie; i rada pokoju będzie między nimi oboma.
14 Chipewa cha ufumucho adzachipereka kwa Helemu, Tobiya, Yedaya, ndi kwa Heni mwana wa Zefaniya, kuti chikhale chikumbutso mʼNyumba ya Yehova.
A [te] korony będą dla Chelema, Tobiasza, Jedajasza i Chena, syna Sofoniasza, jako pamiątka w świątyni PANA.
15 Anthu okhala kutali adzabwera kudzathandiza kumanga Nyumba ya Yehova, ndipo iwe udzadziwa kuti Yehova Wamphamvuzonse wandituma kwa iwe. Zimenezi zidzachitika ngati mudzamvera mwachangu Yehova Mulungu wanu.”
Przyjdą ludzie z dalekich stron i będą budować świątynię PANA, i poznacie, że PAN zastępów posłał mnie do was. A to się stanie, jeśli pilnie będziecie słuchać głosu PANA, swego Boga.

< Zekariya 6 >