< Aroma 2 >

1 Choncho, iwe amene umaweruza munthu wina, ulibe pokanira pakuti nthawi iliyonse pamene uweruza wina ukudzitsutsa wekha chifukwa iwe amene umaweruzawe umachitanso zinthu zomwezo.
Kwa nneyo, monaga nkwiitemba kwaukumula bhananji, nkakola sha kwiibheleketela. Nnakwiukumula mmayene, pabha numbe mmwe inkutenda yoyo peyo.
2 Tsopano ife tikudziwa kuti chiweruzo cha Mulungu, chotsutsa amene amachita zinthu zotere, nʼchokhazikika pa choonadi.
Na uwe tumumanyi kuti ukumu ja a Nnungu ni ja kweli, kwa bhatendanga indu malinga yeneyo.
3 Kodi ukuganiza kuti udzathawa chiweruzo cha Mulungu iwe munthu wamba, pamene uweruza ena, iwe ndi kumachitanso zomwezo?
Ikabheje mmwe anamundupe, nkwaukumulanga bhaatendanga indu malinga yeneyo, akuno mmayene nnitenda yoyo. Bhuli, punkuganishiya kuti shimwiembuye na ukumu ja a Nnungu?
4 Kodi kapena ukupeputsa kukoma mtima kwa Mulungu, kuleza mtima kwake ndi kupirira kwake? Kodi sukuzindikira kuti kukoma mtima kwakeko, nʼkofuna kuti iweyo ulape machimo ako?
Eu nnakuunyegaya uguja gwa a Nnungu, na kwiitimalika na kwiipililila kwabho, gwangali kumumanya kuti uguja gwabho unakunnongoya mwiipete?
5 Koma pakuti ndiwe wosamvera ndi wa mtima wosafuna kulapa, ukudzisungira chilango pa tsiku la mkwiyo wa Mulungu, pamene chiweruzo cholungama cha Mulungu chidzaonetsedwa.
Ikabheje kwa ligongo lya mitau na nonopa kwa ntima gwenu, nnakwiigosheya nnjimwa, lyubha lya nnjimwa ja a Nnungu, na ukumu jabho ja aki.
6 Mulungu adzabwezera aliyense molingana ndi ntchito zake.
Pabha lyene lyubhalyo, a Nnungu bhapinga kwiya kwaalipanga bhandunji bhowe malinga ibhatendangaga.
7 Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
Bhene bhaatendanga ya uguja gwangali kutotoshela, bhanaloleyanga kukopoka kwa a Nnungu, ukonjelo na ishimika na gumi gwangali angabhanika, na shibhapegwanje gumi gwa pitipiti. (aiōnios g166)
8 Koma Mulungu adzakhuthulira mkwiyo ndi ukali wake pa amene amachita zofuna zawo ndi kukana choonadi nʼkumatsatira zoyipa.
Ikabheje bhananji bhaakwetelanga na bhaakananga indu ya aki bhala, nikagulila yangali ya mmbone, shibhajibhonanje nnjimwa ja a Nnungu.
9 Masautso ndi zowawa zidzagwera munthu aliyense amene amachita zonyansa, kuyambira Myuda kenaka anthu a mitundu ina.
Mboteko na shilaje shiimpate mundu jojowe atenda yangali ya mmbone, kutandubhila Bhayaudi na Bhagiliki.
10 Koma ulemerero, ulemu ndi mtendere zidzakhala kwa aliyense amene amachita zabwino, kuyambira Myuda kenaka anthu a mitundu ina.
Ikabheje, ukonjelo na ishima na ulele, shibhapegwanje bhandunji bhaatendanga indu ya aki bhala, kutandubhila Bhayaudi na Bhagiliki.
11 Pajatu Mulungu alibe tsankho.
Pabha a Nnungu bhangali luagu.
12 Onse amene amachimwa osadziwa Malamulo, adzawonongeka ngakhale kuti sadziwa Malamulowo. Ndipo onse amene amachimwa akudziwa Malamulo adzaweruzidwa potsata Malamulowo.
Bhowe bhatendilenje yambi gwangali kujimanya shalia ja a Musha, shibhapotekwanje nngabha kwa ligongo lya shalia, na bhowe bhatendilenje yambi akuno bhalikujimanyanga shalia ja a Musha, shibhaukumulwanje kwa tolelela shalia ja a Musha pejo.
13 Pakuti si amene amangomva Malamulo amene amakhala wolungama pamaso pa Mulungu, koma ndi okhawo amene amachita zili mʼMalamulomo amene adzatchedwa olungama.
Na nngabha bhakujipilikananga shalia ni bhakwete aki kwa a Nnungu, ikabheje bhaakundanga shalia bhala, nibhaakolanga aki.
14 Ndithu, pamene a mitundu ina, amene alibe Malamulo, koma mwachikhalidwe chawo amachita zimene zili mʼMalamulo, iwowo ndi Malamulo pa iwo okha, ngakhale kuti alibe Malamulowo.
Bhandunji bha ilambo ina bhangalinginji shalia, pubhaatendanga indu ya shalia kwa ng'aniyo ya muntima gwabhonji bhanabhanganga bhandunji bha shalia, nkali bhanakolanje shalia.
15 Ntchito zawo zimaonetsa kuti Malamulowo alembedwa mʼmitima mwawo. Chikumbumtima chawonso chimawachitira umboni pakuti maganizo awo amawatsutsa kapena kuwavomereza.
Bhanalanguyanga malajilo ga shalia jijandishwe mmitima jabhonji, ng'aniyo yabhonji ilikwakong'ondelanga na ilikwalonganga na guna ilikwaabheleketelanga ashaayenenji.
16 Izi zidzachitika pa tsiku limene Mulungu adzaweruza zinsinsi za anthu kudzera mwa Yesu Khristu, monga momwe Uthenga wanga Wabwino unenera.
Yeneyo ni ipinga koposhela, lyubha lya ukumu ja a Nnungu, pushibhaukumule indu ya nng'iyo kupitila a Yeshu Kilishitu, malinga shijikuti taya Ngani ja Mmbone jingulunguyaji.
17 Koma iweyo, amene umadzitcha kuti ndiwe Myuda, umadalira Malamulo, ndipo umanyadira ubale wako ndi Mulungu,
Pabha mmwe nkwiishema mmayene Mmayaudi, nnakulupalila shalia, na nnakwiiniya kuti bha a Nnungu.
18 ngati umadziwa chifuniro chake, ndi kudziwa zoyenera kuchita chifukwa unaphunzitsidwa ndi Malamulo;
Mmwe nnikuimanya ibhapinga a Nnungu, na kunda indu ya mmbone, pabha nshijiganywa na shalia.
19 ngati umadziwadi kuti ndiwe mtsogoleri wa osaona, nyale yowunikira amene ali mu mdima,
Mmwe punkwiiganishiya kuti mmayene akalongolele bha ashinangalole, na kabhili mmwe shilangaya sha bhandu bhalinginji nnubhindu,
20 mlangizi wa anthu opusa, mphunzitsi wa makanda, chifukwa umadziwa kuti mʼMalamulo uli nayo nzeru yonse ndi choonadi,
mmajiganya bha mabhelu na bhana bhashoko, pabha kwa shalia, mwiimanyi ukoto indu ya lumanyio na kweli.
21 tsono, iwe amene umaphunzitsa ena, sudziphunzitsa wekha kodi? Kodi iwe amene umalalikira kuti anthu asabe, umabanso?
Bhai mmwe nkwaajiganyanga bhananji, kwa nndi nkakwiijiganya mmayene? Mmwe nkwaalimbiyanga bhananji bhanajibhanje, akuno mmayene nnijibha.
22 Kodi iwe amene umanena kuti anthu asachite chigololo, umachitanso chigololo? Kodi iwe amene umanyasidwa ndi mafano, umalandanso za mʼnyumba zopembedzera mafanowo?
Mmwe nkulunguya kuti, “Mundu analabhelabhe” akuno mmayene nnilabhalabha. Inakunshima yanamu ya ashinnungu, mbena nnijibha indu ya mmajumba gabhonji.
23 Kodi iwe amene umadzitama ndi Malamulo, umamuchititsa manyazi Mulungu posamvera Malamulowo?
Nnikwiiniya kuti nkwete shalia ja a Nnungu, nkakumumanya kuti kuleka kamula shalia, nnakwanyegaya a Nnungu?
24 Monga kwalembedwa, “Dzina la Mulungu likuchitidwa chipongwe pakati pa a mitundu ina chifukwa cha inu.”
Malinga Majandiko ga Ukonjelo shigalugula, “Bhandunji bha ilambo ina, bhashikulitukananga lina lya a Nnungu, kwa ligongo lyenunji.”
25 Mdulidwe umakhala ndi phindu ngati usunga Malamulo, koma ngati sumvera Malamulo, iweyo umakhala ngati kuti sunachite mdulidwe.
Pabha kujaluka kunapwaa punkukamulila shalia ja a Musha, ikabheje nkakamulile shalia ja a Musha, shimme mbuti mmalenje.
26 Ngati amene sanachite mdulidwe achita zomwe zili mʼMalamulo, kodi sadzatengedwa ngati ochita mdulidwe?
Bhai monaga mundu jwangajaluka anakamulila shalia ja a Musha, bhuli na ulenje gwakwe akaganishiywa kuti ajalwishe?
27 Munthu amene sanachite mdulidwe mʼthupi koma amamvera Malamulo adzakutsutsa iwe wosamvera Malamulowe, ngakhale kuti uli nawo Malamulo olembedwawo.
Na jwene jwa nngabha munkubho gwa jaluka, ikabhe anakamulila shalia ja a Musha, bhuli akanng'ukumula mmwe nni munkubho gwa jaluka, na akuno nkakamulila shalia ja a Musha?
28 Myuda weniweni si amene angooneka ngati Myuda pamaso pa anthu, ndipo mdulidwe weniweni si umene umangochitika mʼthupi pamaso pa anthu.
Pabha jwenejo, nngabha Nnyaudi kwa bhoneka palanga, na kujaluka nngabha kwa nshiilupe.
29 Ayi, Myuda weniweni ndi amene ali Myuda mu mtima mwake, ndipo mdulidwe weniweni ndi wa mtima, wochitika ndi Mzimu, osati ndi malamulo olembedwa. Woyamikira munthu wotere ndi Mulungu, osati anthu ayi.
Ikabhe jwenejo ni Nnyaudi, ali Nnyaudi jwa nkati, na kujaluka kwakwe kwa muntima kwa Mbumu jwa Ukonjelo, nngabha kwa mmajandiko ga shalia. Mundu jwa nneyo, kuiniywa kwakwe nngabha kubhandunji ikabhe kwa a Nnungu.

< Aroma 2 >