< Masalimo 80 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Salimo la Asafu. Tcherani khutu Inu mʼbusa wa Israeli, Inu amene mumatsogolera Yosefe monga nkhosa; Inu amene mumakhala pa mpando waufumu pakati pa akerubi, walani
Asafa dziesma dziedātāju vadonim, pēc: „Lilijas ir liecība“. Israēla gans, klausies, Tu, kas Jāzepu vadi kā avis; Tu, kas sēdi pār ķerubiem, parādies ar spožumu!
2 kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase. Utsani mphamvu yanu; bwerani ndi kutipulumutsa.
Uzmodini savu varu priekš Efraīma, Benjamina un Manasus, un nāc mūs pestīt.
3 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu; nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
Ak Dievs, atgriez mūs un liec Savam vaigam spīdēt, tad tapsim pestīti.
4 Inu Mulungu Wamphamvuzonse, mpaka liti mkwiyo wanu udzanyeka kutsutsana ndi mapemphero a anthu anu?
Kungs, Dievs Cebaot, cik ilgi Tava dusmība kūpēs pie Tavu ļaužu lūgšanas?
5 Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale.
Tu tos ēdini ar asaru maizi un tos dzirdini ar lielu mēru asaru.
6 Mwachititsa kuti tikhale gwero la mikangano pakati pa anansi athu, ndipo adani athu akutinyoza.
Tu mūs esi licis par ķildu mūsu kaimiņiem, un mūsu ienaidnieki mūs apmēda.
7 Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse, nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
Dievs Cebaot, atgriezi mūs un liec Savam vaigam spīdēt, tad tapsim pestīti.
8 Munatulutsa mpesa kuchoka ku Igupto; munathamangitsa anthu a mitundu ina ndi kuwudzala mpesawo.
Vienu vīna koku Tu esi atvedis no Ēģiptes, pagānus Tu esi izdzinis un to dēstījis.
9 Munawulimira munda wamphesawo, ndipo unamera ndi kudzaza dziko.
Vietu priekš viņa Tu esi sataisījis un viņam licis iesakņoties, ka viņš zemi piepildījis.
10 Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yamphamvu ndi nthambi zake.
Kalni ar viņa ēnu ir apklāti un Dieva ciedru koki ar viņa zariem.
11 Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja, mphukira zake mpaka ku mtsinje.
Viņš izplēta savus zarus līdz pat jūrai un savus jaunos zariņus līdz tai lielai upei.
12 Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake kuti onse amene akudutsa athyole mphesa zake?
Kāpēc tad Tu viņa sētu esi salauzījis, ka visi, kas iet garām, viņu plosa?
13 Nguluwe zochokera mʼnkhalango zikuwononga ndipo zirombo za mthengo zimawudya.
Mežacūka viņu izrakusi, un lauka zvēri viņu noēduši.
14 Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse! Yangʼanani pansi muli kumwambako ndipo muone! Uyangʼanireni mpesa umenewu,
Dievs Cebaot, atgriezies jel, skaties no debesīm un redzi un uzlūko šo vīna koku,
15 muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala, mwana amene inu munamukuza nokha.
To stādu, ko Tava labā roka dēstījusi, un To Dēlu, ko Tu Sev esi izredzējis!
16 Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto; pakudzudzula kwanu anthu anu awonongeka.
Viņš ar uguni ir sadedzināts un izcirsts; no Tava vaiga rāšanas tie iet bojā.
17 Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja, mwana wa munthu amene mwalera nokha.
Tava roka lai ir pār to vīru pie Tavas labās rokas, pār To Cilvēka Dēlu, ko Tu Sev esi izredzējis.
18 Ndipo ife sitidzatembenukira kumbali kuchoka kwa Inu; titsitsimutseni ndipo tidzayitana pa dzina lanu.
Tad mēs neatkāpsimies no Tevis; uzturi mūs dzīvus, tad mēs Tavu vārdu piesauksim.
19 Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
Ak Kungs, Dievs Cebaot, atgriez mūs, liec Savam vaigam spīdēt, tad tapsim pestīti.

< Masalimo 80 >