< Masalimo 8 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
Aw Bawipa, kaimih a Bawipa, khawmdek khan boeih awh na boeimangnaak be soeih mah hy! Na boeimangnaak ce khankhqik khanawh ta hyk ti.
2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
Qaalkhqi ingkaw lu ak lokhqi sit sak aham ingkaw na qaalkhqi awh, naasenkhqi ingkaw naacakhqi a hui awhkawng kyihcahnaak ce caksak hyk ti.
3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
Khan nakaw ak awm na kut sai pihla ingkaw aihchikhqi, amah a awmnaak hun boeih awh na taakkhqi ce kak poek awh,
4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
Thlanghqing ve ikawpna a awm aih awh, na qeetnaak khaak nawh, thlanghqing capa awm na kqip loet hy voei?
5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
Anih ce khan khaw na ak awm anglakawh ak nem bet na sai nawh boeimang thangleeknaak ing sing hyk ti.
6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
Na kut saikhqi boeih ukkung na ta nawh, a khawk kaiawh ik-oeihkhqi boeih ce taak pe hyk ti.
7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
Tui a nga ingkaw kqawng nakaw qamsa boeih,
8 mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
khawnghi nakaw chukphakhqi, tuih khui nakaw lum a nga boeih ingkaw tuicunli awhkaw ak cawlhtat boeih ce a khawk kaiawh taak pe hyk ti.
9 Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!
Aw Bawipa, kaimih a Bawipa, khawmdek pum awh nang ming qypawm soeih hy.

< Masalimo 8 >