< Masalimo 76 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu. Mulungu amadziwika mu Yuda; dzina lake ndi lotchuka mu Israeli.
Judah qam awh Khawsa ce sim unawh; Israel qam awh ang ming bau soeih hy.
2 Tenti yake ili mu Salemu, malo ake okhalamo mu Ziyoni.
Salem awh a hibai im ce awm nawh, Zion awh awmnaak hun ce awm hy.
3 Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka, zishango ndi malupanga, zida zankhondo. (Sela)
Amah cawh lakhqi, phuhqa ingkaw zawzikhqi, qaal tuknaak liva sapangkhqi ce hqe pehy.
4 Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.
Nang taw vangnaak ing na qym awm soeih hy, chukpha ing ak be tlang anglakawh na qyp awm khqoet hy.
5 Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma, Iwowo amagona tulo tawo totsiriza; palibe mmodzi wamphamvu amene angatukule manja ake.
Am thin ak awm thlangkhqi aming zaih awh muk nawh, ih a dytnaak ing ip poe uhy; qaal tuk tha ak awmkhqi pynoet ca ingawm a kut am phyl hqa uhy.
6 Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo, kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi.
Aw Jacob a Khawsa, nang ing na phep dawngawh meqang ingkaw meqang sen awm zaih hqoeng hy.
7 Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa. Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?
Nang doeng ni kqih aham na awm. Nak kaw a so awh ce na haiawh a u nu ak dyi thai kaw?
8 Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo, ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete,
Khan nakawng awi dengnaak ce kqawn tiksaw, qam ing ak kqih aih awh awm dym hy.
9 pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze, kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko. (Sela)
Aw Khawsa, awi deng aham na hang dyih awh ce, qam khui awhkaw khawdeng thlangkhqi hul aham cawh nang dyih awh.
10 Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu.
Thlanghqingkhqik khan awh nak kawsonaak ing nam kyihcahnaak ce hawlaw nawh, nak kawsonaak nak qoeng thoemkhqi ing thoeihcam qu hyk ti.
11 Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse; anthu onse omuzungulira abweretse mphatso kwa Iye amene ayenera kuopedwa.
Bawipa na Khawsa venawh awi na kam ce soepkep boeih ing kqih aham ak awm thlang a venawh laksawng ce khyn law pe u seh.
12 Iye amaswa mzimu wa olamulira; amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi.
Anih ing ukkungkhqi ang myihla hqe pehy; Khawmdek awhkaw sangpahrang khqi ing anih ce kqih uhy.

< Masalimo 76 >