< Masalimo 70 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
Aw Khawsa, kai hul aham nang hqi tawn sak lah; Aw Bawipa kai hul aham ang tawnna law lah.
2 Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
Kai him aham anik tengkhqi ce chahqai phyi u seitaw ngai hangtum na awm u seh nyng; kai plawci sak aham ak ngaihkhqi boeih kawboet doena awm u seh.
3 Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
Ka venawh, Aha! Ak tikhqi ce chah doena hlat tlaih u seh.
4 Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
Cehlai nang anik sui thlangkhqi taw zeel u seitaw zoeksang na awm seh nyng!” ti u seh.
5 Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.
Cehlai, kai taw khawdeng ingkaw ak voethlauh thlang na awm nyng; Aw Khawsa, ka venawh ang tawnna law lah. Nang taw kai anik hulkung ingkaw kai anik hulkung na awm hyk ti; Aw Bawipa, koeh di lah.

< Masalimo 70 >