< Masalimo 64 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga; tetezani moyo wanga ku chiopsezo cha mdani.
Aw Khawsa, kang ngaih kyinaak awi ka sa awh ve, ngai law lah; kqih awm qaal anglakawhkawng ka hqingnaak ve hlip chung lah.
2 Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa, ku gulu laphokoso la anthu ochita zoyipa.
Thlakchekhqi a tengnaak awhkawng ni thuh nawhtaw, khawboek chekhqi awipungkhqi ven awhkawng ni thuh lah.
3 Iwo amanola malilime awo ngati malupanga, amaponya mawu awo olasa ngati mivi.
Amim laikhqi ce zawzi amyihna taak pat la unawh, ak chy ak ngan la amyihna amik awi ing thlang hyt uhy.
4 Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa; amamulasa modzidzimutsa ndi mopanda mantha.
Ak awm dym thlang ce mah unawh kaap uhy, kqihnaak taak kaana, anih ce kaap zap uhy.
5 Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa, amayankhula zobisa misampha yawo; ndipo amati, “Adzayiona ndani?”
Ak che ik-oeih poeknaak awh tha pe qu unawh, ang hypna ami dun thang akawng ce kqawn uhy; “U ing a huh tang kaw?” ti uhy.
6 Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati, “Takonza ndondomeko yabwino kwambiri!” Ndithu maganizo ndi mtima wa munthu ndi zachinyengo.
Amak thym ik-oeih awh za qu unawh, “sai ham hly nik poek hloem lauh hy aa!” ti uhy. Thlanghqing ak kawlung ve qaai kqawn thai pai hy.
7 Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi; mwadzidzidzi adzakanthidwa.
Cehlai, cekkhqi ce Khawsa ing la ing kaap kaw; kawlkalh awh cekkhqi ce kaap hawh kaw.
8 Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa ndi kuwasandutsa bwinja; onse amene adzawaona adzagwedeza mitu yawo mowanyoza.
A mimah am lai ha ce hawi pek khqi khup phlet kawmsaw plawci sak khqi kaw; ak hukhqi boeih ing thekhanaak ing a lu thlek sih kawm uh.
9 Anthu onse adzachita mantha; adzalengeza ntchito za Mulungu ndi kulingalira mozama zomwe Iye wazichita.
Thlanghqing boeih ing kqih hawh kawm uh; Khawsa bibi ce kqawn kawm usaw a ik-oeih sai ce poek kawm uh.
10 Lolani wolungama akondwere mwa Yehova ndi kubisala mwa Iye, owongoka mtima onse atamande Iye!
Thlakdyng ingtaw Khawsa awh zeel seitaw amah awh ce thuk seh; kawlung ak dyngkhqi boeih ing amah kyihcah seh!

< Masalimo 64 >