< Masalimo 5 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe zoyimbira za zitoliro. Salimo la Davide. Tcherani khutu ku mawu anga, Inu Yehova, ganizirani za kusisima kwanga
Aw Bawipa kak awi ce ning ngai pe nawh, kak khy awi ce poek lah.
2 Mverani kulira kwanga kofuna thandizo, Mfumu yanga ndi Mulungu wanga, pakuti kwa Inu, ine ndikupemphera.
Ka sangpahrang ingkaw ka Khawsa kak khy awi ce ngai lah; na venawh nik cykcah law nyng.
3 Mmawa, Yehova mumamva mawu anga; Mmawa ndimayala zopempha zanga pamaso panu ndi kudikira mwachiyembekezo.
Bawipa, mymcang awh kak awi ve ngai tiksaw; mymcang awh na haiawh qeennaak thoeh doena ngaih-unaak ing qeh nyng.
4 Inu si Mulungu amene mumasangalala ndi zoyipa; choyipa sichikhala pamaso panu.
Nang taw thawlhnaak awh ak zeel Khawsa na am awm hyk ti; na venawh thlak chekhqi am awm thai uhy.
5 Onyada sangathe kuyima pamaso panu; Inu mumadana ndi onse ochita zoyipa.
Thlak oek qu soeih ing na haiawh am dyi thai ti kawmsaw; ik-oeih ak sai palhkhqi ce nang ing sawh na hyk ti.
6 Mumawononga iwo amene amanena mabodza; anthu akupha ndi achinyengo, Yehova amanyansidwa nawo.
A qaai ak kqawnkhqi ce nang ing hqe hyk ti; thlang a thi ak ngaihkhqi ingkaw a qaai ak kqawnkhqi ce Bawipa ing tyih hy.
7 Koma Ine, mwa chifundo chanu chachikulu, ndidzalowa mʼNyumba yanu; mwa ulemu ndidzaweramira pansi kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera.
Cehlai kai taw na lungnaak ak caming na ip khuina law kawng; kqihchahnaak ing na bawk im ciim benna koep kawng nyng.
8 Tsogolereni Inu Yehova, mwa chilungamo chanu chifukwa cha adani anga ndipo wongolani njira yanu pamaso panga.
Aw Bawipa ka qaalkhqi a awm dawngawh na dyngnaak benna ni hqui lah; ka haiawh na lampyi ce dyng sak lah.
9 Palibe mawu ochokera mʼkamwa mwawo amene angadalirike; mtima wawo wadzaza ndi chiwonongeko. Kummero kwawo kuli ngati manda apululu; ndi lilime lawo amayankhula zachinyengo.
Cekkhqi am khak khui awhkaw awi taw lungoet awm cangnaak kawina am awm hy; kawtih, amik kawlungkhqi seetnaak ing be uhy. Amik awihqawngkhqi ce phyi ak awng qu hyt amyihna awm nawh, a mim lai ing ami qaai kqawn uhy.
10 Lengezani kuti ndi olakwa, Inu Mulungu! Zochita zawo zoyipa zikhale kugwa kwawo. Achotseni pamaso panu chifukwa cha machimo awo ambiri, pakuti awukira Inu.
Aw Khawsa, cekkhqi ce thlak thawlh na kqawn khqi hlah! Aming cainaak ce a mimah ang tluknaak na awm lat seh nyng. Thawlhnaak khawzah ami sai hawh a dawngawh hqek khqi bang hlah, cekkhqi ing nang ni oelh uhy.
11 Koma lolani kuti onse amene apeza chitetezo mwa Inu akondwere; lolani kuti aziyimba nthawi zonse chifukwa cha chimwemwe. Aphimbeni ndi chitetezo chanu, iwo amene amakonda dzina lanu akondwere mwa Inu.
Cehlai, nang awh thuknaak ak suikhqi taw zeel u seh. Zeel doena laa sa u seh, cekkhqi ce chung khqi khoep lah. Cawhtaw nang ming ak lungnaak thlangkhqi ce nang awh zeel kawm uh.
12 Ndithu, Inu Yehova, mumadalitsa olungama; mumawazungulira ndi kukoma mtima kwanu ngati chishango.
Aw Bawipa thlakdyngkhqi taw nang ing zosennaak pe kawm tiksaw; nam qeennaak ing cekkhqi ce chung khqi khoep kawp ti.

< Masalimo 5 >