< Masalimo 41 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka; Yehova amamuwombola pa nthawi yamsautso.
Untuk pemimpin kor. Mazmur Daud. Berbahagialah orang yang memperhatikan orang yang lemah; TUHAN akan menolong dia di waktu kesesakan.
2 Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake; Yehova adzamudalitsa iye mʼdziko ndipo sadzamupereka ku zofuna za adani ake.
TUHAN akan melindungi dan memelihara dia, Ia akan membahagiakannya di bumi, dan tidak menyerahkan dia ke tangan musuhnya.
3 Yehova adzamuthandiza pamene akudwala ndipo adzamuchiritsa pa bedi lake la matenda.
TUHAN akan menolong dia pada waktu sakit, dan memulihkan kesehatannya.
4 Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo; chiritseni pakuti ndakuchimwirani.”
Kataku, "Aku telah berdosa terhadap-Mu, ya TUHAN, kasihanilah aku dan sembuhkanlah aku."
5 Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti, “Kodi munthu ameneyu adzafa liti kuti ayiwalike?”
Musuhku mengatakan yang jahat tentang aku, mereka ingin agar aku mati dan dilupakan.
6 Pamene wina abwera kudzandiona, amayankhula mwachinyengo, pomwe mtima wake ukusonkhanitsa zachipongwe; kenaka iye amatuluka ndi kukalengeza kunja.
Orang-orang yang menjenguk aku tidak tulus ikhlas. Mereka mengumpulkan kabar buruk tentang aku, lalu menyiarkannya ke mana-mana.
7 Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane, iwo amalingalira zoyipa kwambiri za ine, ponena kuti,
Semua yang membenci aku berbisik-bisik; mereka mengatakan yang paling jelek tentang aku.
8 “Matenda owopsa amugwira; sadzaukapo pamalo pamene wagona.”
Kata mereka, "Penyakitnya parah sekali, ia tak mungkin bangun lagi."
9 Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira, iye amene amadya pamodzi ndi ine watukula chidendene chake kulimbana nane.
Bahkan kawan karib yang paling kupercayai, orang yang makan bersamaku, telah menghina aku.
10 Koma Yehova mundichititre chifundo, dzutseni kuti ndiwabwezere.
Kasihanilah aku ya TUHAN, sembuhkanlah aku, agar aku dapat membalas kejahatan lawan-lawanku.
11 Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane, pakuti mdani wanga sandigonjetsa.
Kalau aku tidak dikalahkan musuhku, tahulah aku bahwa Engkau berkenan kepadaku.
12 Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga ndi kundiyimika pamaso panu kwamuyaya.
Engkau menolong aku karena ketulusanku, dan membuat aku hidup bersama-Mu untuk selamanya.
13 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli kuchokera muyaya mpaka muyaya. Ameni ndi Ameni.
Pujilah TUHAN, Allah Israel! Pujilah Dia sekarang dan selama-lamanya! Jadilah demikian. Amin!

< Masalimo 41 >