< Masalimo 3 >

1 Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu. Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira!
Psalmus David, Cum fugeret a facie Absalom filii sui. Domine quid multiplicati sunt qui tribulant me? multi insurgunt adversum me.
2 Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” (Sela)
Multi dicunt animae meae: Non est salus ipsi in Deo eius.
3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza, Inu mwandiveka ulemerero ndipo mwanditukula.
Tu autem Domine susceptor meus es, gloria mea, et exaltans caput meum.
4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera. (Sela)
Voce mea ad Dominum clamavi: et exaudivit me de monte sancto suo.
5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo; ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza.
Ego dormivi, et soporatus sum: et exurrexi, quia Dominus suscepit me.
6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene abwera kulimbana nane kuchokera ku madera onse.
Non timebo millia populi circumdantis me: exurge Domine: salvum me fac Deus meus.
7 Dzukani, Inu Yehova! Pulumutseni, Inu Mulungu wanga. Akantheni adani anga onse pa msagwada; gululani mano a anthu oyipa.
Quoniam tu percussisti omnes adversantes mihi sine causa: dentes peccatorum contrivisti.
8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova. Madalitso akhale pa anthu anu. (Sela)
Domini est salus: et super populum tuum benedictio tua.

< Masalimo 3 >