< Masalimo 131 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
En visa Davids i högre choren. Herre, mitt hjerta. är icke högfärdigt, och mina ögon äro icke stolta; och jag vandrar icke i stor ting, de mig för höge äro.
2 Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
När jag icke satte och stillte mina själ, så vardt min själ afvand, såsom en ifrå sine moder afvand varder.
3 Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Israel hoppes uppå Herran, ifrå nu och i evighet.

< Masalimo 131 >