< Masalimo 112 >

1 Tamandani Yehova. Wodala munthu amene amaopa Yehova, amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
Bawipa taw kyihcah lah uh. Bawipa kqih nawh ak awipeekkhqi awh zeelnaak ak takhqi taw ami zoseen hy.
2 Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
A cakhqi qam khuiawh thlak bau na awm kawm usaw; thlakdyngkhqi a cadil taw ami zoseen kawm uh.
3 Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Boeinaak ingkaw mangnaak taw a ipkhui awh awm kawmsaw, a dyngnaak ce kumqui dy awm loet kaw.
4 Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima; wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
Thlang qeenkhaw ak ngai lungnaak ak ta thlak dyngkhqi ham taw, thannaak awh zani vangnaak awm pehy.
5 Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
Boecawn naak ing a zoena thlang pu nawh ak thym na khaw ak sakhqik khan awh ik-oeih leek pha law kaw.
6 Ndithu sadzagwedezeka; munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
Anih ce ityk awh awm am tat tikaw; thlak dyng taw kumqui dy u ing am hilh tikaw.
7 Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
Awithang che awh kqihnaak am ta kaw; ak kaw cak nawh, Bawipa ce ypna hy.
8 Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
Ak kawlung yp nawh, kqihnaak am tahy; a dytnaak awhtaw a qaalkhqi ce noengnaak ing toek kaw.
9 Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya; nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
Khawdeng hahqahkhqi venawh kutdo a qek a ra a dawngawh, a dyngnaak ce kumqui dy cak hy; ak ki ce zoeksangnaak ing kyih na awm kaw.
10 Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.
Thlakche ing a huh awh ak kaw am zeel kaw; a ha taak kawmsaw plal a tham pahoei kaw; thlakchekhqi a ngaihnaak taw dyt hqoeng kaw.

< Masalimo 112 >