< Miyambo 16 >

1 Zolinga za mu mtima ndi za munthu, koma kwa Yehova ndiye kumachokera yankho.
Человеку предложение сердца: и от Господа ответ языка.
2 Zochita zonse za munthu zimaoneka zabwino pamaso pake, koma Yehova ndiye amasanthula zolinga zako.
Вся дела смиреннаго явленна пред Богом, и укрепляяй духи Господь.
3 Pereka ntchito zako zonse mʼmanja mwa Yehova, ndipo zolinga zako zidzachitikadi.
Приближи ко Господу дела твоя, и утвердятся помышления твоя.
4 Yehova amachita zonse ndi cholinga chake, ngakhale anthu oyipa kuti aone tsiku latsoka.
Вся содела Господь Себе ради: нечестивии же в день зол погибнут.
5 Munthu aliyense wodzikuza amamunyansa Yehova. Koma dziwani izi: Iwo sadzakhala osalangidwa.
Нечист пред Богом всяк высокосердый: в руку же руце влагаяй неправедно не обезвинится.
6 Chifukwa cha chikondi chosasinthika ndi kukhulupirika, munthu amakhululukidwa machimo ake; chifukwa cha kuopa Yehova munthu amapewa zoyipa.
Начало пути блага, еже творити праведная, приятна же пред Богом паче, нежели жрети жертвы.
7 Pamene makhalidwe a munthu akondweretsa Yehova, ngakhale adani ake amakhala naye mwa mtendere.
Ищай Господа обрящет разум со правдою:
8 Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono zozipeza mwachilungamo, kusiyana ndi kukhala ndi zinthu zambiri zozipeza popanda chilungamo.
праве же ищущии его обрящут мир.
9 Mtima wa munthu umalingalira zochita, koma Yehova ndiye amakhazikitsa njira zake.
Вся дела Господня со правдою: хранится же нечестивый на день зол.
10 Mawu a mfumu ali ngati mawu ochokera kwa Mulungu; ndipo pakamwa pake sipalakwa poweruza mlandu.
Пророчество во устнех царевых, в судищи же не погрешат уста его.
11 Miyeso ndi masikelo achilungamo zimachokera kwa Yehova; miyala yonse yoyesera ya mʼthumba anayipanga ndi Yehova.
Превеса мерила правда у Господа: дела же Его мерила праведная.
12 Kuchita zoyipa kumanyansa mafumu, pakuti chilungamo ndiye maziko a ufumu wake.
Мерзость цареви творяй злая: со правдою бо уготовляется престол началства.
13 Mawu owona amakondweretsa mfumu. Iyo imakonda munthu woyankhula choonadi.
Приятны царю устне праведны, словеса же правая любит Господь.
14 Ukali wa mfumu ndi mthenga wa imfa, koma munthu wanzeru amawupepesa ukaliwo.
Ярость царева вестник смерти: муж же премудр утолит его.
15 Kuwala kwa nkhope ya mfumu kumapatsa moyo; ndipo kukoma mtima kwake kuli ngati mitambo ya mvula nthawi ya chilimwe.
Во свете жизни сын царев: приятнии же ему яко облак позден.
16 Nʼkwabwino kwambiri kupeza nzeru kupambana golide. Kukhala womvetsa bwino zinthu nʼkwabwino kupambana ndi kukhala ndi siliva.
Угнеждения премудрости избраннее злата: вселения же разума дражайши сребра.
17 Msewu wa munthu wowongoka mtima umapewa zoyipa; wopenyetsetsa kumene akupita amasunga moyo wake.
Путие жизни укланяются от злых: долгота же жития путие праведни. Приемляй наказание во благих будет, храняй же обличения умудрится. Иже хранит своя пути, соблюдает свою душу: любяй же живот свой щадит своя уста.
18 Kunyada kumafikitsa ku chiwonongeko, ndipo munthu wodzikuza adzagwa.
Прежде сокрушения предваряет досаждение, прежде же падения злопомышление.
19 Nʼkwabwino kukhala ndi mtima wodzichepetsa pakati pa anthu oponderezedwa, kusiyana ndi kugawana zolanda ndi anthu onyada.
Лучше кроткодушен со смирением, нежели иже разделяет корысти с досадительми.
20 Munthu womvera malangizo zinthu zimamuyendera bwino, ndipo wodala ndi amene amadalira Yehova.
Разумный в вещех обретатель благих, надеяйся же на Господа блажен.
21 A mtima wanzeru amatchedwa ozindikira zinthu, ndipo mawu ake okoma amawonjezera nzeru.
Премудрыя и разумныя злыми наричут, сладции же в словеси множае услышани будут.
22 Kumvetsa zinthu ndi kasupe wa moyo kwa iwo amene ali nako, koma uchitsiru umabweretsa chilango kwa zitsiru.
Источник животен разум стяжавшым, наказание же безумных зло.
23 Mtima wanzeru umathandiza munthu kuyankhula mwa nzeru, ndipo mawu ake amawonjezera nzeru.
Сердце премудраго уразумеет яже от своих ему уст, во устнах же носит разум.
24 Mawu okometsera ali ngati chisa cha njuchi, amakoma mu mtima ndipo amalimbitsa thupi.
Сотове медовнии словеса добрая, сладость же их изцеление души.
25 Pali njira ina yooneka ngati yowongoka kwa munthu koma kumatsiriziro kwake ndi imfa.
Суть путие мнящиися прави быти мужу, обаче последняя их зрят во дно адово.
26 Njala ya munthu wantchito imamuthandiza kulimbikira; njalayo imamukakamiza kuchitapo kanthu.
Муж в трудех труждается себе и изнуждает погибель свою: строптивый во своих устах носит погибель.
27 Munthu wopanda pake amakonzekera kuchita zoyipa ndipo mawu ake ali ngati moto wopsereza.
Муж безумен копает себе злая и во устнах своих сокровищствует огнь.
28 Munthu woyipa mtima amayambitsa mikangano, ndipo miseche imalekanitsa anthu okondana kwambiri.
Муж строптивый разсылает злая, и светилник льсти вжигает злым, и разлучает други.
29 Munthu wandewu amakopa mnansi wake, ndipo amamuyendetsa njira imene si yabwino.
Муж законопреступен прельщает други и отводит их в пути не благи.
30 Amene amatsinzinira maso ake amalingalira zinthu zokhota; amene amachita msunamo amakonzeka kuchita zoyipa.
Утверждаяй очи свои мыслит развращенная, грызый же устне свои определяет вся злая: сей пещь есть злобы.
31 Imvi zili ngati chipewa chaufumu chaulemerero; munthu amazipeza akakhala moyo wolungama.
Венец хвалы старость, на путех же правды обретается.
32 Munthu wosapsa mtima msanga amaposa munthu wankhondo, munthu wowugwira mtima wake amaposa amene amalanda mzinda.
Лучше муж долотерпелив паче крепкаго, (и муж разум имеяй паче земледелца великаго: ) удержаваяй же гнев паче вземлющаго град.
33 Maere amaponyedwa pa mfunga, koma ndiye Yehova amene amalongosola zonse.
В недра входят вся неправедным: от Господа же вся праведная.

< Miyambo 16 >