< Obadiya 1 >

1 Masomphenya a Obadiya. Ambuye Yehova akunena kwa Edomu kuti, Tamva uthenga wochokera kwa Yehova: Nthumwi yatumidwa kupita kwa anthu a mitundu kukanena kuti, “Konzekani, tiyeni tikachite nkhondo ndi Edomu.”
Utvara Avdijeva. Ovako veli Gospod Gospod za Edomsku: èusmo glas od Gospoda, i glasnik bi poslan k narodima: ustajte, da ustanemo na nju u boj.
2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina; udzanyozedwa kwambiri.
Gle, uèiniæu te malijem meðu narodima, biæeš vrlo prezren.
3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa, iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwe ndipo umamanga nyumba zako pa mapiri ataliatali, iwe amene umanena mu mtima mwako kuti, ‘Ndani anganditsitse pansi?’
Ponos srca tvojega prevari te, tebe, koji živiš u rasjelinama kamenijem, u visokom stanu svom, i govoriš u srcu svom: ko æe me oboriti na zemlju?
4 Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhanga ndi kumanga chisa chako pakati pa nyenyezi, ndidzakutsitsa pansi kuchokera kumeneko,” akutero Yehova.
Da podigneš visoko kao orao i meðu zvijezde da metneš gnijezdo svoje, odande æu te oboriti, govori Gospod.
5 “Anthu akuba akanabwera kwa iwe, kapena anthu olanda zinthu akanafika usiku, aa, tsoka lanji limene likukudikira iwe! Kodi akanangotengako zimene akuzifuna zokha? Ngati anthu othyola mphesa akanafika, kodi akanakusiyiraniko mphesa pangʼono pokha?
Kako si oplijenjen? da su došli k tebi kradljivci ili lupeži noæu, ne bi li pokrali koliko im je dosta? da su došli k tebi beraèi vinogradski, ne bi li ostavili pabiraka?
6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse, chuma chake chobisika chidzabedwa!
Kako se pretraži Isav, kako se naðoše potaje njegove!
7 Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire; abwenzi ako adzakunyenga ndi kukugonjetsa; amene amadya chakudya chako adzakutchera msampha, koma iwe sudzazindikira zimenezi.”
Do granice te odvedoše svi koji bijahu s tobom u vjeri, prevariše te i nadvladaše te koji bijahu u miru s tobom; koji jedu hljeb tvoj podmetnuše ti zamku, da se ne opazi.
8 Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo, kodi sindidzawononga anthu onse anzeru a ku Edomu, anthu odziwa zinthu mʼmapiri a Esau?
U onaj dan, govori Gospod, neæu li pogubiti mudre u zemlji Edomskoj i razumne u gori Isavovoj?
9 Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha, ndipo aliyense amene ali mʼphiri la Esau adzaphedwa pa nkhondo.
I tvoji æe se junaci uplašiti, Temane, da se istrijebe pokoljem svi iz gore Isavove.
10 Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo, udzakhala wamanyazi; adzakuwononga mpaka muyaya.
Za nasilje uèinjeno bratu tvojemu Jakovu pokriæe te stid i istrijebiæeš se zasvagda.
11 Pamene adani ankamulanda chuma chake pamene alendo analowa pa zipata zake ndi kuchita maere pa Yerusalemu, pa tsikulo iwe unali ngati mmodzi wa iwo.
Onaj dan, kad ti stajaše nasuprot; onaj dan, kad inostranci odvoðahu u ropstvo vojsku njegovu, i tuðinci ulažahu na vrata njegova i bacahu ždrijeb za Jerusalim, bješe i ti kao koji od njih.
12 Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wako pa nthawi ya tsoka lake, kapena kunyogodola Ayuda chifukwa cha chiwonongeko chawo, kapena kuwaseka pa nthawi ya mavuto awo.
Ali ti ne trebaše gledati dana brata svojega, dana, kad se odvoðaše u tuðu zemlju, niti se radovati sinovima Judinijem u dan kad propadahu, niti razvaljivati usta u dan nevolje njihove.
13 Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu anga pa nthawi ya masautso awo, kapena kuwanyogodola pa tsiku la tsoka lawo, kapena kulanda chuma chawo pa nthawi ya masautso awo.
Ne trebaše ti uæi na vrata naroda mojega u dan pogibli njihove, ne trebaše da i ti gledaš zlo njihovo u dan pogibli njihove ni da se mašaš dobra njihova u dan pogibli njihove.
14 Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu kuti uphe Ayuda othawa, kapena kuwapereka kwa adani awo Ayuda opulumuka pa nthawi ya mavuto awo.”
Niti trebaše da staneš na rasputicu da ubijaš bježan njihovu, niti da izdaješ onijeh koji ostaše u dan nevolje.
15 “Tsiku la Yehova layandikira limene adzaweruza mitundu yonse ya anthu. Adzakuchitira zomwe unawachitira ena; zochita zako zidzakubwerera wekha.
Jer je dan Gospodnji blizu svijem narodima; kako si èinio, tako æe ti biti, plata æe ti se vratiti na glavu tvoju.
16 Iwe unamwa pa phiri langa loyera, koteronso mitundu ina yonse idzamwa kosalekeza; iwo adzamwa ndi kudzandira ndipo adzayiwalika pa mbiri ya dziko lapansi.
Jer kao što ste vi pili na svetoj gori mojoj, tako æe piti svi narodi vazda, piæe, i ždrijeæe, i biæe kao da ih nije bilo.
17 Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso; phirilo lidzakhala lopatulika, ndipo nyumba ya Yakobo idzalandira cholowa chake.
A na gori æe Sionu biti spasenje, i biæe sveta, i dom æe Jakovljev naslijediti našljedstvo svoje.
18 Nyumba ya Yakobo idzasanduka moto ndipo nyumba ya Yosefe idzasanduka lawi la moto; nyumba ya Esau idzasanduka chiputu, ndipo adzayitenthe pa moto ndi kuyipsereza. Sipadzakhala anthu opulumuka kuchokera mʼnyumba ya Esau.” Yehova wayankhula.
I dom æe Jakovljev biti oganj i dom Josifov plamen, a dom Isavov strnjika; i razgorjeæe se na njih, i spaliæe ih; i neæe biti ostatka domu Isavovu, jer Gospod reèe.
19 Anthu ochokera ku Negevi adzakhala ku mapiri a Esau, ndipo anthu ochokera mʼmbali mwa mapiri adzatenga dziko la Afilisti. Adzakhala mʼminda ya Efereimu ndi Samariya, ndipo Benjamini adzatenga Giliyadi.
I naslijediæe jug, goru Isavovu, i ravnicu, Filisteje; i naslijediæe polje Jefremovo i polje Samarijsko i Venijaminovo i Galad;
20 Aisraeli amene ali ku ukapolo adzalandira dziko la Kanaani mpaka ku Zarefati; a ku Yerusalemu amene ali ku ukapolo ku Sefaradi adzalandira mizinda ya ku Negevi.
I zarobljena vojska sinova Izrailjevijeh naslijediæe što je bilo Hananejsko do Sarepte; a roblje Jerusalimsko, što je u Sefaradu, naslijediæe južne gradove.
21 Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyoni ndipo adzalamulira mapiri a Esau. Koma ufumuwo udzakhala wa Yehova.
I izbavitelji æe izaæi na goru Sion da sude gori Isavovoj, i carstvo æe biti Gospodnje.

< Obadiya 1 >