< Mateyu 26 >

1 Yesu atamaliza kuyankhula zonsezi, anati kwa ophunzira ake,
Wakati Yesu ayomwi longela malongelo goti, abakiye anapunzi bake,
2 “Monga mukudziwa, kwatsala masiku awiri kuti Paska ifike ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kuti apachikidwe.”
“Mutangite baada ya masoba gabele kwalowa baa na lisoba lya pasaka, na mwana wa Adamu apiyilwa linga bakongele.”
3 Pamenepo akulu a ansembe ndi akuluakulu anasonkhana ku nyumba ya mkulu wa ansembe dzina lake Kayafa,
Baada ya bakuu ba makuhani ni apindo ba bandu bakwembanike pamope mu'ukumbi wa kuhani nkolo, ywakemelwage Kayafa.
4 ndipo anapangana kuti amugwire Yesu mobisa ndi kumupha.
Kwa pamope bapangite mpango wa kumoywa Yesu kwa siri na kumulaga.
5 Ndipo anati, “Osati nthawi yaphwando chifukwa pangabuke chipolowe pakati pa anthu.”
Mana batibaya, kana ipangike lisoba lya sikukuu, yakana yoka puyo kwa baadhi ya bandu.”
6 Yesu ali ku Betaniya mʼnyumba Simoni Wakhate,
Wakati Yesu paabile Bethania mu'nyumba ya Simoni ywabile nkoma,
7 mayi wina anabwera kwa Iye ndi botolo la mafuta onunkhira a mtengowapatali, amene anathira pa mutu pake Iye akudya pa tebulo.
pagoloki pameza, nnwawa yumo aisi kachake abile apotwi kikoba chakibile na mauta ga garama ngolo, aijitii mu mutwe wake.
8 Ophunzira ataona izi anayipidwa nafunsa kuti, “Chifukwa chiyani akuwononga chotere?
Lakini anapunzi bake bapakibweni kitendo choo, batichukya muno no baya, mwanja namani upangite nyoo.
9 Mafuta amenewa akanatha kugulitsidwa pa mtengo waukulu, ndipo ndalama zake zikanaperekedwa kwa osauka.”
Aga tulowe weza pemeya kwa kiasi kikolo na kwapeya maskini.”
10 Yesu podziwa izi anawawuza kuti, “Chifukwa chiyani mukumuvutitsa mayiyu? Wandichitira Ine chinthu chabwino.
Lakini Yesu ayomwile tanga lee, ngababakiya, “Mwanza na matusuluya nnwawa yoo? kwa kuwa apangite kilebe kinanoga kasango.
11 Osauka mudzakhala nawo nthawi zonse, koma simudzakhala ndi Ine nthawi zonse.
Maskini mubile nabo kila lisoba, lakini mutama kwaa na nenga kila lisoba.
12 Pamene wathira mafuta onunkhirawa pa thupi langa, wachita izi kukonzekera kuyikidwa kwanga mʼmanda.
Kwa mwanza panijili maula payega yango, apangite nyo kwa mwanza ya kunisika kwango.
13 Zoonadi, ndikuwuzani kuti kulikonse kumene Uthenga Wabwinowu udzalalikidwa ku dziko lonse lapansi, zimene wachitazi zidzanenedwanso pomukumbukira.”
Kweli nenda kwamakiya, popote payahubiliwa injili pakilambo chote, kitendo cha kipangite ayo nnwawa, chalowa pangilwa kwa mwaya kombokya.”
14 Pamenepo mmodzi wa khumi ndi awiriwo wotchedwa Yudasi Isikarioti anapita kwa akulu a ansembe
Nga yumo nkati ya balo komi ni ibele, ywakemelwa Yuda Iskariote, ayei kwa apindo ba makuhani,
15 nafunsa kuti, “Kodi mundipatsa chiyani ngati nditamupereka Iye kwa inu?” Pamenepo anamuwerengera ndalama zokwanira masiliva makumi atatu.
no baya, “Mwalowa mbeya namani mana ninangile?” Ngaba mpemwa Yuda ipande thelathini ya mbanje.
16 Kuyambira pamenepo Yudasi anafunafuna nthawi yabwino yoti amupereke Yesu.
Buka muda wo apalange nafasi ya kwalangya.
17 Pa tsiku loyamba laphwando la buledi wopanda yisiti, ophunzira anabwera kwa Yesu ndi kumufunsa kuti, “Kodi mukufuna tikakonze kuti malo odyera Paska?”
Hata lisoba lya kwanza lya mikate yange lola, anapunzi banyendeli Yesu na kumakiya, “Kwaako kupala tukutayarishie ulye chakulya cha Pasaka?”
18 Iye anayankha kuti, “Pitani mu mzinda kwa munthu wakutiwakuti ndipo kamuwuzeni kuti, ‘Aphunzitsi akuti, nthawi yanga yoyikidwa yayandikira. Ine ndidzadya phwando la Paska ndi ophunzira anga ku nyumba kwako.’”
Ngabakiya, “Muyende mjini kwa mundu fulani na mumakiye, mwalimu abaya, “Muda wango uyomwike. Nicha yomolya pasaka pamope ni anapunzi bango munyumba yako.””
19 Pamenepo ophunzira ake anachita monga momwe Yesu anawawuzira ndipo anakonza Paska.
Anapunzi gabapanga kati Yesu mwalangile, batayarishe chakulya cha Pasaka.
20 Kutada, Yesu ndi ophunzira ake khumi ndi awiriwo anakhala pa tebulo nʼkumadya.
Pasaka iikite kitamunyo, atami lya chakulya pamope na anapunzi bake balo komi ni ibele.
21 Akudya, Iye anati, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti mmodzi wa inu adzandipereka.”
Pabile kabalya chakulya, atibaya, “Kweli nenda kwabakiya panga pakatikati yinu yumo apala kunisaliti.
22 Iwo anamva chisoni kwambiri ndipo anayamba kuyankhulana naye mmodzimmodzi nati, “Kodi nʼkukhala ine Ambuye?”
Batihuzunika muno, na kila yumo ande kunaluya, “Nenga buli kwa, Ngwana?”
23 Yesu anayankha nati, “Iye amene akusunsa mʼmbale pamodzi ndi Ine, yemweyo adzandipereka.
Kayangwa, aywo ywasanja pamope na nenga mubakuri ngalowa kunisaliti.
24 Mwana wa Munthu adzaphedwa monga mmene kunalembedwera za Iye. Koma tsoka kwa munthu amene apereka Mwana wa Munthu! Kukanakhala bwino kwa iye akanapanda kubadwa.”
Mwana wa Adamu endabuka, kati mwaiandikilwe. Ila ole wake mundu ywasaliti mwana wa Adamu! Yanogite bora mundu ywo akakotoka belekwa.”
25 Ndipo Yudasi amene anamupereka Iye anati, “Monga nʼkukhala ine Aphunzitsi?” Yesu anayankha nati, “Iwe watero.”
Yuda ywapala kusaliti atibaya, “Je, nenga mwalimu?” Yesu kammakiya, “Ngawenga wolongela.”
26 Pamene ankadya, Yesu anatenga buledi, nayamika ndipo anamunyema nagawira ophunzira ake nanena kuti, “Tengani, idyani; ili ndi thupi langa.”
Pababile kaba lya chakulya, Yesu autweli nkate, atikubariki, na metwana. Apei anapunzi bake no baya, “Mutole, mulye. Aye yega yango.”
27 Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo nati, “Imwani nonsenu.
Ngatola kikombe no shukuru, ngapeya no baya, Munye mwabote mukikombe chee.
28 Awa ndi magazi anga a pangano amene akhetsedwa chifukwa cha ambiri kuti akhululukidwe machimo.
Kwa mwanja aye maiyango yo lagano kwango, yaipenganika kwa sababu banansima kwa kwasamiya sambi.
29 Ndikuwuzani kuti sindidzamwanso kuchokera ku chipatso cha mtengo wa mpesa kuyambira lero mpaka tsiku ilo pamene ndidzamwenso mwatsopano ndi inu mu ufumu wa Atate anga.”
Lakini nenda kuamakiya, nanywali kae matunda ya zabibu go, ata lisoba lelo lyana lowanywa pamope namwee ku'utawala wa Tate bango.”
30 Atayimba nyimbo, anatuluka kupita ku phiri la Olivi.
Payomwile yemba mwambo, batiboka yenda kukitombe cha mizeituni.
31 Pamenepo Yesu anawawuza kuti, “Usiku omwe uno inu nonse mudzandithawa, pakuti kwalembedwa: “‘Kantha mʼbusa, ndipo nkhosa zidzabalalika.’
Boka po Yesu atikwabakiya, “Kilo cheno mwabote walowa kwikobala kwa mwanja nenge, kwasababu itiandikilwa, Nalowa kukombwa mchungaji na ngondolo bakikundi basambalalika.
32 Koma ndikadzauka, ndidzatsogola kupita ku Galileya.”
Lakini baada yo yoka kwango, nalowa longolya yenda Galilaya.”
33 Petro anayankha nati, “Ngakhale onsewa atakuthawani, ine ndekha ayi.”
Lakini Petro atikummakiya, “Hata mana itei bote bakukani kwa mwanja ya makowe gagalowa kupata, Nenga nikukana kwaa.
34 Yesu anayankha nati, “Zoonadi, ndikukuwuza kuti usiku omwe uno, asanalire tambala, udzandikana Ine katatu.”
Yesu kannyangwa, “Kweli nenda kuabakiya, kilo cheno ngoko nanome anabeka kwaa, alowa kunikana mara itatu.”
35 Koma Petro ananenetsa nati, “Ngakhale kutakhala kufa nanu pamodzi, sindidzakukanani.” Ndipo ophunzira onse ananena chimodzimodzi.
Petro ngamakiya, hata mana itei waa na wenga, nikukana kwaa.”Na anapunzi bake benge bote babaite nyonyonyo.
36 Kenaka Yesu anapita ku malo otchedwa Getsemani, ndipo anawawuza kuti, “Khalani pano pamene Ine ndikukapemphera apo.”
Baadae Yesu ayei nabo pandu papakemelwa. Gethsemane atikwabakiya anapunzi bake, “Mutame paa wakati paniyenda loba apo.”
37 Anatenga Petro ndi ana awiri a Zebedayo, ndipo anayamba kumva chisoni ndi kuvutika mu mtima.
Apotwi Petro na bana abele ba Zebedayo ngatumbwa huzunika na sikitika.
38 Pamenepo anawawuza kuti, “Moyo wanga uli ndi chisoni chofa nacho. Khalani pano ndipo dikirani pamodzi ndi Ine.”
Boka po atikwabakiya, “Roho yango yenda minya muno, hata kiasi cho waa. Mwiigale papamukeshe loba nanee.”
39 Atapita patsogolo pangʼono, anagwa pansi chafufumimba napemphera kuti, “Atate anga, ngati ndikotheka, chikho ichi chichotsedwe kwa Ine. Koma osati monga mmene ndifunira, koma monga mufunira Inu.”
Ayei nnonge pachene, kalola pae wa kukama, no loba, Tate bango, mana kewezekana, kikombe sekinipele, kana ipange kati mwanipala nenga, ila kati mwamupata mwee.”
40 Kenaka anabwera kwa ophunzira ake nawapeza ali mtulo. Iye anafunsa Petro kuti, “Kodi anthu inu, simukanakhala maso pamodzi ndi Ine kwa ora limodzi lokha?
Ngayendeya anapunzi kakolya bangonjike lugono, ngamakiya Petro, mwanja namani ukotwike keleka pamope na nee kwa lisaa limo?
41 Khalani maso ndi kupemphera kuti musagwe mʼmayesero. Mzimu ukufuna koma thupi ndi lofowoka.”
Mukeleke mulobe linga kana uyingii mumajaribu. Roho ibile radhi bai, lakini yega ibii zaipu.”
42 Anachokanso nakapemphera kachiwiri kuti, “Atate anga, ngati chikhochi sichingandichoke, mpaka nditamwa, kufuna kwanu kuchitike.”
Atiboka kae mara yene ibele yoloba, “Tate bango, mana itei likowe lee ngwesa kwaa kulikwepa na lazima nikinyweli kikombe chee, mwamupendi mwenga itimii,”
43 Atabweranso anawapeza ali mtulo chifukwa zikope zawo zinalemedwa ndi tulo.
Kaabuya kae aisi kwakolya bagonjike lugono, mana minyo gabe gabi matopau.
44 Choncho anawasiya napitanso kukapemphera kachitatu nanenanso chimodzimodzi.
Ngabakiya kae kaboka ngayengda loba mara yenge itatu kabaya makowe gagalo.
45 Kenaka anabwera kwa ophunzira ake nati kwa iwo, “Kodi mukanagonabe ndi kupumula? Taonani, ora layandikira ndipo Mwana wa Munthu akuperekedwa mʼmanja mwa ochimwa.
Baadae Yesu ayendeli anapunzi bake nakwabakiya, “Bado mugonjike na pomolya? Mulinge saa iegelile, mwana wa Adamu endasa litiwa mmokoya bene sambi.
46 Imirirani, tiyeni tizipita! Wondipereka Ine wafika!”
Muyumuke tuboke. Mulinge yolo ywapala kunisaliti aegelite.”
47 Akuyankhula choncho, Yudasi mmodzi mwa khumi ndi awiriwo anafika. Pamodzi ndi iye panali gulu lalikulu la anthu ali ndi mikondo ndi zibonga otumidwa ndi akulu a ansembe ndi akuluakulu.
Wakati abibalo kalongela, Yuda yumo kati ya balo komi ni ibele, atiisa. kipenga sa bandu chatiisa nabo, kaliboka kwa apindo ba makuhani na apindo ba bandu. Baisi na mapanga na ndolonga.
48 Womuperekayo anawawuziratu chizindikiro anthuwo kuti, “Amene ndidzapsompsona ndi iyeyo; mugwireni.”
Na mundu ywakusudie Yesu ampei ishara, atibaya, yoloywa nannoniya ngaywo. Mwamoywe.”
49 Pamenepo Yudasi anapita kwa Yesu nati, “Moni, Aphunzitsi!” Ndipo anapsompsona Iye.
Mra ngaisa kwa Yesu no baya, “Salamu, mwalimu!”Nakunnoniya.
50 Yesu anayankha kuti, “Bwenzi langa, chita chimene wabwerera.” Pamenepo anthuwo anabwera patsogolo namugwira Yesu ndi kumumanga.
Yesu ngammakiya, “Webwiga lyango, Ulipange lelo lya likuletike,” Ngabaisa kumoywa Yesu na maboko gabe.
51 Pa chifukwa ichi, mmodzi wa anzake a Yesu anagwira lupanga lake, nalisolola ndi kutema wantchito wa mkulu wa ansembe, nadula khutu lake.
Lola, mundu yumo ywabile pamope ni Yesu, ngasolomwa kyembe na kumkombwa mmanda wa ntumwa nkolo na kukata likutu lyake.
52 Yesu anati kwa iye, “Bwezera lupanga lako mʼchimake, chifukwa onse amene amapha ndi lupanga adzafa ndi lupanga.
Nga Yesu kaamakiya, “kelebuya lipanga lyako mulupata lwake. Kwa mwanza bote babatumya lipanga balowa polota kwa lipanga.
53 Kodi mukuganiza kuti sindingathe kupempha Atate anga ndipo nthawi yomweyo nʼkundipatsa magulu a angelo oposa khumi ndi awiri?
Muwasa panga ngwesa kwaa kwakema Tate bango, naywembe alowezekunilumya majeshi zaidi ya komi ni ibele ba malaika?
54 Koma nanga malemba akwaniritsidwa bwanji amene akuti ziyenera kuchitika motere?”
Lakini kwa kitiwi gagaandikilwe gaweza timya, aga ngagapalikwa gapiti?”
55 Pa nthawi yomweyo Yesu anati kwa gululo, “Kodi ndine mtsogoleri wa anthu owukira kuti mwabwera ndi malupanga ndi zibonga kudzandigwira? Tsiku ndi tsiku ndimakhala mʼNyumba ya Mulungu kuphunzitsa, koma simunandigwire.
Wakati woo Yesu kakikoya chelo kipenga sa bandu, “Mbona mwisi na mapanga na mandolonga kuniboywa kati na mwii? Kila lisoba natami muhekalu kanipundisa, mwaniboywi kwaa!
56 Koma zonsezi zachitika kuti zolembedwa ndi aneneri zikwaniritsidwe.” Pamenepo ophunzira anamusiya nathawa.
Lakini aga gote gapangike lenga maandiko ya manabii gatimii.” Nga anapunzi bake kabanneka ni kabatila.
57 Iwo amene anamugwira Yesu anamutengera kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anasonkhana.
Balo babamoywile Yesu bampeike kwaa Kayfa, kuhani nkolo, pandu pabakusanyike aandishi na apindo babile bakusanyilwe pamope.
58 Koma Petro anamutsatira Iye patali, mpaka ku bwalo la mkulu wa ansembe. Analowa nakhala pansi pamodzi ndi alonda kuti aone zotsatira.
Lakini Petro atikukengama msongo kwakutalu mpaka mukumbi wa kuhani nkolo. Ajingii munyumba notama pamope na alinzi akibone chakilowa pangila.
59 Akulu a ansembe ndi akulu olamulira Ayuda amafunafuna umboni wonama wofuna kuphera Yesu.
Bai apindo amakuhani na baraza lyote babile kabapala ushaidi wa ubocho kwa Yesu, lenga bate kumulaga.
60 Koma sanathe kupeza uliwonse, angakhale kuti mboni zambiri zabodza zinapezeka. Pomalizira mboni ziwiri zinabwera patsogolo.
Ijapo bapitike mashahidi banansima, lakini bapatike kwa sababu. Ila baadae mashaidi abele bati kwipiya nnonge
61 Ndipo zinati, “Munthu uyu anati, ‘Ndikhoza kupasula Nyumba ya Mulungu ndi kuyimanganso mʼmasiku atatu.’”
no baya, “Mundu yo atibaya “Ngwesa kulibomwana hekalu lya Nnongo na kuchenga kwa masoba gatatu.”
62 Pamenepo mkulu wa ansembe anayimirira nati kwa Yesu, “Kodi suyankha? Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?”
Kuhani nkolo kayema ni kunaluya, “Huweza kwaa yangwa? Hababakushitakya namani wenga?”
63 Koma Yesu anakhalabe chete. Mkulu wa ansembe anati kwa Iye, “Ndikulamulira Iwe ndi lumbiro pamaso pa Mulungu wa Moyo: utiwuze ife ngati ndiwe Khristu Mwana wa Mulungu.”
Lakini Yesu atami liki. Kuhani kulo ngamakiya, “Kati Nnongo mwabile, nenda kulasimisha utubakiye, panga wenga wa Kristo, wa mwana wa Nnongo.”
64 Yesu anayankha nati, “Mwanena ndinu. Koma ndikunena kwa inu nonse: mʼtsogolomo mudzaona Mwana wa Munthu atakhala kudzanja lamanja la Wamphamvuzonse ndipo akubwera ndi mitambo ya kumwamba.”
Yesu kayangwa, “Wenga wa mwene ubaite likowe lyo. Lakini enakubakiya, boka sayeno no yendelya wamona mwana wa Adamu atami kuluboko lwa mmalyo lwene ngupu, na kaida mu maunde ga kunani.”
65 Pamenepo mkulu wa ansembe anangʼamba zovala zake nati, “Wanyoza Mulungu! Tifuniranji mboni zina? Taonani, tsopano mwamva mwano wake.
Nga kuhani nkolo kalendwana ngobo yake no baya, Atikupuru! Je, tupala kae ushahidi wakele? Linge, tayari muyowine kakufuru.
66 Mukuganiza bwanji?” Iwo anayankha kuti, “Ayenera kuphedwa!”
Je! muwaza namani? Ngabayangwa no baya.”Ipalikwa awee.”
67 Kenaka anamulavulira kumaso namumenya ndi zibakera. Ena anamumenya makofi.
Ngaba mwuniya mata kuminya na kukombwa makofi kwa maboko gabe,
68 Ndipo anati, “Tanenera kwa ife, Khristu. Wakumenya ndani?”
no baya, ututabilie wenga wa Kristo. Naiywa kukombwile?”
69 Tsopano Petro anakhala ku bwalo la nyumbayo, ndipo mtsikana wantchito anabwera kwa iye nati, “Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya.”
Wakati wo Petro atami panja kuhukumbi, amanda alwawa batikunnyendelya no baya, “Wenga wabi pamope ni Yesu wa Galilaya.
70 Koma iye anakana pamaso pawo nati, “Sindikudziwa chimene ukunena.”
Lakini atikana nnonge yabote, ngabaya nee nitangite kwaa chaakibaya.”
71 Kenaka anachoka kupita ku khomo la mpanda, kumene mtsikana wina anamuonanso nawuza anthu nati, “Munthu uyu anali ndi Yesu wa ku Nazareti.”
Payei pannango, mmanda ywenge nwawa atikumona na kwabakiya bababile apo,'Mundu yoo nembe abile pamope ni Yesu wa Nazareti.
72 Iye anakananso molumbira kuti, “Sindimudziwa munthuyu!”
Ngankana kae kwa kulapa, “Nenga nintangite kwaa mundu yolo.”
73 Patapita kanthawi pangʼono, amene anayimirira pamenepo anapita kwa Petro nati, “Zoonadi, ndiwe mmodzi wa iwo, popeza mayankhulidwe ako akukuwulula.”
Muda mwipi baadae, balobabayemi karibu, batiyenda yolongela ni Petro, kwa kweli wenga wipamope nakwe, kwa mana hata longela kwako kwenda yowanika.
74 Pamenepo anayamba kudzitemberera ndipo analumbira kwa iwo nati, “Sindimudziwa munthu ameneyo!” Nthawi yomweyo tambala analira.
Nga tumbwa lapangwa no lapa,'Nenga nitangite kwa mundu yoo,” Mara ngoko kabeka.
75 Ndipo Petro anakumbukira mawu amene Yesu anayankhula kuti, “Tambala asanalire, udzandikana Ine katatu.” Ndipo anatuluka panja nakalira kwambiri.
Petro kakombokya makowe gamakiye Yesu. Pai panga kabla ngoko anabeka kwaa walowa nikana mara itatu. Ngapita panja kono kalela.

< Mateyu 26 >