< Levitiko 16 >

1 Atafa ana awiri a Aaroni amene anaphedwa atapita pamaso pa Yehova mosayenera, Yehova anayankhula ndi Mose.
INkosi yasikhuluma kuMozisi emva kokufa kwamadodana amabili kaAroni ekusondeleni kwawo phambi kweNkosi, asesifa.
2 Yehova anawuza Mose kuti, “Uza mchimwene wako Aaroni kuti asamalowe ku Malo Wopatulika, kuseri kwa katani, pamaso pa chivundikiro cha Bokosi la Chipangano nthawi iliyonse imene akufuna kuopa kuti angadzafe, pakuti Ine ndimaoneka mu mtambo umene uli pamwamba pa chivundikiro cha Bokosi la Chipangano.
INkosi yasisithi kuMozisi: Khuluma kuAroni umnewenu ukuthi angangeni langasiphi isikhathi endaweni engcwele ngaphakathi kweveyili, phambi kwesihlalo somusa esiphezu komtshokotsho, ukuze angafi; ngoba ngizabonakala eyezini phezu kwesihlalo somusa.
3 “Aaroni azilowa Malo Wopatulika Kwambiri motere: azitenga mwana wangʼombe wamwamuna kuti akhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza.
Elalokhu uAroni uzangena endaweni engcwele: elejongosi ithole lenkomo, libe ngumnikelo wesono, lenqama ibe ngumnikelo wokutshiswa.
4 Azivala mwinjiro wopatulika wa nsalu yosalala, azivalanso kabudula wa mʼkati wa nsalu yosalala, azimanga lamba wa nsalu yosalala, ndipo avalenso nduwira ya nsalu yosalala kumutu. Zimenezi ndi nsalu zopatulika ndipo atasamba thupi lonse azivala zimenezi.
Uzakwembatha isigqoko esingcwele lelembu elicolekileyo, lokabhudula wangaphansi welembu elicolekileyo uzakuba senyameni yakhe, azibophe ngebhanti lelembu elicolekileyo, athandele ngeqhiye yelembu elicolekileyo; lezi yizembatho ezingcwele. Ngakho uzageza umzimba wakhe ngamanzi, azembathe.
5 Kuchokera pa gulu la Aisraeli, Aaroni azitenga mbuzi zazimuna ziwiri kuti zikhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza.
Lakunhlangano yabantwana bakoIsrayeli uzathatha izimpongo ezimbili zembuzi zibe ngumnikelo wesono, lenqama eyodwa ibe ngumnikelo wokutshiswa.
6 “Aaroni apereke ngʼombe yayimuna kuti ikhale yopepesera machimo a iye mwini kuti achite mwambo wopepesera machimo ake pamodzi ndi a banja lake.
Njalo uAroni uzanikela ijongosi lomnikelo wesono elingelakhe, azenzele inhlawulo yokuthula lokwendlu yakhe.
7 Kenaka atenge mbuzi ziwiri zija ndipo aziyimike pamaso pa Yehova pa khomo la tenti ya msonkhano.
Athathe impongo ezimbili, azibeke phambi kweNkosi emnyango wethente lenhlangano.
8 Aaroni ndiye achite maere pa mbuzi ziwirizo kuti imodzi ikhale ya Yehova, ndipo inayo ikhale ya Azazele.
UAroni uzakwenza-ke inkatho phezu kwezimpongo ezimbili, enye inkatho ibe ngeyeNkosi lenye inkatho ibe ngeyempongo yokususa.
9 Aaroni abwere ndi mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi ya Yehova, ndipo apereke kuti ikhale nsembe yopereka chifukwa cha tchimo.
UAroni uzasondeza-ke impongo okuphezu kwayo inkatho yeNkosi, ayenze ibe ngumnikelo wesono;
10 Koma mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi yosenza machimo, apereke ya moyo pamaso pa Yehova, kuti achite mwambo wopepesera machimo pa mbuziyo poyitumiza ku chipululu kuti ikhale ya Azazele.
kodwa impongo okuphezu kwayo inkatho yempongo yokususa uzayibeka iphilile phambi kweNkosi ukwenza inhlawulo yokuthula ngayo, ukuyiyekela ihambe njengempongo yokususa enkangala.
11 “Aaroni apereke ngʼombe yayimuna kuti ikhale nsembe yopepesera machimo ake. Ndiye achite mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake pamodzi ndi banja lake. Pambuyo pake aphe ngʼombe yopepesera machimo ake aja.
Njalo uAroni uzasondeza ijongosi lomnikelo wesono elingelakhe, azenzele inhlawulo yokuthula leyendlu yakhe; ahlabe ijongosi lomnikelo wesono elingelakhe.
12 Kenaka iye atenge chofukizira chodzaza ndi makala a moto ochokera pa guwa lansembe pamaso pa Yehova. Atengenso lubani wonunkhira ndi woperapera wokwanira manja awiri, ndipo alowe naye kuseri kwa katani.
Athathe umganu wokutshisela impepha ugcwele amalahle omlilo avele elathini phambi kweNkosi, lezandla zakhe zigcwele impepha elephunga elimnandi echolisisiweyo, akulethe ngaphakathi kweveyili,
13 Athire lubani pa moto pamaso pa Yehova kuti utsi wa lubaniyo uphimbe chivundikiro chimene chili pamwamba pa Bokosi la Chipangano, kuti Aaroniyo asafe.
abeke impepha phezu komlilo phambi kweNkosi, ukuze iyezi lempepha lisibekele isihlalo somusa esiphezu kobufakazi, ukuze angafi.
14 Ndipo atenge magazi ena a ngʼombeyo, awawaze ndi chala chake pa chivundikiro cha kummawa; kenaka awaze magaziwo ndi chala chake kasanu ndi kawiri patsogolo pa chivundikirocho.
Athathe okwegazi lejongosi, alifafaze ngomunwe wakhe phezu kwesihlalo somusa empumalanga; langaphambi kwesihlalo somusa uzafafaza okwegazi kasikhombisa ngomunwe wakhe.
15 “Kenaka Aaroni aphe mbuzi ya nsembe yopepesera machimo a anthu, ndipo magazi ake alowe nawo kuseri kwa katani ndi kuchita chimodzimodzi monga anachitira ndi magazi a ngʼombe aja: Aaroni awaze magaziwo pa chivundikiro chija ndi patsogolo pa chivundikirocho.
Abesehlaba impongo yomnikelo wesono engeyabantu, alethe igazi layo ngaphakathi kweveyili, enze ngegazi layo njengokwenza kwakhe ngegazi lejongosi, alifafaze phezu kwesihlalo somusa laphambi kwesihlalo somusa.
16 Pamenepo ndiye kuti wansembeyo wachita mwambo wopepesera ku Malo Wopatulika chifukwa cha kudetsedwa ndi kuwukira kwa Aisraeli pa machimo ena aliwonse amene achita. Achite chimodzimodzi ndi tenti ya msonkhano imenenso ili yodetsedwa chifukwa cha machimo awo.
Ngalokho uzakwenzela indawo engcwele inhlawulo yokuthula, ngenxa yokungcola kwabantwana bakoIsrayeli, langenxa yeziphambeko zabo, ezonweni zabo zonke. Futhi uzalenzela njalo ithente lenhlangano, elihlala labo phakathi kokungcola kwabo.
17 Mu tenti ya msonkhano musakhale munthu ndi mmodzi yemwe nthawi imene Aaroni akupita kukachita mwambo wopepesera ku Malo Wopatulika mpaka atatulukako. Musakhale munthu mu tenti ya msonkhano mpaka atachita mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake, banja lake ndi gulu lonse la Aisraeli.
Kakungabi khona lamuntu ethenteni lenhlangano, ekungeneni kwakhe ukwenza inhlawulo yokuthula endaweni engcwele aze aphume, esezenzele inhlawulo yokuthula, leyendlu yakhe, leyebandla lonke lakoIsrayeli.
18 “Kenaka, Aaroniyo akatuluka apite ku guwa limene lili pamaso pa Yehova ndi kulichitira mwambo wolipepesera. Atengeko magazi a ngʼombe yayimuna ndiponso magazi a mbuzi ndi kuwapaka pa nyanga zonse za guwa lansembe.
Uzaphumela-ke elathini eliphambi kweNkosi, alenzele inhlawulo yokuthula, athathe okwegazi lejongosi lokwegazi lempongo, akufake empondweni zelathi inhlangothi zonke;
19 Magazi ena awawaze pa guwalo ndi chala chake kasanu ndi kawiri kuliyeretsa ndi kulipatula kuchotsa zodetsa za Aisraeli.
afafaze okwegazi phezu kwalo kasikhombisa ngomunwe wakhe, alihlambulule, alingcwelise ekungcoleni kwabantwana bakoIsrayeli.
20 “Aaroni akatsiriza mwambo wopepesera Malo Wopatulika, tenti ya msonkhano ndi guwa, azibwera ndi mbuzi yamoyo kudzayipereka nsembe.
Lapho eseqedile ukwenzela indawo engcwele ukubuyisana, lethente lenhlangano, lelathi, uzasondeza impongo ephilayo;
21 Aaroni asanjike manja ake pa mutu wa mbuziyo ndipo awulule pa mbuziyo zoyipa zonse ndi zowukira zonse za Aisraeli, kutanthauza machimo awo onse. Machimowo awayike pa mutu wa mbuziyo. Kenaka munthu amene anasankhidwa athamangitsire mbuziyo ku chipululu.
uAroni abeke-ke izandla zakhe zombili enhlokweni yempongo ephilayo, avume phezu kwayo bonke ububi babantwana bakoIsrayeli, leziphambeko zonke zabo, lezono zabo zonke, akubeke enhlokweni yempongo, ayiyekele ihambe ngesandla sendoda efaneleyo, iye enkangala.
22 Mbuziyo isenze machimo awo onse ndi kupita nawo kutali ndipo munthuyo aleke mbuziyo kuti ipite ku chipululuko.
Impongo izathwala-ke phezu kwayo bonke ububi babo, iye emmangweni owehlukanisiweyo; njalo izayiyekela impongo iye enkangala.
23 “Pambuyo pake Aaroni alowe mu tenti ya msonkhano ndi kuvula zovala zosalala zija zimene anavala polowa ku Malo Wopatulika ndi kuzisiya komweko.
LoAroni uzangena ethenteni lenhlangano, akhulule izembatho zelembu elicolekileyo abezembethe ekungeneni kwakhe endaweni engcwele, azitshiye khona,
24 Asambe thupi lonse ku Malo Wopatulika ndi kuvala zovala zake za nthawi zonse. Kenaka atuluke ndi kukapereka nsembe yopsereza ya iye mwini, ndiponso nsembe yopsereza yoperekera anthu. Akatero ndiye kuti wachita mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake ndi a anthu.
ageze umzimba wakhe ngamanzi endaweni engcwele, agqoke izembatho zakhe, aphume, enze umnikelo wakhe wokutshiswa lomnikelo wokutshiswa wabantu, azenzele yena inhlawulo yokuthula leyabantu.
25 Mafuta a nyama yopepesera machimo awatenthe pa guwa lansembe.
Lamahwahwa omnikelo wesono uzawatshisa elathini.
26 “Tsono munthu amene anaperekeza mbuzi yosenza machimo ija achape zovala zake ndi kusamba. Pambuyo pake alowe ku msasa.
Lalowo oyekele impongo njengempongo yokususa uzahlamba izembatho zakhe, ageze umzimba wakhe ngamanzi, emva kwalokho angene enkambeni.
27 Ngʼombe ndi mbuzi zoperekera nsembe yopepesera machimo zimene magazi ake anabwera nawo kuti achitire mwambo wopepesera Malo Wopatulika, azitulutsire kunja kwa msasa. Koma zikopa zake, nyama yake ndi matumbo ake azitenthe.
Kodwa ijongosi lomnikelo wesono lempongo yomnikelo wesono, ogazi lazo langeniswa ukwenza inhlawulo yokuthula endaweni engcwele, zizakhitshelwa ngaphandle kwenkamba; babesebetshisa izikhumba zazo lenyama yazo lomswane wazo ngomlilo.
28 Munthu amene azitenthe achape zovala zake ndi kusamba. Pambuyo pake alowe mu msasa.
Lalowo okutshisayo uzahlamba izembatho zakhe, ageze umzimba wakhe ngamanzi, emva kwalokho angene enkambeni.
29 “Ili likhale lamulo lanu lamuyaya: Mwezi wachisanu ndi chiwiri, pa tsiku la khumi la mwezi, mugonje pamaso pa Yehova. Musamagwire ntchito iliyonse, kaya ndinu mbadwa kapena mlendo amene akukhala pakati panu,
Kuzakuba yisimiso esaphakade kini: Ngenyanga yesikhombisa ngolwetshumi lwenyanga lizathobisa imiphefumulo yenu, lingasebenzi lamsebenzi, owokuzalwa elizweni lowemzini ohlala njengowezizwe phakathi kwenu.
30 chifukwa tsiku limeneli kudzachitika mwambo wopepesera machimo anu, kukuyeretsani kuti mukhale oyeretsedwa ku machimo anu pamaso pa Yehova.
Ngoba ngalolusuku uzalenzela inhlawulo yokuthula ukulihlambulula; kuzo zonke izono zenu phambi kweNkosi lizahlanjululwa.
31 Limeneli ndi tsiku lanu la Sabata lopumula, ndipo muzigonja pamaso pa Yehova. Limeneli ndi lamulo lanu la muyaya.
Kulisabatha lokuphumula kini; njalo lizathobisa imiphefumulo yenu; kuyisimiso saphakade.
32 Wansembe amene wadzozedwa ndi kupatulidwa kuti akhale wansembe kulowa mʼmalo mwa abambo ake ndiye azichita mwambo wopepesera machimo atavala zovala zake zosalala ndi zopatulika.
Njalo umpristi ogcotshiweyo, owehlukaniselwe ukusebenza njengompristi esikhundleni sikayise, uzakwenza inhlawulo yokuthula, agqoke izembatho zelembu elicolekileyo, izembatho ezingcwele,
33 Adzachite mwambo wopepesera machimo Malo Wopatulika, tenti ya msonkhano ndi guwa lansembe. Adzachitenso mwambo wopepesera anzake ndi gulu lonse la anthu.
enzele inhlawulo yokuthula indawo engcwele ngcwele, lethente lenhlangano, lelathi uzakwenzela inhlawulo yokuthula, labapristi labantu bonke bebandla uzabenzela inhlawulo yokuthula.
34 “Ili likhale lamulo lanu lamuyaya. Mwambo wopepesera machimo uzichitika kamodzi pa chaka chifukwa cha machimo a anthu onse.” Ndipo Mose anachita monga momwe Yehova analamulira.
Lokhu kuzakuba yisimiso esilaphakade kini, ukwenzela inhlawulo yokuthula abantwana bakoIsrayeli kanye ngomnyaka ngazo zonke izono zabo. Wenza-ke njengokuba iNkosi yalaya uMozisi.

< Levitiko 16 >