< Yobu 4 >

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,
Na Eliphaz el fahk, “Job, ku kom ac toasrla nga fin sramsram?
2 “Ngati wina atakuyankha, kodi ungakhumudwe? Koma ndani angakhale chete wosayankhula?
Nga koflana misla ac tia fahk nunak luk.
3 Taganiza momwe iwe walangizira anthu ambiri, momwe walimbitsira anthu ofowoka.
Kom luti mwet puspis tari, Ac akkeye poun mwet su munas.
4 Mawu ako analimbitsa anthu ofuna kugwa; unachirikiza anthu wotha mphamvu.
Ke pacl sie mwet el munasla ac tukulkul, Kas lom tuh akkeyal elan tuyak.
5 Koma tsopano mavuto akufikira ndipo wataya mtima, zakukhudza ndipo uli ndi mantha.
Na inge ke kom pa sun ongoiya uh, Kom arulana lofongla kac.
6 Kodi kuopa Mulungu kwako sindiko kulimbika mtima kwako? Ndipo moyo wako wosalakwa ndiye chiyembekezo chako?
Kom tuh alu nu sin God, ac moul lom arulana suwohs; Ke ma inge fal na in oasr lulalfongi ac finsrak lom.
7 “Ganiza bwino tsopano: Kodi munthu wosalakwa anawonongekapo nʼkale lonse? Nʼkuti kumene munthu wolungama mtima anaphedwa?
Srike esam lah acnu oasr pacl se sie mwet suwoswos el sun ongoiya, Ku sie mwet wangin mwata el wotla liki sou lal?
8 Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa, ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.
Nga liye tari ke mwet uh ac taknelik orekma sesuwos, In ima lun ma koluk; Na elos ac kosrani pac sesuwos ac ma koluk.
9 Iwo amaphedwa ndi mpweya wa Mulungu; amawonongeka ndi mpweya waukali wa mkwiyo wake.
In kasrkusrak lun God, El kunauselosla oana sie paka.
10 Mikango imabangula ndi kulira, komabe mano a mikango yamphamvu amathyoledwa.
Mwet koluk elos kou ac wowo oana lion uh, Tuh God El kutongulosi ac kotala wihselos.
11 Mkango umafa chifukwa chosowa nyama, ndipo ana amkango amamwazikana.
Oana luman lion su wangin ma elan uniya ac kang, Elos ac misa, ac tulik natulos nukewa fahsrelik.
12 “Mawu anabwera kwa ine mwamseri, makutu anga anamva kunongʼona kwake.
“Sie pacl ah oasr kas se tuku kakasrisrikna; Aok arulana srikla pusra, apkuranna ngan tia ku in lohng.
13 Mʼkati mwa maloto ochititsa mantha usiku, nthawi imene anthu amagona tulo tofa nato,
Pusra se inge lusrongla motul luk ah oana sie mweme koluk. Nga rarrar,
14 ndinagwidwa ndi mantha, ndi kuyamba kunjenjemera ndipo mafupa anga onse anaweyeseka.
Ac monuk nufon usrusryak ke sangeng.
15 Pamenepo mzimu unadutsa pamaso panga, ndipo ubweya wa pa thupi langa unayima kuti njoo.
Sie engyeng na srisrik ukya mutuk, Ac monuk nufon tuninmihsrisrla ke sangeng.
16 Chinthucho chinayimirira koma sindinathe kuzindikira kuti chinali chiyani. Chinthu chinayima patsogolo panga, kunali zii ndipo ndinamva mawu akuti,
Nga liye lah oasr ma se tu insac; A nga ne ngetang nu kac, nga tia ku in akilen lah mea se. Mihsna in pacl sac, ac nga lohng sie pusra kasla, fahk mu:
17 ‘Kodi munthu angathe kukhala wolungama kupambana Mulungu? Kodi munthu angathe kukhala wangwiro kupambana Mlengi wake?
‘Ya sie mwet ku in suwoswos ye mutun God? Ya mwet se ku in nasnasna ye mutun El su oralla?
18 Ngati Mulungu sakhulupirira atumiki ake omwe, ngati Iye amawapeza angelo ake ndi cholakwa,
God El tia lulalfongi mwet kulansap lal inkusrao. Finne lipufan uh, El konauk lah oasr pac ma elos sufalla kac.
19 nanga kuli bwanji ndi iwo amene amakhala mʼnyumba zadothi, amene maziko awo ndi fumbi, amene amathudzuka mosavuta ngati kadziwotche!
Kom nunku mu El ku in lulalfongi sie ma su orekla ke fohk kle, Sie ma orekla ke fohk, su fisrasr in itungyuki oana sie srenyuhu?
20 Mmawa ali moyo, pofika madzulo afa; mwakachetechete, amawonongeka kwamuyaya.
Sahp sie mwet ac ku in moul ke lotutang uh, A ekela na el misa, wangin eteya.
21 Kodi zonse zimene ali nazo sizimatheratu, kotero kuti amafa osadziwa nʼkanthu komwe?’
Ma lal nukewa ac itukla lukel; El ac misa, a srakna wangin etauk in el.’

< Yobu 4 >