< Genesis 10 >

1 Nayi mbiri ya ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti. Ana atatuwa anabereka ana awo chitatha chigumula.
Teć są rodzaje synów Noego, Sema, Chama i Jafeta, którym się narodziło synów po potopie.
2 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
Synowie Jafetowi Gomer, i Magog, i Madai, i Jawan, i Tubal, i Mesech, i Tyras.
3 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.
A synowie Gomerowi: Aschenaz, i Ryfat, i Togorma.
4 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
A synowie Jawanowi: Elisa, i Tarsis, Cytym, i Dodanim.
5 (Amenewa ndiwo makolo a anthu okhala mʼmphepete mwa nyanja. Awa ndi ana a Yafeti monga mwa mafuko a mu mitundu yawo, uliwonse ndi chiyankhulo chake).
Od tych rozdzielone są wyspy narodów po swych ziemiach; każdy według języka swego, i według pokolenia swego, w narodziech swoich.
6 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani.
A synowie Chamowi: Chus, i Micraim, i Put, i Chanaan.
7 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka. Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
Synowie zaś Chusowi: Seba, i Hewila, i Sabta, i Regma, i Sabtacha. A synowie Regmy: Seba i Dedan.
8 Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
A Chus spłodził Nemroda, który począł być możnym na ziemi.
9 Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”
Ten był możnym myśliwcem przed obliczem Pańskiem; przetoż się mówi: Jako Nemrod możny myśliwiec przed Panem.
10 Malo oyambirira a ufumu wake anali Babeli, Ereki, Akadi ndi Kaline. Malo onsewa anali mʼdziko la Sinara.
A początek królestwa jego był Babel, i Erech, i Achad, i Chalne w ziemi Senaar.
11 Atachoka mʼdziko limeneli anapita ku Asiriya kumene anakamanga Ninive, Rehoboti-Iri, Kala,
Z tej ziemi wyszedł Assur, i zbudował Niniwe, i Rechobot miasto, i Chale.
12 ndi Reseni, mzinda waukulu umene uli pakati pa Ninive ndi Kala.
Także Resen, między Niniwe i między Chale; to miasto jest wielkie.
13 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
Micraim też spłodził Ludyma, i Hananima, i Laubima, i Neftuhyma.
14 Apaturusi, Akasilu ndi Akafitori (kumene kunachokera Afilisti).
I Patrusyma, i Chasluchyma, ( z których poszli Filistynowie, ) i Kaftoryma.
15 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba, Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti;
Chanaan też spłodził Sydona pierworodnego swego, i Heta.
16 Ayebusi, Aamori, Agirigasi;
I Jebusa, i Amorra, i Gergesa.
17 Ahivi, Aariki, Asini,
I Hewa, i Archa, i Syma.
18 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati. Pambuyo pake, mafuko a Akanaani anafalikira ponseponse,
I Arada, i Samara, i Chamata, skąd się potem rozrodziły domy Chananejczyków.
19 mpaka ku malire a Kanaani. Malirewo anachokera ku Sidoni kulowa cha ku Gerari mpaka ku Gaza, ndi kulowa ku Sodomu, Gomora, Adima ndi Zeboimu mpaka ku Lasa.
A granice Chananejskie były od Sydonu idąc do Gerary, aż do Gazy, aż wnijdziesz do Sodomy i Gomorry, i Adamy, i Seboima, aż do Lazy.
20 Amenewa ndiwo ana aamuna a Hamu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe amakhala ndi mitundu yawo.
Ci są synowie Chamowi w familijach swych, w językach swych, w ziemiach swych, w narodziech swych.
21 Semu amene anali mkulu wake wa Yafeti nayenso anabereka nakhala kholo la Eberi.
A Semowi, ojcu wszystkich synów Heberowych, bratu Jafeta starszego, urodzili się synowie.
22 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.
Synowie Semowi: Elam i Assur, i Arfachsad, i Lud, i Aram.
23 Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
Synowie zaś Aramowi: Hus, i Hul, i Geter, i Mesech.
24 Aripakisadi anabereka Sela, ndipo Selayo anabereka Eberi.
Arfachsad zaś spłodził Selecha, a Selech spłodził Hebera.
25 A Eberi anabereka ana aamuna awiri: Wina anamutcha Pelegi chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
A Heberowi urodzili się dwa synowie: imię jednemu Faleg, iż za dni jego rozdzielona jest ziemia; a imię brata jego Jektan.
26 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
Jektan też spłodził Elmodada, i Salefa, i Hasarmota, i Jarecha.
27 Hadoramu, Uzali, Dikila,
I Adorama, i Uzala, i Dekla.
28 Obali, Abimaeli, Seba,
I Hebala, i Abymaela, i Sebaja.
29 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
I Ofira, i Hewila, i Jobaba: ci wszyscy są synowie Jektanowi.
30 Chigawo chimene ankakhala chinayambira ku Mesa mpaka ku Seferi, ku dera la mapiri chakummawa.
A było mieszkanie ich od Mescha idąc, do góry Sefar na wschód słońca.
31 Amenewa ndiwo ana a Semu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe ankakhala ndi mitundu yawo.
Cić są synowie Semowi w domach swych, w językach swych, w ziemiach swych, w narodziech swych.
32 Amenewa ndiwo mafuko a ana aamuna a Nowa monga mwa mibado ya mitundu yawo. Mitundu yonse ya anthu inatuluka mwa iwowa ndi kufalikira pa dziko lonse lapansi chitatha chigumula chija.
Teć są domy synów Noego, według pokolenia ich, i w narodziech ich, i od nich rozdzielone są narody na ziemi po potopie.

< Genesis 10 >