< Deuteronomo 30 >

1 Madalitso ndi matemberero awa onse amene ndawayika pamaso panu akadzafika pa inu, inu nʼkukumbukira kulikonse kumene Yehova Mulungu wanu wakubalalitsirani pakati pa mitundu ya anthu,
När nu allt detta kommer öfver dig, antingen välsignelsen eller förbannelsen, som jag dig föresatt hafver, och du begynner lägga på hjertat, huru du äst ibland Hedningar, dit Herren din Gud dig fördrifvit hafver;
2 ndipo inu pamodzi ndi ana anu nʼkudzatembenukira kwa Yehova Mulungu wanu ndi kumumvera ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse molingana ndi chilichonse chimene ndakulamulani lero lino,
Och du omvänder dig till Herran din Gud, så att du lyder hans röst, du och din barn, af allo hjerta, och af allo själ, i allt det som jag bjuder dig i denna dag;
3 pamenepo Yehova Mulungu wanu adzakukhalitsani monga kale ndi kukuchitirani chifundo, ndipo adzakusonkhanitsani kukuchotsani ku mitundu ina ya anthu kumene anakubalalitsirani.
Så skall Herren din Gud vända ditt fängelse, och förbarma sig öfver dig, och skall åter församla dig utur all folk, dit Herren din Gud dig förskingrat hafver.
4 Ngakhale atakupirikitsirani ku malekezero a dziko lapansi, adzakusonkhanitsani kuchokera kumeneko ndi kukubweretsaninso.
Om du vore bortdrifven allt intill himmelens ända, så skall dock Herren din Gud församla dig dädan, och hemta dig dädan.
5 Adzakubweretsani ku dziko limene linali la makolo anu, ndipo lidzakhala lanu. Iye adzakulemeretsani ndi kukuchulukitsani kupambana makolo anu.
Och Herren din Gud skall låta dig komma i det land, som dine fäder besutit hafva; och du skall det intaga, och han skall göra dig godt, och föröka dig öfver dina fäder.
6 Yehova Mulungu wanu adzasintha mitima yanu pamodzi ndi mitima ya zidzukulu zanu, kotero kuti mudzamukonda ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse, ndipo mudzakhala ndi moyo.
Och Herren din Gud skall omskära ditt hjerta, och dine säds hjerta, att du Herran din Gud älska skall af allo hjerta, och af allo själ; på det att du må lefva.
7 Yehova Mulungu wanu adzayika matemberero awa onse pa adani anu amene amadana nanu ndi kukuzunzani.
Men denna förbannelsen skall Herren din Gud alla låta komma uppå dina fiendar, och uppå dem som dig hata och förfölja.
8 Inu mudzamveranso Yehova ndi kutsatira malamulo ake onse amene ndikukupatsani lero lino.
Men du skall omvända dig, och lyda Herrans röst, att du gör all hans bud, som jag bjuder dig i dag.
9 Pamenepo Yehova Mulungu wanu adzakulemeretsani pa zochita zanu zonse ndipo adzakupatsani ana ambiri, zoweta zambiri, ndiponso mudzakhala ndi zokolola zambiri za mʼdziko lanu. Yehova adzakondwera nanunso ndi kukulemeretsani monga momwe anakondwera ndi makolo anu,
Och Herren din Gud skall gifva dig lycko i alla dina händers gerningar; i dins lifs frukt, i dins boskaps frukt, i dins lands frukt, att det kommer dig till godo; ty Herren skall vända sig, så att han skall fröjda sig öfver dig, dig till godo, såsom han sig öfver dina fäder fröjdat hafver;
10 ngati mudzamvera Yehova Mulungu wanu ndi kusunga malamulo ake ndi mawu ake amene alembedwa Mʼbuku ili la Malamulo ndi kutembenukira kwa Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
Derföre, att du Herrans dins Guds röst lyder, till att hålla hans bud och rätter, som skrifne äro i desso lagbok; såframt du vänder dig till Herran din Gud af allo hjerta, och af allo själ.
11 Tsopano zimene ndikukulamulirani leroli sizovuta kapena zapatali.
Ty det budet, som jag bjuder dig i dag, är dig icke fördoldt, ej heller för fjerran;
12 Sizili kumwamba, kuti muzichita kufunsa kuti, “Kodi ndani amene akwere kumwamba kuti akazitenge ndi kudzatilalikira kuti timvere?”
Ej heller i himmelen, så att du måtte säga: Ho vill fara oss upp i himmelen, och hemta oss det, att vi måge hörat och görat?
13 Komanso sizili pa tsidya la nyanja, kuti muzichita kufunsa kuti, “Kodi ndani amene adzawoloke nyanja kuti akatenge ndi kudzatilalikira kuti timvere?”
Det är icke heller på hinsidon hafvet, så att du måtte säga: Ho vill fara oss öfver hafvet, och hemta oss det, att vi måge hörat och görat?
14 Ayi, mawu ali pafupi ndi inu; ali mʼkamwa mwanu ndi mu mtima mwanu kuti muwamvere.
Ty ordet är ganska hardt när dig, i dinom mun, och i dino hjerta, att du det göra må.
15 Taonani, lero ine ndayika pamaso panu moyo ndi zokoma, imfa ndi chiwonongeko.
Si, jag hafver i dag satt dig före lifvet, och det goda; döden, och det onda;
16 Pakuti lero ndikukulamulani kuti mukonde Yehova Mulungu wanu, kuti muyende mʼnjira zake, ndi kusunga malamulo ake, malangizo ake. Mukatero mudzakhala ndi moyo ndi kuchulukana, ndipo Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani mʼdziko limene mukulowa kukakhalamo.
Det jag bjuder dig i dag, att du skall älska Herran din Gud, och vandra i hans vägar, och hålla hans bud, lag och rätter, och få lefva, och varda förökad; och Herren din Gud skall välsigna dig i landena, der du indrager till att intaga det.
17 Koma ngati mtima wanu udzatembenuka, inu nʼkukhala osandimvera, ndipo ngati mudzatengeka ndi kupita kukagwadira milungu ina ndi kuyipembedza,
Men vänder du ditt hjerta, och lyder icke, utan låter förföra dig, så att du tillbeder andra gudar, och tjenar dem;
18 lero ndikulengeza kwa inu kuti mudzawonongeka ndithu. Simudzakhala nthawi yayitali mʼdziko limene mukulowamo pamene mukuwoloka Yorodani kuti mulitenge.
Så förkunnar jag eder i dag, att I skolen förgås, och icke länge blifva i landena, der du indrager öfver Jordan, det att intaga.
19 Lero kumwamba ndi dziko lapansi zikhale mboni zodzakutsutsani pakuti ndayika pamaso panu moyo ndi imfa, madalitso ndi matemberero. Tsopano sankhani moyo kuti inu ndi ana anu mukhale ndi moyo.
Jag tager i dag himmel och jord till vittne öfver eder, jag hafver satt eder före lifvet och döden, välsignelse och förbannelse, att du skall utvälja lifvet, och du och din säd mågen lefva;
20 Ndi kuti mukonde Yehova Mulungu wanu, kumvera mawu ake, ndi kukhulupirika kwa Iye. Pakuti Yehova ndiye moyo wanu, ndipo mudzakhala zaka zambiri mʼdziko limene analumbira kulipereka kwa makolo anu, Abrahamu, Isake ndi Yakobo.
Att I skolen älska Herran edar Gud, och lyda hans röst, och hålla eder intill honom; ty det är ditt lif, och din långa ålder, att du må bo i landena, som Herren dina fäder, Abraham, Isaac och Jacob, svorit hafver dem att gifva.

< Deuteronomo 30 >